83% found this document useful (6 votes)
9K views107 pages

Reformed Church in Zambia Nyimbo Za Khristu (Hymn) (Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Download as pdf or txt
Download as pdf or txt
Download as pdf or txt
You are on page 1/ 107

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)

(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Mwana wosatha wa Atate ndinu!


Simunanyoza mimba ya Namwali
1 Potipulumutsa.
1. NDINU wakuyera! Wamphamvu 7. Imfa mutagonjetsa ndi zoŵaŵa.
zonse. Njira munatsegula tikaloŵe
Nthaŵi ya m’mamaŵayi tiimba Momwe mukhala Inu ndi Atate
nyimboyi. Mwaulemerero
Mlengi wachifundo, tikuyamikani, 8. Kumva milandu yathu mudzabwera
E! Mlungu Mmodzi mwa Atatuwo. Mutithandize, atumiki anu;
2. Ndinu Wakuyera! Anthu ochuluka Mwatiwombola nawo mwazi wanu:
Akuimbirani, nakupempharanibe; Mutipulumutse.
Akumwamba omwe nagwadira Inu, 9. Mtiŵerengere m’Mwamba ndi oyera;
Wachikhalire ndi wosafa ’yi. Mutidalitse, ndife anthu anu;
3. Ndinu wakuyera! Ife akuchimwa Moyo wosatha, mutipatse tonse,
Zaulemerero zanu sitiona’yi; Mutilamule.
Mwayera nokha, wina saoneka 10. Tsiku ndi Tsiku timalemekeza:
Wangwiro m’mphamvu ndi Nanu tikukuzani osaleka;
m’kuyeramo. Mbuye, mtisunge tingachimwe lero;
4. Ndinu wakuyera! Zakumwamba zonse Mtichitire nsisi.
Ndi zapansi zitamabe dzina lanulo; 11. Mbuye, chifundo chanu chitigwere
Mlengi wachifundo, Mphambi, Monga tikhulupira inu nokha:
Ambuyathu, Ndakhulupira zedi mwanu, Mbuye
E! Mlungu Mmodzi mwa Atatuwo. Ndisagome konse!
2 3
1. INU Mulungu, tikuyamikani; 1. ATATE wa Kumwambako,
Tivomereza ndinu Ambuyathu; Munawombola ife ndi
Ponse, atate, akugwadirani, Chikondi chanu chijacho;
Ndinu wamuyaya! Tiyamikira Inutu.
2. Nanu akukuzani amithenga, 2. Ambuye Yesu Inutu
Nanu zam’mwamba ndi zamphamvu Munabadwira anthu ’fe;
zake, Munatifera tonsefe;
Nanu angelo a mitundu yonse Tiyamikira Inutu.
Akuimbirani: 3. Mzimu Woyera, m’mtimamo
3. Mbuye Woyera! E, Woyera nokha! Tiyeretsedwe ndinutu;
Mbuye Woyera! Mbuye wa makamu! Munatisunga bwinoli;
Ponse ulemu wanu ndi wodzaza Tiyamikira Inutu.
Pansi ndi Kumwamba.” 4. Atate, Mwana, Mzimunso,
4. Nanu Atumwi akumveka aja, Ndinu Atatu Mmodzitu,
Ndi Aneneri oyanjana omwe,
2
Ndi aunyinji anakuferani
Ochimwa tikupemphani:
Akuyamikani.
Mutikhululukire ’fe
5. Mpingo woyera wa kwa anthu onse
Ukumverani Mfumu ndi Atate, 4
Mwana woona wa ulemu wonse, 1. LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
Mzimu Nkhoswe yemwe. Lemekeza Mulungu Mwana,
6. Khristu Mfumuyo yaulemerero! Lemekeza Mulungu Mzimu,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Mulungu Mmodzi ndi wamkulu, Yogunda mvula m’mlengalengamo,


Lemekeza, lemekeza Mawu akulu muzinenadi:
Mulungu wathu yemweyo. Aleluya.
2. Mlemekeze, anakonda 2 Paphiri paja papakulupo,
Natitsuka m’mtima mwathu; Pamwala ponse pakuŵala mbuu!
Anatiwombola ife Mumvomereze mawu omwewo:
Tikakhale ndi chifumu. Aleluya.
Lemekeza, lemekeza 3 Mphepo yay’kulu yakuwombayo,
Yesu Mbuye Nsembeyo. Chisanu chija chozizirachi,
3. Lemekeza Mfumu yathu, Ndi kabvumbulu muzinenadi;
Mfumu ya mipingo yonse, Aleluya.
Ipambana anthu onse 4 Mitengo yaitalitali ’nu
Akumwamba ndi apansi. Yachiimire mumaimabe,
Lemekeza, lemekeza Mubvomereze ndi kunenabe:
Mfumu ya mafumuyo. Aleluya.
5 Zam’madzi zonse zakuopsyazo,
Nyanja, matiti ndi mitsinjeyo,
5 Chigumula chakulindimacho,
1. Ndi aleluya imbirani Aleluya.
Tate wathu wakumwamba, 6 Zamoyo zili m’thengo zonsezo,
Analenga zones, Zodzuma, zina zobangulazo,
Chifundo chache chachikulu, Zimene ndi kulira konseko:
Nzeru mphamvu ndi unfumu, Aleluya.
Tayamike tonse. 7 Inu mumvere anyamatawo,
2. Ndi aleluya imbirani Okondedwa kuseŵerako,
Yesu Kristu Mpulumutsi, Mumtima mubvomere monsemo:
Anachoka kwawo, Aleluya.
Nakhala munthu pansi pano, 8 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
Nasauka, natifera, Ndi ana osakula msinkhu ’nu
……… mawu, Ana a Mulungu mubvomeretu:
3. Ndi aleluya imbirani Aleluya.
Mzimu wake wakuyera 9 Akulu nonse ndi mafumu ’nu
Amakhala nafe. Magulu nonse apadzikopa,
Atilangisa na Mulungu Mumlemekeze Mbuye yemweyo:
Nayeretsanso mitima Aleluya.
ya akristu ife. 10 Ndi amithenga akumwambako,
4. Mulungu wathu tiyamika, Ndi anthu ndi zamoyo zonsezo,
“Tate, Mwana, Mzimu yemwe,” Bvomerezani mau omwewo:
Aleluya inu. Aleluya.
Woyera inu ndi wamphamvu, 7
Muyenera anthhu onse
1. TAMANI Ambuye,
Agwadira inu.
Wamphamvu ndi Iye
Akhala m’ulemu
6 Kumwamba komweko:
Chikopa cholimba
1 MITAMBO inu yakumwambako

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Ndi kothaŵiranso 2. Mulungu yemweyo


Kwa anthu akewo, Akhale m’fupi mwathu;
Kotero ndi Mlungu. Mtendere wakewo
2. Uzani zamphamvu, Ukhale m’mtima mwathu;
Imbani chisomo, Titsate Iyedi
Za Mwini ulemu, Ndi nsoni zakezo,
Ambuye wathuyo; Panjira yakeyi
Powomba chimphepo Masiku onsewo.
Mvulanso ndi bingu 3. Tilemekezetu
Padziko, pathambo, Atate wakumwamba,
Akhala ponsepo. Ndi Yesu Mbuyathu,
3. Zozizwa za m’dziko, Ndi Mzimu Wakuyera;
Za m’mwamba zonsezi, Mulungu Mmodziyu
Mulungu wamphamvu, Wanthaŵi zonsezo,
Munalenga zonse; Timlemekezetu
Muyendetsa mwezi Masiku onsewo.
3 9
Nyenyezi ndi dzuŵa: 1. NDI mitima yokondwera
Zolengedwa zonse Mbuye wathu tiyamika.
Zimvera Ambuye. E, chifundo chake chonse
4. Sitiha ifedi Ndi chosatha nthaŵi zonse.
Kukamba zokoma 2. Dzina Lake Tibukitsa,
Za Inu Mulungu Mlungu ndiye yekhayekha.
Wolera anthuwa; 3. Mphamvu yake inalenga
Zifika ndi mphepo Dziko lonse ndi kumwamba.
Ndi mvula ndi dzuŵa, 4. Anatsogolera kale
Zigwera ponsepo M’chipululu anthu ake.
Pa anthu onsewa. 5. Ndi chifundo atipenya
5. Wamphamvu yosatha, Ife anthu osauka.
Chikondi changwiro, 6. Amaŵeta nyama zonse.
Angelo akonda Zingasoŵe kanthu konse.
Kutama Mulungu; 7. Tiimbire Mlungu wathu
Ndiponso ifetu Waulemu ndi wamkulu.
Ananu tonsefe 8. Tithaŵire kwa Mulungu,
Tiyimba nyimboyi Ndiko tikapeze moyo.
Yotama Ambuye.
10
8 1. NDITAMATU Ambuyangayu,
1. TSOPANO linoli Moyo wanga wonse ndidzamtamatu,
Tiimbe nyimbo zathu; Ndiponso dziko lakumwambako;
Tiimbe nyimbozi, Masiku anga onse ndidzamlemekeza
Titame Mlungu wathu; Iye;
Masiku onsewo Sindizaleka konsekonse m’mene ndili
Anatisungadi, m’moyotu,
Anatipatsanso Padziko pano pena m’Mwambamo.
Zabwino zonsezi. 2. Ndiye wokondwa, E, munthuyo

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Wokhulupirira Mlungu yekhadi, 3. Okwaŵa pansi inu,


Wolenga dziko, nyanja, zonsezi; Oyenda m’madzi inu,
Choona chake chonse chingokhalatu Oyesa dziko nkwanu,
chosatha; Am’mlengalenga inu,
Apulumutsa onse namadyetsa anthu Nonsenu ntchito zake
akewo, Muona tsiku n’tsiku,
Wokonda ndiye Mbuye wathuyo. Saleka kusamala
3. Mlungu kuona athiratu Ndikudalitsa inu.
Inde m’maso awo osapenyawo. 4. Nditama mphamvu yake
Natuma akumvera mpumulo; Ya Mlungu yondizinga;
4 N’kafoka an’limbitsa,
Amathandiza inde aulendo awo N’kadwala andichiza
ofokatu, Pakundisiya bwenzi
Akazi amasiye maka ndi anawo Mulungu ali paja;
onsewo, N’kaloŵa imfa ine
Olira otonthoza mtimadi. Alipo Mlungu wanga.
4. Nditama Ambuyangayu, 12
Moyo wanga wonse ndidzamtamatu 1. Mtima wanga uyamike
Ndiponso m’dziko lakumwambako; MfumuYakumwambako;
Masiku anga onse ndidzamlemekeza Anandiwombola ine
Iye: Nanditsuka m’mtimamo
Sindidzaleka konsekonse m’mene Ife tonse, ife tonse,
ndili m’moyotu, Tiyamike Mlunguyo.
Padziko pano pena m’Mwambamo. 2. Tiyamike Mulungu wathu,
11 Kaamba ka chifundocho;
1. Paphiri ndi padambo Nthaŵi zonse sasanduka
Ponsepo pali Mlungu, Mlungu wathu yemweyo
Poyenda ife m’njira 3. Nthaŵi zonse monga ‘Tate
Mpoima pali Mlungu; Atisamaliratu,
Kokwera Maganizo, Atisunga m’manja mwake,
Komwe kuli Mlungu, Atipulumutsatu.
Kumwamba ndi pansipo 4. Anthu a mitundu yonse,
Ponsepo pali Mlungu. Ndipo a Kumwambako,
(Mulungu ali nane!) Yamikani Mungu wathu,
(Ali nane, ali nane, ali nane Ndiye wakukomatu.
Ali nane, Aa! Anthu onse, anthu onse,
Mulungu ali nane!) Yamikani Mlunguyo.
2. Ndi maso Ambuyathu 13
Apenyetsetsa ife; 1. YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
Amadalitsa onse sin’ngasoŵe konse:
Okhulupira Iye; Andigonetsa pali busa
Amamva timbalame, la misipu yonse.
Nabveka dziko lonse; (Ndiye Mbusa wanga,
Sataya tizirombo, Ndiye Mbusa wanga!
Asunga zina zonse. Yehova ndiye Mbusa wanga,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Sin’ngasoŵe konse.) Aleluya! Kondwerani!


2. Kumadzi kuli njiratu Mlungu wathu yamikani!
5 15
andiyendetsa bwino, 1. MULUNGU ndiye Mbusa wanga,
Nalimbikitsa moyo wanga sindisoŵa konse;
ndi chifundo chino. Amandiŵeta nandidyetsa
3. Pabande lolunjika nandipatsa zonse.
andilondolera njira; (Ndiye Mbusa wanga,
Chifukwacho cha dzina lake Ndiye Mbusa wanga!
anandisungira. Mulungu ndiye Mbusa wanga,
4. Chigwa choopsacho cha imfa Sindisoŵa konse)
ndikachiloŵera, 2. M’mitsinje yamtendere mtima
Ndilibe mantha, muli ndine, wanga aumwetsa;
ndodo ndiigwira. Mapazi omwe m’njira
5. Pamaso pa adaniwo Yolungama nayendetsa.
mwayala gome langa; 3. Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa
E, mutu mwaudzoza, sindiopa;
chisefuka chikho changa. Ndikakhumudwa ndi kutopa,
6. Zabwino ndi zokoma Andipulumutsa.
zinditsata chitsatire; 4. Podwala ine pobvutidwa
E, m’nyumba ya Yehova Andisamalira;
ndidzakhala chikhalire. Pondisauts’ adani anga
14 nandithangatira.
1. MTIMA wanga lemekeza 5. Chisomo ndi zokoma zake
Mlungu wako ndi Chimwemwe. sizileka konse;
Nthaŵi zonse ndimtamanda; Ndi m’nyumba ya Mulungu
Ndimwimbira nyimbo zanga. Ndidzakhala nsiku zonse.
Moyo, mphamvu, nzeru zonse, 16
Zidzamlekeza konse. 1. ZOBVUTA zoopsya ndi zosaukazi
2. Ndi wamwayi munthu uja Sitingathe ife kuzithaŵa tokha.
Amthandiza Mbuye wake Koma Ambuyathu timtamande Iye,
Akachita mantha iye Uthenga Wabwino timveretu kokha.
Amchotsera nkhaŵa yake, 2. Amadyetsa iye mbalame
Ndipo likamgwera tsoka zam’mwamba,
Amakhulupira kokha. Timtamande ndithu potisunga ife;
3. Mbuye ndiye wachifundo, Timvere malembo a m’kalata mwake,
Achiritsa akudwala; Ambuye yemweyo atisungirabe.
Anyamula akufoka 3. Abramu kalelo anamvera bwino;
Naŵadyetsatu anjala. Timverenso ngatitu yemwe wakale.
Wakusunga mlendo ndiye, Pokhala alendo atsogoza iwo,
Nathandiza amasiye. Timkhulupirire Ambuye tonsefe.
4. Ndiye Mbuye wa ambuye;
6
Mphamvu yake ndi yokwana.
4. Timtamande Iye ndi moyo wathunso
Adzakhala chikhalire,
Pakutsatatsata malembedwe awo.
Mfumu yathu yopambana,
Tipezamo malembedwe awo.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Tipezamo malo okwanira ife Ndi Mlungu Iyeyo,


Ambuye wathu atipatsa kwawo. Anatifera anthu ’fe
17 Ndi Mulungu Iyenso.
6. Ndi m’munda muja chete, phee!
1. POKONDWA ndi poona bvuto
Pamtanda pati njo!
Ndi tsoka pena mwayi,
Anaphunzitsa ’bale ’fe
Ndikumbukira, ndiimbira
Titero ifenso.
Mulungu wangayo.
7. Kuuzani Mlungu m’Mwambamo
2. Kwezani nane Ambuyathu,
Mtamande m’kuyanso;
Timlemekeze yekha;
Nzozizwa nkhani zakezo,
Popsinja mtima ndinamtchula,
Njolimba ntchito njo!
Nandithangata ’ne
3. ANGELO amazinga nyumba 19
Za anthu olungama; 1. KALELO anthu onse
Mulungu ateteza omwe Nachimwa kwa Mulungu
Amkhulupirira. Mulungu anaona
4. Laŵani chikondano chake; Naona tchimo lawo,
Mudzadziŵitsa msanga Nafuna kwawononga,
Kudala kwawo kwa anake Nafuna kwawononga.
Omkonda Mbuyeyo. 2. Mulungu anatuma,
5. Opani iye, nimuleke Natuma mvula ija,
Kuopa kanthu kena; Nadzaza dziko lonse
Mumtumikire mokondwera, Anafa anthu onse,
Akusungani ’nu. Anafa m’mvula muja,
6. Mulungu wathu Mmodzi yekha Anafa m’mvula muja.
Atate, Mwana, Mzimu, 3. Mulungu anatuma,
Akhale ndi ulemerero Natuma Nowa uja,
Wachikhalirewo! Wamanga chombo chake,
18 Ndi chachitalitali,
Nowayo nayendamo,
1. KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
Nowayo nayendamo.
Mtamande m’kuyanso;
4. Nowayo anatuma,
Nzozizwa nkhani zakezo,
Natuma chikwangwala,
Njolimba ntchito njo!
Chatsika pansi pansi,
2. Pochimwa anthu onsewo
Chosabwerera konse,
Nja Mlungu nzeruyi;
Adamu wachiŵiriyo 7
Wathetsa tchimoli. Chithaŵa m’talitali,
3. Thupi la mwazi wathu ’li Chithaŵa m’talitali.
Lochimwa kalelo, 5. Kutuma wabwereza,
Labweranso ku nkhondoyi, Natuma nkhunda ija,
Laposa monsemo. Yatsika pamadzipo,
4. Choposa nalo thupilo Yathyolatu mayani,
Chikhale momwemu, Yampatsa Nowa yemwe,
Chiyeretsetsa m’katimo, Yampatsa Nowa yemwe.
Ndi Mulungu Iyeyu. 6. Kalelo Mbuye Yesu
5. Anatikondakonda ’Ye, ’Nafera anthu onse,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Ndiyeyo chombo chathu, Kutifikitsa m’Mwambamo.


Tikabisala mommo 3. Pakuwoloka mtsinje wa imfa
Tipulumuka mommo, Dzanja Mbuyathu agwira;
Tipulumuka mommo. Tikadagwira ntchito zake
20 Atipatsatu korona;
Komwe kulibe masauko,
1. MULUNGU aŵakonda anthu
Pena misozi maliro;
Ali pansi pano;
Mulungu tidzamtamandira,
Afuna kuŵapulumutsa
Inde kosalekezanso.
Kumilandu yawo.
A! Chikondi chachikulu 22
Mulungu ali nacho, 1. NDIKONDA Mlungu pomva
Chimam’tengera Mpulumutsi, Mbuye wanga
Andifere pano Amva pemphero ndi kulira kwanga,
2. Ndikhulupira mwa Ambuye, Namachereza khutu nditapfuula,
Mulungu namukitsa, Andithandiza, nandipulumutsa.
Imfayo indipulumutsa, 2. Mulungu wanga ndiye wachifundo
Mwazi und’yeretsa. Ndi wolungama mtima ndi wabwino;
3. Chikondi chake chindidzera Apulumutsa anthu akufoka,
M’mtima mwanga muno, Akathandiza nkhaŵa imachoka.
Chipulumutsa nditalema 3. Mtimanga, bwera kuti upumule,
Ndi machimo anga. Wakuchitiranso zokoma Mbuye,
4. Mukondwe anthu a Mulungu, Wakuchotsera imfa ndi misozi,
Tere mulandira Ndingakhumudwe asungira phazi.
Chimwemwe chija chakumwamba, 4. Nditani ine kubwezera Mbuye
Chidzaloŵa m’mtima. Zokoma zonse anandichitira?
5. Mulungu atipatsa mphamvu Chipulumutso chake ndidzatama,
Yoletsetsa tchimo; Ndinalumbira zija ndidzapatsa.
Pofika tsikulo la imfa, 5. Imfa ya anthu ake imkomera,
Tidzakhala bwino. Aŵalandira m’nyumba zokonzeka.
21 8
1. TIIMBE nyimbo zotamanda Mbuye, kapolo wanu ndipereka
Mulungu wathu wabwino, Nsembeyi yonga yanu, ndine ndekha.
Pakuti akondana nawo 23
Anthu okhala padziko; 1. TITAME Mlungu Wakumwamba,
Tero natuma Mwana wake, Timwimbire nyimbo,
Wakukondedwa kalelo, Kukoma kwake kwatipatsa
Kutiphunzitsa ife tonse Zonse tili nazo.
Za chikondano chakecho. (Timwimbire nyimbo,
2. Mulungu ndiye wachifundo, Timwimbire nyimbo!
Nadzalandira onsewa Kukoma kwake kwatipatsa
Akuulula mphulupulu Zonse tili nazo)
Ndi kukondana ndi Yesu 2. Poyamba paja analenga
Tilondelonde njira yake Zonse dziko muno,
Yopapatiza yaing’ono; Tsopano lomwe azisunga
Adzatilondolera ndiye Zonse zili moyo.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

3. Tinasokera ngati nkhosa, anandichitira zazikulu;


Moyo tinataya, Dzina la Ambuyanga
Tinakondwera ndi zoipa lili loyera kopambana.
Zonse tinatsata. 4. Ndiye amachitira
4. Komweko titasaukira, chifundo anthu a mibadwo,
Titafuna kufa, E! a mibadwo yonse
Atate anatilondola yakumuopa ndi kummvera.
Naitana ife. 5. Iye amazichita
5. Tiyeni tizipita kwathu, zamphamvu nawo mkono wake;
Tisasokerenso, Iye nabalalitsa
Tilape m’mtima kuti omwe anyada nadzitama
tikakhale ndi Mulungu. 6. Iye natsitsa kunsi
24 mafumu ku mipando yawo.
Iye nakweza konko
1. OONADI mtima,
omwe afatsa nasauka.
’Dzani mokondwera,
7. Ife amakhutitsa
Tiyeni, tiyeni ku Betlehemu;
anjala ndi zabwino zake,
Modyera ng’ombe
Ndi olemera onse
Muli Mfumu yathu.
naŵaingits’ opanda kanthu.
Tiyeni timgwadire
8. Monga anapangana
Khristuyo.
ponena kwa makolo athu,
2. Mulungu wamkulu
Wakuyerayera 9
Kubadwa mwamkazi sanakana ’yi; Ali kuthandizadi
Mwana wa ’Tate, lero anake a Yakobo,
Sanalengedwadi. 9. Poti akumbukira
3. Angelo kwezani atate wathu Abrahamu;
Nyimbo zanu zonse, Inde chifundo chokha
M’wambamo mumveke zoyamikazo; akuchitira ana ake.
Lemekezani 26
Mulungu Wakumwamba. 1. AMITHENGA a Mulungu
4. M’dzikomo Ambuye Anaimba nyimbo yomwe,
Mnabadwira ife, Posonkhana m’mlengalenga,
Ulemu wosatha muyeneradi. Natitu usiku womwe;
Mawu a ’Tate, “Onse azilemekeza
Munaloŵa m’thupi. Mlungu Wakumwambamwamba;
25 Akhalebe ndi mtendere
1. NDIKULEMEKEZA Anthu ali ponseponse.”
Ambuye Mpulumutsi wanga; Amithenga anaimba
Moyo ndi mtima wanga Ndi usiku m’mlengalenga.
ndilikukondwa mwa Mulungu. 2. Anamva abusa omwe
2. Ndiye anayang’ana Anaŵeta nkhosa zawo.
umphaŵi wa mdzakazi wake; Mthenga nati: “Musaope;
Onse adzandiyesa Mumve ndikufotokoza:
ine wodala nsiku zonse. Wabadwa usiku uno
3. Ndiye wamphamvu zonse Yesu Kristu Ambuyathu

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Ndiye Mpulumutsi wathu; Ndiye kumwamba komwe


Anabadwa m’Betlehemu.” Ationetsa mbanda kucha,
Amithenga anaimba 9. Poŵalitsira omwe
Ndi usiku m’mlengalenga. ali mumdima ndi muimfa,
3. Yesu ndinu Mbuye wathu, Ndi potilunjikitsa
Munasiya za Kumwamba; tonse munjira yamtendere.
Munakhala mwana kuno; 28
Mnatifera mwaufulu.
1. AMBUYE tsopano lino,
Inu nonse amithenga,
monga mwa mawu anu aja,
Inu mumtamande Iye;
Lolani kapolo wanu
Anthu onse ali pansi
ndikachokere mumtendere;
Adza akondane naye.
2. Chifukwa chipulumutso
Zoonazi amithenga
chanu mwandionetsa zedi,
Anaimba m’mlengalenga.
Chimene munachikonza
27 akachione anthu onse;
1. AMBUYE ngwodalitsika, 3. Ndi nyali yakuŵalitsa
Mulungu wa Israyeli ndiye, 10
Poti anayang’ana omwe sadziŵa mawu anu;
naŵawombola anthu ake, Ndiwo ulemerero
2. Napulumutsa tonse wa Israyeli mpingo wanu.
mwapfuko la Davide mwana wake;
Monga analankhula 29
mwa aneneri ake, kuti 1. M’KATI mwa zobvuta zathu
3. Adzatipulumutsa Yesu aitana ife,
kudzanja la onse akutida, Tsiku lonse amanena:
Ndipo adzachitira “Tsata Ine mkristu iwe.”
akulu chifundo ndi chisoni. 2. Kale ophunzira ake
4. Ndiye akumbukira Namvanso kunyanja kwawo,
pangani loyera lake lija, Zinthu zonse anasiya
Ndi chilumbiro chake Kukatsata Mbuye wawo.
cha kwa atate Abrahamu, 3. Yesu aitana ife;
5. Choti timtumikire Tikakonda chuma chokha,
osaŵaopa ’dani athu, Ati Yesu; “Mwana wanga,
Ndi kuyeranso mtima Undikondetu koposa.”
mwa chilungamo nsiku zonse. 4. Mwachimwemwe, mwachisoni,
6. Mwana, adzakuyesa Pogwiritsa ntchito zonse,
mneneritu wa Wamkulukulu, Aitana Mpulumutsi
Ndiwe udzakonzera Kuti tizimkonda tonse.
njira ya Mbuye Wakumwamba. 5. Yesu aitana ife;
7. Udzadziŵitsa anthu Mbuye, mutimvetse ndithu,
za Mpulumutsi wawo yemwe Tipereke mtima wathu,
Aŵakhululukira Tikondane lero ndithu.
Nafafaniza tchimo lawo, 30
8. Poti Mulungu wathu 1. IFE timakufunani
ali ndi mtima wachifundo. Inu wotonthoza mtima.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Yesu, nyimbo zathu zonse 4. “Senzani mtanda wanuwu.”


Ziyamika Inu nokha. Nawo muyende chetetu,
Munasiya zonse m’Mwamba,
Mutsogoledwe nawonso
Kudzakhala pansi pano
Kuwombola akapolo, Kwanu Kumwamba komweko.
Kumasula anthu anu. 5. “Senzani mtanda wanuwu.”
2. Yesu, ndi chifundo chanu Tsatani Yesu m’njiramu;
Chachikulu munadzera Iye wakusalemayo
Ife anthu osauka, Ndiye alandiridwadi.
Tsoka lathu mnachotsera.
Mwazi ndi misozi yanu
Munakhetsa m’munda muja, 32
Kukonzera ife njira 1. MUNTHU wacisoniyo
Yonkako Kumwamba kuja. …...... dzina lakelo,
3. Yesu munalaswa m’mtima,
Mpulumutsi linanso;
Ndi zonyoza munafoka,
Mnasenzera anthu mkwiyo Alleluia, ndiye Yesu.
Wa Atate, Inu nokha. 2. Anapeputaidwako,
Chikho chija ndi choopsa Nandifera m’mtandamo,
Munamwacho m’phiri lija Anandowombolayo;
M’mene munalola mtanda, Aleluya ndiye yesu
E! chifundo chanu chinja.
3. Ife tinacimwadi,
4. Yesu ndinu moyo wathu,
Chuma chathu choposetsa. Iye sanachimwa ayi,
E! tikondwerera mtanda, Anachotsa chimoli,
Apo moyo munapatsa. Aleluya, ndiye Yesu.
Mbuye tikondana nanu, 4. Anapachikidwathu
Yesu Mbuye Mwini zonse; Watha nchito yake……
Ndi mitima ndi milomo,
Azakwera m’mwamba……
Tikuyamikani tonse.
Aleluya, ndiye Yesu.
31 5. Azdabwera Iyenso
1. “SENZANI mtanda wanuwu.” Kudzatenga okhawo;
Atero Yesu Mbuyathu; Nyimbo tidzakaimbanso,
“Mukanditsata Inetu, Aleluya ndiye Yesu.
Mudzikanize nokhanu.”
2. “Senzani mtanda wanuwu.”
33
Musaopsedwe nawotu; 1. Unakhetsedwa mwazi dol
Mphamvu za Yesu nzanunso; Wa Yesu Mfumuyo,
Limba mtima wanuwo. Poweramira mutuwo
3. “Senzani mtanda wanuwu.” Pamtanda pakepo.
Bwanji manyazi mumva ’nu?
Yesu anapiriratu, Mbuye mthandiza inetu
Kuti mupulumuketu. Kukonda inidi,
Ndi kuli mpando wanuwo
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Ndufuna kuzdako. Poona anthu amanyoza?


2. Zochimwa zanga zonsezo Onani umo apirira;
Wapachikidwa Ambuyathu.
Anaziferadi,
3. Anena mawu m’mtanda momwe
Chikondi chake chonsecho Mawu ochepa achifundo,
Sindingadziwe ayi. Apempherera ’dani ake;
3. Linadetsadi dzuwa bii, Wapachikidwa Ambuyathu.
Pakufa iyeyo 4. Mtima wangawe, uyenera
Pakumwalira indedi Kuduka ndi manyazi lero,
Zamlasa ndi zoipa zako;
Wakundilengayo.
Wapachikidwa Ambuyathu.
4. Pokumbukira mtandawo 5. Ona chikondi cha Mulungu,
Wa mpulumutsiyu, Ona zoipazo za anthu,
Ndiphimba nkhope yangayi, Koma chakula ndi chikondi;
Ndi nsoni n’chitatu. Wapachikidwa Ambuyathu.
5. Zofuna zanga zosenzo 36
Za mutima wangawu 1. PAMTANDAPO Ambuyeyo
Ndipereka kwa inu, Anatifera ifetu,
Mundiweruzetu. Nakhetsa mwazi wakewo
Kutiwombola tonsefe.
Pamtandapo, pamtandapo
34 Ambuye wanga ’nafatu;
1. KU Mzinda wakuyerawo Pamtandapo, pamtandapo
Wapachikidwa Mbuyeyo, Anandiwombolerapo.
Nasautsidwa Mbuyeyo, 2. Kwa munthu wosokerayo
11 Kudziko lakutaliko,
Akatipulumutsa ’fe. Atero Yesu: “Bweratu
2. Padzanja lachifundolo Ukhale nawo moyowo.”
Linapenyetsetsa ’khunguwo, 3. E! Yesu Mbuye wangadi,
Lachiza nalo nthendazo, Ndipatsa Inu mtimawu;
Papyolatu msomaliwo. Ndithandizeni inedi
3. Mapazi ake namvatu Ndisalekane nanu ’yi.
Zoŵaŵa zopambanazo, 4. Zochimwa zanga zonsezo
Napachikidwa kaamba ka Wandichotsera mwaziwo;
Zoipa zathu zonsezi. Mumtima mwanga muli mbee!
4. Ambuye, tikondweratu Mwayeretsedwa indetu.
Kupulumutsa kwanuko; 37
Satana tisammvere ’yi 1. ZATHEDWA zonsetu
Komabe Mpulumutsiyo. Za moyo wakewo,
35 Ambuye anatsikayo
1. TIYENI, dzalireni nane, Nafika pansipa.
Tidze ku mtanda wa Ambuye, 2. Zintchito zakezi
Tionse tichitetu maliro; Zofuna ’Tatewo
Wapachikidwa Ambuyathu. Anatsiriza zonsedi,
2. Kodi misozi itisoŵa, Sanazisiya ’yi.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

3. Pa Iye padzapo E, mudzandimasula;


Chisoni m’mtimamo, Ndipenyetsetsa Yesu,
Mpweteko wonse wathuwo Ambuye Mfumu yanga,
Wa dziko lonseli. Ndikafa ndine wanu,
4. Pamutu minga kwe! Ndikhale nanu m’Mwamba.
Pamoyo wakewo 39
Zoipa zathu zonsezo,
1. POKUMBUKIRA mtandawo
Zinaikidwapo.
Ambuye ’nandiferapo,
5. Anandiferatu ’Ye,
Ndiyesa zingochepazo
Afera inedi;
Ndinazitama kalelo.
Athetsa nsembe zonsezi
2. Mndiletse ndisatame’yi
Ambuye Nsembeyi.
Zachabe, koma imfayi;
6. Pakugomedwapo
Zijazo ndinakondazo
Pa mlandu wangawo,
Ndazilekera mwaziwo.
Ndidzaitana Mbuyeyo
3. Onani m’mutu, m’manjawo
Andilanditsepo.
Mudzera nsoni m’mwazimo.
12 A! panalibe kalelo
38 Wondibvalira mingayo.
1. A! MUTU wakuyera, 4. Chinkana dziko lonselo
Wolaswa wachisoni, Lichepa ndithu mtulowo,
Abveka Inu anthu Chikondicho chagwirabe
Ndi minga ya udani; Mtimanga, moyo, ndense ’ne.
Ambuye mwafokatu 40
Ndi masauko aja, 1. LERO Kristu anauka, Aleluya.
Mwatuŵa m’maso mwanu Ndilo tsiku lokondwera. Aleluya.
Mumayerera kale. Iye kale anafera, Aleluya.
2. Ambuye Mwini moyo, Nawombola otaika Aleluya.
Kokoma mnafumako; 2. Timwimbire zomtamanda Aleluya.
Ndizizwa pomva mawu Ndiye Kristu wa Kumwamba
Umo mwachitiramo. Aleluya.
Chisoni chija chanu Natsikira kumanda, Aleluya.
Ncha pamachimo anga, Nalanditsa akuipa. Aleluya
Mwasaukira Inu 3. Koma masauko ake Aleluya.
Kupalamula kwanga. Anatiwombola ife. Aleluya.
3. Nditani! Bwezi langa Ndiye Mfumu ya mafumu Aleluya.
Kulemekeza Inu Mwana ndithu wa Mulungu.
Chifukwa cha chifundo Aleluya.
Ndi imfa ija yanu? 4. Timwimbire Mulungu wathu,
Mundikhalitse wanu, Aleluya.
Wokhulupira inu; Kuti atikonda ndithu: Aleluya.
Musandilole konse Mtamenso angelo inu, Aleluya.
Kufulatira Inu. Ndiye ‘Tate, Mwana, Mzimu
4. Pakufa ine Mbuye Aleluya.
Mukhaletu pafupi,
Mundithandize ine, 41
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

1. NLA Mlungu dzuŵali: 43


Pa mbanda kuchapo
1. KONDWERANI dzuŵa lino,
Angelo ‘nadzatu
Aleluya.
Nachotsa mwalawo.
Yesu wanka m’Mwamba momwe:
Ndi mtima wonse mwimbedi,
Aleluya.
Wauka Mbuye leroli.
Wachokera m’dziko lino, Aleluya.
2. Akonda onsewo
Wabwerera kwawo komwe. Aleluya.
‘Nagwidwa manthadi
2. Zomkwezetsa zili m’Mwamba,
Poona zo’psyazo
Aleluya.
Zoonekerazi.
Zodikira Mbuye wathu; Aleluya.
3. Mulibe m’mandamu,
Mloŵetseni n’kumlambira, Aleluya.
Wadzuka Mbuyetu;
Mfumu yathu yaulemu. Aleluya.
Woposa imfayo
3. Yesu nkana saoneka, Aleluya
13 Atipempherera komwe: Aleluya.
Ndi Mwini moyowu. M’nyumba yake yokonzeka Aleluya.
4. Dzukani nayetu, Atilinda ife tomwe Aleluya.
Oyera inunso, 4. Tiyamike Dzina lake, Aleluya.
Lekani m’mandamo Mfumu ya ulemu wonse. Aleluya.
Zakufa zanuzo. Tibukitse mbiri yake Aleluya.
5. Titama Yesuyo, Pansipa padziko lonse. Aleluya.
Ambuye m’Mwambamo,
Wofera anthu ’Ye, 44
Timkondakondako. 1. LAMBIRA, Mfumuyo,
Ndi Yesu Mbuyathu,
42 Tamvani nyimbo za ‘mithenga a
ALELUYA, Aleluya, Aleluya! Kumwambako;
1. Nkhondoyo yatha, imfa yagonja, Nafenso pansipa
Yesu wamoyo anaiposa, Timyamikire ’Yo,
Msampha woipa wonse nawonja, Ndi Mpulumutsi wathu wotifera
Aleluya! kalelo.
2. Mphamvu za imfa ndi za Satana 2. Lambira Yesuyo
Naye Ambuye zinalimbana, Wokonda tonsefe;
Komatu Yesu anapambana. Mabala ake achikondi aonekabe;
Aleluya! Tisaiwale ’yi
3. Atha masiku aja ansoni, Zoŵaŵa zakezo,
Mbuye wauka, ali ndi mboni; Tileke kumchimwira, kumsautsa
Lero chimwemwe, chatha chisoni, Yesuyo.
Aleluya! 3. Lambira Yesuyo,
4. Nsinga za imfa Iye ’nadula, Uthenga wakewu
Khomo la m’Mwamba, nalitsegula; Uyanjanitsa anthu onse m’dziko
Yesu timtama tonse tipfuula, munomo:
Aleluya! Amaiŵala za
5. Mbuye mabala anu olimba Kudana kwawoko,
Atichotsera mantha a imfa; Nayamikira Mfumu yamtendere
Tsono ndi mtima wonse tiiimba: monsemo.
Aleluya! 4. Lambira Mfumuyo

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Wolenga zonsezi: Adzakudalitsa iwe,


Nyenyezi, dziko, dzuŵa, mwezi ndi Nadzaletsa tsoka lonse,
mitamboyi; Nadzakutsogoza kwawo,
Tikweze dzinalo Akondadi!
La Mbuye Yesuyo,
Timyamikire pansi pano ndi
Kumwambako. 46
45 1. Msandipitirire, Yesu,
1. YESU wakukoma mtima, Mundimvere ine;
Akondadi! Mukudalitsa ena,
14 Msandipitirire.
Wakuposa mbale ndiye,
Akondadi! Yesu mbuye,
Wina asautsa iwe, Khutu munditchere
Pena adzasiya iwe, M’mene muitana ena
Yesu sadzanyenga iwe, Msandipitirire.
Akondadi! 2. Ndigwadira inu, Yesu,
2. Kumdziŵitsa ndiko moyo, Musandikanize;
Akondadi! Ndizalapatu machismo
Akhumbira mtima wako, Mbuye mndithandize
Akondadi 3. Nkhope yanu ndifunitsa
Mwazi wake ngwowombola, Sind’yenera konse;
M’chipululu akufuna, M’mtima mwanga muchiritse
M’khola mwake akusunga, Nthenda zanga zones.
Akondadi! 4. Yesu ndinutu chitsime cha
3. Akufuna kumdziŵitsa, chimwemwe chokha,
Akondadi! Sindifuna wina konse,
Udzimpatsa moyo wako, Koma inu nokha.
Akondadi!
Kodi umachita mantha? 47
Pena umadera nkhaŵa?
1. Idza wolema,
Yesu amasangalatsa,
Akupumitsa;
Akondadi!
Womva chisoni,
4. Bwenzi ndiye wakufera,
Akutonthoza;
Akondadi!
Mulendo limbika,
Nthaŵi zonse sakusiya,
Mphamvu apatsa
Akondadi!
Amtisunga, yesu ambuye.
Anthu ena akunyenga,
2. Ndiye mtsamiro
Yesu sadzanyenga iwe,
Pogona ine;
Zakubvuta adzachotsa,
Pofika kufa
Akondadi!
Andidzutsanso;
5. Akhululukira iwe,
Podzichepetsa;
Akondadi!
Andikwedzanso;
Nadzainga mdani wako,
Moyo wa moyo,
Akondadi!
Yesu abuye.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

3. Ndikakhumudwa Chikhala chosatha;


Andilimbitsa; Ndi mwaziwo
Ndikadzitama; Akhalatu Wansembe wanga Yesuyo.
Andichepetsa; 3. Mabala ajawo
Ndikasokera; A m’thupi mwakemo
Andilondola; Amukumbutsanso
E! wokondedwa Za ine pansipa;
Yesu Ambuye. Zoipazo
Achotsadi kotero sindingafe ’yi
4. Ndimachitira 4. Mulungu ali wokhulula
Inu umboni mtimatu,
Ndikukuzani Ndilibe mantha ’yi,
Moyamikira; Andisungiradi;
Mphamvu ndi nzeru Ndibwera kwa
Moyo, zonsezi, Atatewo, titayanjana leroli.
Si zanga, nzanu, 50
Yesu ambuye.
1. M’KHOLA mwa ng’ombe ku
Betlehemu
48 Anabadwamo Ambuyangayo;
1. MBUYE , mutsaganetu Etu, ndizizwa! natsikirako,
Nane ndingachimwenso; Kufuna inetu.
Nanu ndisungidwedi, Kufuna inetu, kufuna inetu,
Mwa chikondi chanucho. 15
Mbuye Yesu, Etu ndizizwa! Natsikirako
Mundiperekeze inetu; Kufuna inetu.
Ndine mlendo, Mbuye ‘Nu, 2. Popachikidwa pa Golgotapo
Mutsagane nanetu Yesu anandiwombola ine,
2. Inu mundibisadi Etu, ndidziŵa! Nakondetsadi
M’mene ndabvutidwamo, Nafera inetu.
Ngati muli ndinedi Nafera inetu, nafera inetu,
Bwino ndidzakhalamo. Etu ndizizwa! Nakondetsadi
3. Mbuye, mutsaganebe Nafera inetu.
Mpaka moyo watha zi! 3. Mbusa wokoma ndi Mbuyangayo,
Kwanu mundifitseko, Nandiitana posokerapo,
Kwanu nsoni zathadi. Konse koipa nalondolako
49 Kubweza inetu.
1. E, MOYO wanga’we Kubweza inetu, kubweza inetu,
Utsitsimuketu; Konse koipa nalondolako
Ambuye Yesuyo Kubweza inetu.
Akhala m’Mwambamo. 4. Uko kumwambako Mbuyangayo
Pampandopo Andikonzera mokhaliramo;
Akhalabe, natchula dzina langali. Tsiku linalo adzabweranso
2. Kwa Mlungu m’Mwambamo Kutenga inetu.
Amapempherako; Kutenga inetu, kutenga inetu,
Chikondi chakenso Tsiku linalo adzabweranso

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Kutenga inetu. 1. MBUYE Yesu adzabwera,


Asekere anthu onse;
51 Mawu awa achimwemwe
Azimveka m’dziko lonse.
1. Alinkuza wansoni munthu
Adzabwera, adzabwera;
Wakukhala kumwamba,
E! bwerani Mbuye wathu.
Alinkudza m’ulemelero
2. Dziko lino linaona
Ndi mwamuna wa mtanda.
Masauko a Mbuyathu,
Lidzaonanso ulemu,
Aleluya, aluluya
M’mene adzabwera Iye.
Alinkudza kwa ife;
Adzabwera, adzabwera;
Ndi chimwemwe ……………..
Timvomera, E! mubwere
Pakufika Ambuye.
3. Anthu anu amafoka,
2. Alinkudza Ambuye Yesu
Pa ulendo nasokera;
Wakuphedwa pa dziko,
Ha! Adzaonana nanu
Alinkudza kukhala mfumu
Atabvalanso zoyera.
Yoweruza maiko.
Mudzabwera, mudzabwera;
3. Pakufika asonkhanitsa
Inde Mbuyetu mubwere.
Anthu ake oyera;
4. Ndi chiyembekezo ichi
Adzafuna m’mitundu yonse
Sitikhala chete ife:
Omwe iye anafera.
Tiimbitsa nyimbo zathu
52 Zakulemekeza Mlungu.
1. PAKWITANA Mbuye wanga Adzabwera, adzabwera
Potsiriza dzikoli, E!! mubwere msanga YESU.
Pakufika tsiku la kuŵalalo, 54
Posonkhana akumvera,
1. YANG’ANANI, anthu onse,
Pakuona Yesuyo,
Yesu Mbuye wathuyo:
Ndidzakondwerera naye komweko.
Alinkudza ndi ulemu,
Pakwitana Mbuye wanga,
Kuoneka m’Mwambamo.
Pakwitana Mbuye wanga,
Anthu onse amlambire
Pakwitana Mbuye wanga,
Yesu Mwana wa Mulungu
Ndidzakondwerera naye komweko.
Alinkudza ndi ulemu
2. Potuluka m’manda mwawo
Wopambana, indetu.
Anthu ake onsewo,
2. Adzatenga anthu ake
Tidzasanganatu nawo nthaŵiyo.
Akumvera pansipo
Pakuuka osankhidwa,
Iwo adzakhala naye
Kunka naye Yesuyo,
Ndidzakondwerera naye komweko. 16
3. Tisaleke kugwirabe M’dziko la Kumwambako.
Ntchito ya Mulunguyo, 3. Koma anthu onse omwe
Tibukitse mbiri yake m’dzikoli, Anamnyoza pansipo,
Ndi podzatha moyo wathu Nthaŵi Yesu alinkudza
Ndi zintchito zathuzo, Adzaopa m’mtimamo.
Tidzakondwerera naye komweko. 4. Ife tonse tikumbuke
Mawu ake onsewo;
53 Timuyang’anire Iye,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Yesu Mbuye wathuyo. Nakweradi Kumwambako,


55 Nakhala Mfumu monsemo,
1. A MULUNGU, Ambuye wathu Mlunguyo.
Munatuma Yesuyo, 4. Adzadza indetu
Mwana wanu Yekhayo. Kudziko linoli;
2. Anabadwa, Tidzanka nayeyu
Anabadwa motere, M’ufumu wakedi.
Monga mmphaŵi m’kholamo. Momwemo tidzampenya ’Ye,
3. Anakonda Momwemo tidzakhala ‘fe
Anakonda anthuwo, M’kuŵala kwake koti mbee!
Naŵapulumutsanso. 57
4. Anafera, 1. Yesu, dzina lakukonda,
Anafera m’mtandamo, Lopambana onse ena,
Anafera ifenso. Tonse tidzaligwadira
5. Anadzuka Ndi mitima yochepetsa.
Anadzuka m’mandamo, 2. Yesu, dzina lokondwetsa
Anatenga moyowo. Akuipa a padziko,
6. Anakwera, Kale linatidziŵitsa
Anakwera m’Mwambamo Mpulumutsi ndiye Yesu.
Kwa Mulungu ’Tatewo. 3. Yesu dzina lakufatsa,
7. Adzabwera, Anamutcha ’kali Mwana,
Adzabwera Iyeyo M’mene analoŵa kale
Tsiku lomalizalo. M’dziko lino lakudana.
8. Aleluya, 4. Yesu, dzina ndi lomweli
Aleluya Yesuyo, La pa dziko lino lonse,
Tizitama dzinalo. Ndi lamphamvu yolanditsa
56 Anthu mu masoka onse.
1. IDZANI nonse ’nu 5. Yesu, dzina lakukonda
Okonda Yesuyo; 17
Libuke Dzinali, La Mwanayo wa Mulungu,
Timtame konseko. Ife anthu osauka
Uzani onse m’Mwambamo, Tithaŵira nalo kwanu.
Uzani onse pansipa, 58
Wafera Iye anthuwo. 1. Inde ndifuna kumvatu
2. Waleka kronayo, Za chikondano chakecho
Nasiya ’Tatewo, Cha Yesu mbuye wangayo
Natsika m’Mwambamo, Zomwe anmva kalelo.
Nalira, nafatu.
Zoŵaŵa zake zonsezo E! zina za Yesu
Nazimva, zinaposatu E! zina za Yesu
Kuti tipulumukedi. Inde, ndirira m’mtima
3. Nadzuka m’mandamo Chipulumutso chakecho
Moopsya m’mdimamo,
Nigonja imfayo 2. Zina za Yesu Ndimvetu,
Ndi mdani waketu; Kuti ndichite zakezo;

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Mzimu woyera, mudzetu 2. Ndinasokera kalelo,


Ndiphunzitseni zonsezo. Ndamkana Iye Yesuyo,
3. M’mawu a Yesu mbuyeyo, Koma ndiimba leroli:
Inde, acheza nanemo; Wandiwombola inedi.
Liu ndimamva m’bukumo 3. M’mtima ndimakondweramo
Ndilo la Yesu Mbuyeyo. Popenyetsetsa Yesuyo
4. Zina za Yesu m’mwambamo Pamtanda pake pomwepo,
Ali pampando pakepo; Pakundifera inenso.
Udze ufumu wakewo, 4. Sizitha ntchito zangazo
………………………… Kundiyeretsa m’mtimamo;
59 Anandiyesa inetu
Wakulungama Yesuyo.
1. Wina atikonda ife,
5. Tsono mubwere inunso;
Bwenzi lathu ndiyeyu,
Mtetezi wanu ndiyedi.
Atifunafuna ife,
Apulumusa onsewo
Inde nthawi zonsetu.
Akumkhulupiriradi.
Chikondano chakechi
Nchachikulukuludi 61
1. Konda dzinalo la Yesu,
2. Ndani mwa abale athu Mwana wosauka iwe;
Angatifere ife? Ndilo lothandiza anthu;
Koma yesu m’malo mwathu Khala nalo ponse phee.
Anapachikidwatu
3. Anamnyoza pansi pano, Dzina la Yesuyo
Bwenzi la ochimwawo; Nlokondetsa onsewo,
Mu’ulemerero wake M’mwambamo, ponsepo
Alizonda Dzinali. Litonthoza m’mtimamo.
4. Timchimwira kopambana,
Ndi kumsautsa iye, 2. Konda dzinalo la Yesu
Koma Bwenzi lathu Yesu M’moyo mwakomo
Atikondakondabe. M’mene ulikuyesedwa,
5. Mtiphunzitse, mbuye Yesu, Tchula Dzina lakelo.
Tikondane nanutu; 3. Dzina ili ndi lokoma
Tisaiwalire konse La mtetezi wathuwo;
Bwenzi lathu ndinutu. M’mene adzatilandira
M’mwamba, tidzakondwa.
60 4. Mbuye Yesu timtamanda
Ndi nyimbo zathuzo;
1. NDITAME Mlungu m’mtimamo,
Mfumu ya ma mfumu onse
Wakundifera pansipo,
Yesu timavesadi.
Nafafaniza tchimolo,
Nanditengera dipolo
Wandiwombola inetu 62
Pokhetsa nwazi wakewo; 1. KHAMULO liliko
Timlemekeza Iyetu Kumwambako mbuu!
Wotilipira dipolo. Pakukhala ndi Yesu

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Aimbirako: Mbveke Mbuyeyo!


“Kwa Iye atikonda 64
Natsuka ’fe mbuu!
1. MUBWERE Mzimu Wakuyera,
E! kukhale ulemu
Kuyatsa moto m’mtima mwathu;
Kwa Mbuyathuyu.”
Ntchito ndi yanu kudzozera
2. Onsewa ’nachimwa
Nadetsedwa bii, 18
Nthaŵi yino ayera Ndi kutininkha mphatsozo.
Naimbiradi: 2. Kudzodza kwanu kutipatsa
3. Akhala mafumu Chimwemwe, moyo ndi mtendere;
Kwa Mbuyathuyo, Kuŵala kwanu kupenyetsa
Anawombola onse A m’mdima ndi a m’ndendemo.
Ndi mwaziwo pyu! 3. Mtima wodetsa mukonzere,
4. Akadakhalabe Chisomo chanu chakwanira;
Osaukako Adani athu muthaŵitse
Ngati Yesu sakana- 4. Mutidziŵitse ‘Tate wathu,
Wombolatuwo. Ndi mwana wake ndinu Mmodzi.
5. Ndi nyimbo yabwino Mnafuma kwa aŵiri onse,
Tidzamtamako, Koma Mulungu Mmodziyo.
Kuti ena pakumva 65
Amwimbirenso: 1. MZIMU Woyera, mudze mumitima
“Kwa Iye atikonda mwathumo,
Natsuka ’fe mbuu! Mufike nazo mphamvu zanu zazikuluzo.
E! kukhale ulemu 2. Mufike monga nyali younika
Kwa Mbuyathuyu.” m’mtimamo.
63 Mutidziŵitse zakuipa zakukhalamo.
1. TAMANI mphamvu ya Yesu, 3. Mufike monga moto wakuotcha
Angelo agwade; zomwezo.
Tulutsanitu korona, Mutiyeretse ifetu m’mitima mwathumo.
Mumbveke, mbveke, mbveke, 4. Mufike monga ngati njiŵa
Mbveke Mbuyeyo! yamtenderewo.
2. Inu osankhidwa ake, Kutitu anthu anu onse akondanetu.
Owomboledwa ’nu, 5. Mufike monga ngati mphepo
Tamani Mpulumutsiyo, yokokomayo,
Mumbveke, Mbveke, Mbveke, Tikhale tonse nazo mphamvu zanu
Mbveke Mbuyeyo! zonsezo.
3. Anthu onse ndi mitundu 66
Pa dziko linotu, 1. MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
Amlemekeze Mfumuyo. E, ngati mvula m’dziko lakuuma,
Mumbveke, mbveke, mbveke, Ndikhale munda wanu wakupatsa
Mbveke Mbuyeyo! Zipatso zoyenera Mbuyeyo.
4. Tifuna kuti komweko 2. Mphunzitsi, ndinu mudziŵitse ine
Tikamgwadire ’Ye; Chikondi chanu chija chachikulu;
Tidzaimba kosaleka: Lembani mawu anu pamtimanga,
Mumbveke, mbveke, mbveke, Kuti ndikhumbukire zanuzo.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

3. Wosangalatsa, ine ndikalira A Mbuyathu Yesu.


Muchotse nsoni, m’mtimamo mudikhe; 19
Mundigoneke pachifuwa chake 3. Mtitsitsimutse ife
Cha Yesu kuti ndikakondwepo. Kuchotsa nkhaŵa zathu,
4. Wotsogolera, munditsogolere Muyatse moto wachikondi
Kuti n’kafike kwawo kwa Atate, Mu mitima yathu.
Nditsate Yesu ndikuyendayenda 4. Mtitsutse titachimwa
M’njira yomweyo anapondamo. kutilapitsa m’mtima,
5. Mthandizi ndinu, mndithangate ine Mwonetsenso chikondi chokhululukira
Kupempha bwino izo zindisoŵa. tchimo.
Kupempha monga Mlungu amafuna 5. Kutiyeretsa m’mtima
Kulingalira zake zokhazo. Ndi ntchito yanu yokha,
6. Mzimu Woyera, n’dzipereke ndense, Kupatsa moyo watsopano
Mundichitire ntchito yaikulu; M’mene timafoka.
Mtima woyera ndi womvera mpatse, 6. Mukhale m’kati mwathu,
Wodzala ndi chikondi chanucho. Mutichotsere mantha,
67 Tidzayamika ’Tate wathu,
1. MPUME pa inetu, Mpweya wa Mwana wawo ndi ’Nu.
Mulungu, 69
Ndi kundidzaza moyo wanuwo, 1. IDZANI, Mzimu Inu,
Kuti ndikonde zomwe mukondanso, Mundidalitse kuno;
Ndichite chomwe mumachitanso. Ndafoka mtima ine
2. Mpume pa inetu, Mpweya wa Polendo wanga uno;
Mulungu, Kwambiri ndakhumudwa
Mpaka mtimanga ukayeretu, Panjirayo ya moyo;
Ndipo zokhumba zanga zilingane Mkaleka kutsogola
Nazo zanuzo zakuyera mbuu! Ndiwonongeka pompo.
3. Mpume pa inetu, Mpweya wa 2. Wakunga mwana ine,
Mulungu, Sindidziŵitsa konse;
Mpaka ndikhale wanu nokhatu; Mundilangize Mzimu
Ayeretsedwe makhalidwe anga Panjira yanga yonse;
Ndi mphamvu yanu yondisunga nji! Mundiyendetse bwino
4. Mpume pa inetu, Mpweya wa Ndifike ine ndemwe
Mulungu, Panjira yolungama,
Kuti inedi ndisafe ’yitu, Kudziko lachimwemwe.
Koma ndikhale nanu m’moyo womwe 3. Mundilimbitse m’mtima
Wangwiro ndi wa nthaŵi zonsetu. Pogwira ntchito izi;
68 Ndikapumula pena
1. MUBWERE Mzimu Inu Mukhale ndithu ndine;
Woyera wakufatsa, Zolingirira zanga
Muchotse mdima m’mtima mwathu Ziyere zonse m’mtima
Tikapenye m’maso. Zoipa muzichotse,
2. Mtisangalatse m’zonse, Sindidzazichitanso.
Ndi wachifundo Inu, 70
Tiyembekeze kumapazi 1. MZIMU Woyera, mudzetu,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Tiyeretsedwe m’mtimamu; Atipatsa ife makhalidwe


Mupatse anthu anuwa Ofanana naye Yesu,
Mitulo yanu yonseyo. Anatsika kumwambako.
2. Kudzoza kwa Kumwambako
Kutitonthoza m’mtimamo, 2. Naye mzimu mndiphunzitsekuko
Ndi kutidzutsa m’moyomu, Kukondwera nsiku zones
Tikhale okondanatu. Ndi kukhara ndi mtendere
3. Pankhope pathu mthirepo Osadaratu nkhawa ayi!
Chisomo chanu chijacho; 3. Mndithandize kukondana
Mtendere mutininkhebe, Ndi kuthangatira onse
Mutiyendetse ponse phee! Ndi kukhululukirabe
4. Tionetseni tonsetu Akundichimwirawo.
Umodzi wanu wonsemo, 4. Mndirimbitse ndipirire
Atate, Mwana, Mzimu ’Nu Osadandaura konse,
Tiimbe Nthaŵi zonsezo: Ndi kulamulira thupi
Titamire Nthaŵi zonse Ndi zofuna zakezo.
’Tate, Mwana, Mzimu, Nonse. 5. Kudzirala ndi kufatsa,
Amen. Inde, zonse muzikonda,
71 Mndiphunzitse pondipatsa
1. MUBWERE kuno Mzimu ’Nu Mzimu wanu woyerawo.
Chitsime cha chikondicho; 73
Mudziŵa ndimaliratu, 1. MBUYE, Mawu anu
Mukhale m’mtima mwangamo; Atikondweretsa,
Ndipatsa inu mtimawu, Atitsogolera,
Masiku onse mkhalemu. Salephera konse.
2. Mukonze mtima wangawu, 20
Muyere ndithu m’katimo; 2. Poyesedwa ife
Ndilinda tere, Mzimu ’Nu, Atipambanitsa,
Mupatsetu chikondicho; Natonthoza mtima
Lichepa dontho lokhali, Natipulumutsa.
Ndipempha mundidzazedi. 3. Tikaona bvuto
3. Ndilira Mzimu leroli, Tikaloŵa m’dima,
Mutsimikize Mawuwo; Kuunika kwake
Ya Mbuye Yesu mphamvuyi, Kusonyeza njira.
Ikhale yathu, yanganso; 4. Atisangalatsa,
Muloŵe m’mtima, mdzazetu Atilemeretsa
Ndi mphamvu, nzeru, moyowu. Poŵerenga mommo
Nawo mtima wonse.
72 5. Ndiwo alimbitsa
1. Mbuye wondipulumutsa Omwe akufooka,
Mulandire mtima wanga, Naŵapatsa moyo
Mwandipatsa mzimu wanu Akufuna kufa.
Womeretsa zipatsomo. 6. Mbuye, mtiphunzitse
Nzeru zake zonse,
Ndiye mzimu wakuyera Tikayenderane

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

N’tiyanjane nanu. 2. Mkate wamoyowo


Ndinu Ambuye;
74 Mawu oyera anu n’khumbanso,
Mun’dyetse onsewo
1. Cholimbitsa mtima ndi
Ndikhale moyo,
Chonditsogolera
Ndikonde zakuona zanuzo.
M’njira ya Mulunguyo,
3. Mtume tsopanoli
Ine ndili nacho.
Mzimu Woyera,
Kuti andikonzere m’masomo;
M’Bukuli ine ndi
Abvumbulutse zinsinsi za m’Mawu,
Onse owerenga
Kuti ndionemo Ambuyeyo.
Mawu a Mulunguwo,
4. Mndidalitsire ’ne
Timapeza moyo
Mawu amoyo,
Monga munadalitsa mkatewo;
Ndikhale mfuludi,
2. Dzinthu zakumundazo
Wosamangika,
Zilimbitsa thupi
Mukhale moyo wanga wonsewo.
Zolembedwa m’Bukumo
Zimadyetsa mtima.
3. Ndikachimwa, Bukuli 76
Lindiyambotsutsa 1. MBIRI yakalelomwe
Limanditonthoza ndi Mundisimbiretu
Mau a mtendere. Ya Yesu Mbuye yemwe
4. Pakudera nkhawa ine, Anandiferatu.
Pakuchita mantha, 2. Simbani bwinobwino –
N’kawerenga m’Bukuli Ndilibe nzeru ’yi –
Lindipatsa mphamvu. Ndimve tsopano lino
5. Lindionetsela ‘ne Mbiri ya moyowo.
Chifuniro chake Mbiri yakalelomwe,
Cha mbuynga Yesuyo, Mbiri yakalelomwe,
Ndikamvera bwino. Mbiri yakalelomwe
6. Zonse mwazilembamo, Mundisimbiretu.
Mzimu wakuyera, 3. Mawu amveke bwino,
Kuzimvera zonsezo Aloŵe m’mtimamo,
Mundithangatire. Ndizindikire tsono
7. M’Buku lakuyerali Chipulumutsocho.
Powerenga ife, 4. Simbani mobwereza,
Mbuye mutipatsemo Ndisaiŵale ‘yi
Moyo, moyo, moyo. Koma ndisunge bwino
75 Mumtima Mbiriyi.
5. Simbani Mbiri yonse
1. MUNDINYEMERE ’ne
Ya Mbuye wangayo;
Mkate wamoyo
Zochimwa zanga ndizo
Monga kunyanja kuja kalelo;
Zinapha Yesuyo.
Ndipyola Mawuwo,
6. Simbanitu mwachete
Ndifuna Inu,
Mbiri ya Yesuyi,
Ndikhumba Inu mwini moyowo.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Pakubvutidwa ine 2. Musachitenso nthantha ’yi,


Inditonthozepo. Mufulumire inutu;
7. Simbani Mbiri yomwe, Tsiku labwino nleroli,
Ndikhulupiredi, Mulandirenso moyowu.
Kuti pakuyesedwa 3. Zokondweretsa m’dzikomu
Ndipulumukepo. Nzosakhutitsa m’mtimamu,
8. Inde, pakufa panga Koma za Yesu zonsezo
M’maso mukhale mbee! Zikwaniritsa inudi.
Mbiri ya Mbuye wanga 4. Sakukanani Yesudi,
Mundisimbirebe. E, mukalapa m’mtimamo;
77 Lolani kuti Mzimuyo
Agwire ntchito zakezo.
1. Kodi ulikulemedwa
Ndi zoipazo? 79
Idza kuno, ati Yesu, 1. PAKUPEMPHA ife pano,
21 Pakwitana ’Tatewo,
Pumako. Pakudziŵa tsoka lako,
2. Ndikamzindikira ninji Bweratu kwa Mbuyeyo.
Mbuye wangayo? Idzatu, idzatu
Ali ndi mabala m’manja Kwa Mbuyathu Yesudi
Mwakemo. Idzatu, idzatu,
3. Kodi ali ndi chilemba Iwe bwera leroli.
M’phumi mwakemo? 2. Unachimwachimwa ndithu,
E, chilembacho chaminga Wasokera m’talimo
Chilimo. Unachedweranji kudza
4. Ndikampeza, ndikamtsata Pakulinda Yesuyo?
Ninji pansipa? 3. M’dziko lino pansi pano
Masauko ndi misozi Sungapeze kanthumo
Zilipo. Kokwanitsa mtima wako;
5. Ndikamfunafuna Iye, Bweratu kwa Mbuyeyo.
Ndipezenjiko? 4. Bvumbulutsa zonse zako
Kumaliza kwa chisoni Zobisika m’mtimamo;
Chonsecho. Ayeretse moyo wako
6. Ndikampempha anditenge, Nawo mwazi wakewo.
Akataniko? 80
Ati Yesu, “Idza msanga, 1. MIPINGO iyo idzatu,
Idzatu.” Yoyenda mangu pajapo,
78 Afuma kuti anthuwo?
1. MUSAŴALOLE mawuwo Afika bwanji komweko?
Apite ngati mphepozi, Anena anthu onsewo,
Musaumitse mtimatu, “Yesu Sing’anga apitapo.”
Polira Yesu Mbuyedi. Anena anthu onsewo,
Idzanitu, idzanitu, “Yesu Sing’anga apitapo”
Idzani kwa Ambuyeyo. 2. Azizwa anthu ajawo,
Idzanitu, idzanitu Nafunsa, “Ndani mlendoyo?
Apulumutse inunso. Wanzeru monga Iyeyo

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Kulibe wina konseko.” 4. Anathera pamtanda zintchito


3. Ndi Yesu yemwe kalelo zonsezi
’Nakhala munthu pansipa; Zowombola mizimu yathuyi,
Anthenda onse nthaŵiyo Ndipo yense akadza
Nachira yake mphamvuyo. mokondwakondwadi
22 Moyo apeza kwa Yesuko.
4. Afika Yesu leroli, 82
Chifundo m’mtima mwakemo, 1. AMBUYE wathu Yesu
Timfitse msanga kwathuko Akhala Mfumunso;
Akhale nafe ponsepo. Zoipa zazikulu
5. Timsankhe Yesu Mbuyeyo, Azigonjetsa ’Ye;
Timyese Mfumu yathuyo, Anena mawu ake
Chifukwa tikamkanatu Ochotsa zonsezo,
Tikhala otayikawo. Kalelo nalamula:
Tsopano inu ’dzanitu, Pakhala bata duu!
Asanapitirirepo. 2. M’ulemerero mwake
Tsopano inu ’dzanitu, Anenanenabe:
Asanapitirirepo. Munkhondo apambana
Ndi mawu akewo.
81 Akristu akondwera
1. Ukapenya kwa yesu uliko Poona mphamvuyo
moyobe, Ya Mbuye wathu Yesu
Inde, moyo tsopanopanotu; Wotiwombolayo.
Olakwira upenye kwa Yesu 3. Zobvala zake zonse
mbuyeyo, Nza mwazi woti pyu!
Kuwombola naferatu ‘we. Pamphumi pake pomwe
Korona waketu.
Ona! Ona! Anatu! Unyolo wa Satana
Kuli moyo kwa yense apenya Umasulidwako;
yesuyo Kumwamba amithenga
Wakuferatu pamtandapo. Atama Mbuyeyo.
4. M’kufatsa kwake komwe
2. Anasenza pa bwanji uchimo Anena nafenso,
wonsewo Tonsefe omangidwa
Ngati wanu pa Yesu sulipo? Ndi zakuipazi;
Bwanji mwazi wakhetsa kutsuka Ambuye amanena
ifetu, Zotichenjezazi:
Ngati uwu sutikwanako. Ananu, msiye zonse,
3. Zilepheradi zonse kugula Mupulumuketu.
moyowu, 5. Chikondi cha Mbuyathu
Koma mwazi wa Yesu mbuyeyo. Chiposa zonsetu;
Khulupira mwa phamvu ya Chisomo chake chomwe
mlungu wathuyu. Chikondweretsabe;
Nuyeretsa ‘we m’timakoma Ulemu wake wonse
Umapambanadi;

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Tiyeni, tikondwere Akuti anthu akumvera


Popita m’Mwambamo. Yesu aŵapulumutsa,
Inde, aŵapulumutsa, indetu.
83 85
1. Sing’anga ‘mkulu ndiye Yesu, 1. OKOMA ndiwo mawu
Mwana wa Mulungu; A Yesu Mbuyeyo,
Asangalatsa achisoni, Wopatsa ife anthu
Ali wachifundo. Mtendere wakewo.
Kwa ife akumvera
Dzina la Yesu ndi lokoma, Kulibe mantha ’yi;
Dzina la Yesu lipambana, Timamva liu lake
Dzina lake lakukonda, Lingoti, “Mudze ’nu.”
Yesu, inde Yesu. 23
2. ……………. Sakhululukidwa Inu akutopawo
Yesu amatero; Yesu aitana ’nu;
Tiyende bwino mnjira yake Mudze kwa Ambuyeyo,
………………….. Mudze msangatu.
3. Nditama nsembe ya mulungu, 2. Mukana Iye bwanji,
Ndilandira Yesu; Wokoma Bwezilo?
Ndikonda dzinalo labwino, Mutsate Yesu yekha,
Dzina lanu Yesu. E, mpaka imfayo.
4. Akulu inu mbwere nonse, Mwafoka osokera,
Ana inu nomwe, Mwadetswa nazozi
Ambuye akuitanani; Zoipa mwazichita;
Bvomerani nonse. Mumvere Mbuyedi.
84 3. Ambuye, musendeze
1. UTHENGA wa Mulungu Pafupi nafedi,
Waloŵa m’mtimamu, Timvetse Inu msanga,
Wochotsa zakuipa Poyenda m’dzikoli.
Zakundidetsazo. M’ulendo m’moyo uno
Pakuti anthu akumvera Titsate Inutu;
Yesu aŵapulumutsa, Kumwamba mutifitse,
Ine, aŵapulumutsa, indetu. Tidzamve: “Idzani.”
2. Ndidziŵa kuti Yesu
Anafa kalelo, 86
Nafafaniza zonse 1. Inu nonse obutidwa,
Tinazichimwazo. Mbuye alipanopa;
3. Satana ndi unyolo M’maso mwanu muli msozi;
Anandimanga nji! Dzani kwa Mbuye wathuyo.
Ambuye Yesu yekha
Nandimasuladi.
4. Ambuye muloŵetse Yesu ngwachifundodi
Mtendere m’mtimamo, K! wafera inutu,
Ndimvetse mawu anu K! wafera inutu.
Masiku onsewo.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

2. Yesu ndiye bwenzi lanu, Idza msanga ’we,


Ali wachikondicho; Adikira iwenso;
Kodi inu mumkanabe? Wachedwatu.
Mlape msanga m’mtimamo. 2. Iwe afuna,
3. Pena imfa idza mawa, Inde, kalelo;
Manda ali mfupimo; Leronso adika
Nthawi yino niyabwino, Mbuye wathuyo.
Mlole Yesu m’mtimamo. Uza Iye zonse
4. Ndi angelo akumwamba Za uchimowo;
Anke ndi uthengawo Yesu ati leroli:
Kuti wina adza lero “Wachedwa ’we.”
Kwa mbuyathu yesuyo. 3. Yesu alindira,
87 Inde, iwetu;
Idza ndi kukhala
1. Wochimwa iwe bweratu
Ndi chimwemwenso
Kwa Yesu mbuyeyo;
Ndi mikono yake
Atero iye; pumatu;
Yachikondiyo;
Umvere mawuwo.
Sankha Iwe msangatu;
Wachedwatu.
Khulupira mawu onse
A mbuyeyo;
Ulinawo pakumvera 89
Inde, moyowo. 1. Lero lino mbale wanga,
Ndilo dzuwalakukoma;
2. Ambuye Yesu anatsira Talandira mpulumutsi
Mwazi wake pyu! M’mene ali kuitana.
Ubire m’mwazi omwewo, 2. Lero lino mbale wanga,
Uyereyere mbuu! Usazengereze ayi;
3. Wamoyo ndiye Yesudi, Ngati ulindira Yesu
Nzoona zakezo; Lero udzachita mwayi.
Akhala iye njiratu 3. Lero lino ndi la bwino;
Yofika m’mwambamo. Moyo wako ulinawo;
4. Tiyeni tonse, tinkeko Pena mawa umwalira,
Ulendo wakewo Uzdatani mlandu wako?
Mudziko lake m’mwambamo, 4. Lero lino mbale wanga,
Tikhale nayeko. Lapa mtima, lapa tchimo,
88 Yesu adzakulandira,
Ukapempha lero lino.
1. YESU ndi wokonda;
5. Ndiwe mlendo lero lino,
Ati “Idzatu,
Mvera ndikupepha iwe;
Yense wakufuna,
Yesu mwana wa Mulungu
Bwera msangatu.”
Akufuna ndithu iwe.
Ali wachifundo
6. Inde, lero lino Yesu
Ndi wamphamvunso
Aitana inu nonse.
Nthaŵi zonse Yesuyo
Landirani Mpulumutsi,
Alindatu.
Musazengereze nonse.
Yesu akukonda,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

90 Ungamvetu Kumwambako,
“Akusowanso malo.”
1. PENYETSETSA Yesu,
2. Wina panalibe
Mtima wosauka;
Kumlandira Iye,
Anafera iwe,
Wakumsangalatsa,
Idza, nupumule.
Wamkonda nasowa.
Iye anachotsa
Anthu sanafuna
Nsoni ndi zoipa;
Chuma chosatha,
Penyetsetsa Yesu,
Sanamkondweresa,
Ndi kukhulupira.
Malo unalibe.
2. Penyetsetsa Yesu
Likatentha dzuŵa; 92
Yachuluka ntchito, 1. ATATE,’nu, atate ’nu,
Mphamvu idzakula. Mverani Ambuye.
Akonzera kwawo Khulupirani kuti mukaloŵe
Nyumba zokhalamo; m’Mwambamo,
Penyetsetsa Yesu, Khulupirani kuti mukaloŵe
Mtsatetu tsopano. M’Mwambamo.
3. Penyetsetsa Yesu 2. Amayi ’nu, amayi ’nu
Pogwirana nawo; Tsatani Ambuye.
Nkhondo ikabvuta 3. Abale ’nu, abale ’nu,
Tamva Mbuye wako. Kondani Ambuye.
Achuluka ’dani, 4. Alongo ’nu, alongo ’nu
Iwe ungofoka; Kondani Ambuye.
Penyetsetsa Yesu, 5. Abwezi ’nu, abwenzi ’nu,
Mantha adzachoka. Tamani Ambuye.
4. Ndipo pakuloŵa 6. Oipa inu nonsetu,
M’dziko la Kumwamba, Mverani Ambuye.
Udzapeza komwe 93
Onse adzatama.
1. NDICHITENJI kukapeza
Mwa zoŵala zija
Moyo? thandizeni!
Za Kumwamba kwawo,
Ndili wakutopa; Mzimu,
Udzapenya maso
Muthandize ine.
Yesu Mbuye wako.
Zonse zinathedwadi;
91 Yesu watha zonsezo;
1. MALO anachepa, Sutha ntchito, ungomvera
Nyumba anammana, Mawu ake omwewo.
Agona m’modyera, 2. Iye anatsika m’Mwamba,
Mutu paudzuwo. Anachoka kwawo,
Anthu sanamtama, Anafera anthu, nati:
Nyimbo panalibe, “Ndatha zonse zawo.”
24 3. Mbuye wanga ndilikumva,
M’nyumba ya alendo Ndikondana nanu;
Malo munalibe. Umapuma mzimu wanga,
Apempha malo Ambuye; Kwathu ndiko kwanu.
E, mlandiretu m’mtimamo,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

94 1. YESU ponong’oneza, idzanitu;


Mupempherera ife, idzanitu;
1. KODI mwalandira Yesu?
Njabwino nthaŵi yino, idzanitu,
Iye anakuferani.
Yodziŵa Mpulumutsi, idzanitu.
Afunitsa inu nonse;
2. Tulani zoipazo, idzanitu;
Kodi mumufunanso?
Yesu adzatha zonse idzanitu;
Kodi mufunatu Yesu?
Olema ndi ochimwa, idzanitu;
Bvomerani msangatu:
Sakambukira izo, idzanitu.
“Inde Yesu ndifunadi,
3. Imvani mawu ake, idzanitu;
Ndinu Mbuye wangatu.”
Mudzalandira dalo, idzanitu;
2. Nthaŵi zonse mufunabe
Nacho chisomo chake, idzanitu,
Zinthuzo za pansi pano;
Yesu alinda inu, idzanitu.
Koma munyozabe Yesu
4. Mverani Iye ati: Idzanitu
Wopachikidwa kalelo.
Tiyeni mudzamwone, idzanitu;
3. Yesu akuitanani
E! akuitanani, idzanitu;
Kwanja kwake kwakukulu;
Ife tibvomereza, Tibweratu.
‘Mvani mawu ake lero,
Musachite nthantha ’yi 97
4. Imfa idzafika msanga; 1. IWE tiye, iwe tiye,
Ndipo mdzaikidwa m’manda; Tiye tsopanoli;
Nthaŵi yomwe simudzamva Pano tiye kuti Yesu,
Kutitana kwakeko. Tiye tsopanoli.
95 (Ndaima pano, ndaima pakhomo!
Loŵa, loŵa, loŵa, loŵa!
1. ’MVANI liu lomwe
Ndaima pano, ndaima pakhomo!)
M’khutu mwakomo,
2. Akukonda, akukonda,
Alikuitana
Tiye tsopanoli:
Mpulumutsiyo:
Pano akukonda iwe,
“Undipatsetu
Tiye tsopanoli.
Mtima wakowo;
3. Akupeza, akupeza,
Ndinakuferau
Tiye tsopanoli;
Kalekalelo.”
Pano akupeza iwe,
2. Ati: “Undiuze
Tiye tsopanoli.
25 4. Salephera, salephera,
Nsoni zakozo; Tiye tsopanoli;
Ine ndidzachotsa Pano salephera Iye,
Zonse zomwezo.” Tiye tsopanoli.
3. Kodi ukafuna 5. Mvera Yesu, mvera Yesu,
Kupumulatu? Tiye tsopanoli;
Yesu aitana: Pano mvera Yesu iwe,
“Udze kunoku.” Tiye tsopanoli.
4. Tula mtolo wako 6. Aleluya, aleluya,
Pali mtandapo, Aleluya, Amen;
Akaunyamula Aleluya, Aleluya,
Mpulumutsiyo. Aleluya, Amen.
96 98
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

1. Tadza kukudyaku, Wotifera kalelo.


Kwakonzedwatu; 100
Mkate wamoyodi, idyatu ’we;
1. YESU wathu Mbuyeyo
Bwera wochimwanso,
Alandira onsewo
Yesu adikatu,
Akuipa omwewo,
Akuitanaku; mvetsatu ’we
Osokera m’talimo.
2. Tadza kumtsinjeku
Imba kaŵiri ndi kaŵirinso,
Wa moyo weni,
Yesu Ambuye sakanatu,
Chiza zoŵaŵazo za m’mtimamo;
Mvetsa Uthenga Wabwinowo,
Mtsinje wodzalawo,
Wakukchimwa adzatu.
Wokwaniratuwo
2. Idzatu kwa Yesuyo,
Yesa sakana ’yi; idzatu ’we.
Apumitsa inunso,
3. M’dzina la Yesuyo
Inde m’mtima mwanumo
Pemphatu iwe,
Ndi mtendere wakewo.
Iye adzamvatu, dikirapo.
3. Walandira inetu
Wamphamvu Mlunguyo,
Tsiku lija kalelo,
Ndiye apatsatu,
Wanditsuka ine mbuu
Dalo labwinolo; idzatu ’we
M’mtima mwanga momwemo.
4. Yamba ulendowo
4. Wandifera Yesuyo
Wonka Kumwamba;
Pansi pano kalelo,
Pano mpoipatu padzikoli;
Sindiopa mlanduwo
Komwe tikondwako,
Pakubwera Iyeyo.
Tidzasekeranso;
Tinke Kumwambako; idzatu ’we. 101
99 1. A! MBUSA wathu amvatu
Uko kuchipululuko
26 Zilira nkhosa zakezo,
1. MWAMVA Mawu a Mulungu; Zili kuthengo kunjako.
Mukabvomeranjiko? Bwezatu, bwezatu,
Kodi musandula mtima Bwezatu zonse m’moopsyamo;
Ndi kumvera Yesuyo? Bwezatu, bwezatu
Bvomerani, Bvomerani Bweza zakezo kwa Yesu
Bvomerani msangatu, 2. Ndani afuna kunkako
Musazengereze ayi, Kukazipeza nkhosazo?
Landirani Yesuyo. Ndani adzathandizako
2. Munachita nthantha kale, Kuti zifunde m’kholamo?
Musazengereze ’yi; 3. M’tali mutali m’phirimo
Yesu akulindirani, Mvetsa, zilira nkhosazo;
Sadzakana inu ’yi. A! Mbusa wathu atitu;
3. Musaope pokumbuka “Bweza zothodwa m’kholamo.”
Zakuipa anuzo; 4. Etu, zilira konseko
Khulupilirani Yesu, Zili m’phiri moopsyamo.
Adzachotsa zonsezo Imva, anena Mwiniyo:
4. Perekani mtima wanu “Kweye, upeze nkhosazo.”
Kwa Mulungu wathuyo;
Khulupirirani Yesu,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

102 Laleka ndithu ludzulo,


Tsopano moyo wadza
1. Thanthwe long’ambikatu,
5. Ambuye naitana ’ne;
Ndibisale momwemu!
“La dziko ndine Dzuŵa,
Madzi ndipo mwaziwo
Zotuluka mthitimo 27
Zinditsuke m’mtima mbuu! Yang’ana Ine, kwacha ’we,
Zindilimbikitsetu. Wachoka mdima uja.”
2. Ntchito zanga zonsezo 6. Ndayang’anira Mbuyeyo
Sindikondweretsa ‘Nu; Ndzapeza Dzuŵa langa
Ndikazigwiritsadi, Londiyendetsa bwinoli
Ndikalira nsonizi, Pa njira yonse yanga.
Zonse sizikwanazi, 104
Koma Yesu yekhayo. 1. YESU wondikondadi,
3. M’manja mopanda kanthu, Ndithaŵire mwanumo
Mtanda ndingogwiradi; Pakugunda mvulazi.
Maliseche mbveke ‘ne; Pakubvuta madziwo,
Ndili ndekha, msunge ‘ne; Yesu mundibise ’ne!
Ndithawira m’mtsinjewo, Ikaleka mphepoyo
Munditsuke m’mtimamo. Tsidya lija chete phee!
4. M’moyo uno kunsiku Mundilandire momwemo
Pena ndinawaliratu, 2. Pothaŵira pena ’yi
M’mene ndidzakwerako Ndikhulupirira ’Nu;
Tionane masowo; Musasiye inedi,
Thanthwe long’ambikatu Mundigwirizizetu.
Ndibisale momwemu. Ndinu wothandiza ‘ne
Wolimbitsa mtimawu;
(maiwe! Thanthwe Pansi pamapiko phee!
long’ambikatu ndibisale Mundifungatiretu.
momwemu) 3. Wina sindifuna ’yi,
Zokhutitsa nzanuzo;
103 M’utsetu akugwawo,
1. AMBUYE ’naitan ’ne; Mchizetu odwalawo.
“Dzapumulire kuno, Ndine wakuipa bii,
Tsamira mutu, mwana ’we Ndinu wakuyera mbuu!
M’chifuwa mwanga muno.” Ndimadzala tchimoli
2. Ndabwera kwa Ambuyeyo; Wolungama ndinutu.
Wolema, wachisoni; 4. Zindichulukirazi
Anandipulumutsako, Nsoni zanu m’mtimamu;
Nakondweretsa ine. Zindichiza nthendazo,
3. Ambuye naitana ’ne; Zindiyeretsetsa mbuu!
“Ndipatsa anthu madzi, Pachitsime panupo
Wotopa ndi waludzu ’we Moyo ndimwe ndimwebe;
Dzamwere moyo kuno.” Mubukatu m’mtimamo,
4. Ndabwera kwa Ambuyeyo. Mundilanditsetu ’ne
Ndamwera madzi awa; (Mulungu ali nane!)

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

(Ali nane, ali nane, ali nane, ali nane, 2. Mzimu mndipatseko,
Aa! Wondilimbitsayo
Mulungu ali nane!) Mumtimamu.
105 Munandiferadi;
Ndiyambe leroli
1. NDI inetu sinditha ’yi
Kukonda Inu ndi
Kunenako milanduyi
Mtimangawu.
Kupempha zachisonizi;
3. Poyenda m’mdima bii,
Ndagonjatu Mbuyanga ’Nu.
M’mtimamo nsonizi
(Aa! Mulungu wanga,
Mndigwirepo;
Mundilembe pamphumipo:
Mdima uchoke zi,
Chidzakhala chizindikiro
Msozi ulekedi,
Cha mpumulo ulinkudza ndi Yesu.)
Ndisasokere ’yi
2. Ndi ine sizitheka ’yi
Kwa Inuko.
Kuchoka zakuipazi;
4. Moyo ukatha zi,
Ndisambe m’mwazi wanuwo;
Pofika imfadi,
Ndagonjatu Mbuyanga ’Nu.
Mndisungepo:
3. Ndi ine pondibvutapo
Yesu Mbuyanga ’Nu
Kugwira nazo m’mtimamo,
Mantha mthaŵitsetu
Mundithandize monsemo;
Ndifike m’Mwambamo,
Ndagonjatu Mbuyanga ’Nu.
E, wanuyu.
4. Ndi ine ndasaukadi,
Zabwino m’mtima zonsezi 107
Mwa Inu ndingapezezi; 1. CHITSIMECHO cha mwaziwo
Ndagonjatu Mbuyanga ’Nu. Udzera mwa Mbuyanga;
5. Ndi ine simufuna ’yi Wochimwa ndikasambamo,
Ndingatayike m’mdima bii, Nditaya tchimo langa.
Ndimvere mwandiuzazi 2. Wakuba uja nachiona,
Ndagonjatu Mbuyanga ’Nu Nangokhulupira,
6. Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee! Ambuye namva pempholo,
Mokoma ndingakhalebe, M’Mwambamo namlandira.
Ndikhale wanu wanudi; 3. Ambuye, mwazi wanuwo
Ndagonjatu Mbuyanga ’Nu. Siitha mphamvu yake,
7. Ndi inetu ndidziŵedi E, Mpingo wonsewo
Chikondi chodabwitsachi Wayera m’kati mwake.
Pansipa ndi Kumwambako; 4. Chionerere mwaziwo
Ndagonjatu Mbuyanga ’Nu Wofuma m’bala lanu,
106 Sindinaleke ineyo
Kutama mtima wanu.
1. NDIKHULUPIRA ’Nu,
5. Kumwamba komwe n’dzaimbira
Mwana wa Mlungutu,
Mpulumutsi wanga,
Mbuyangayo;
Chifukwa ayeneratu,
Mumve popempha ’ne,
Wakonza m’mtima mwanga.
28
Tchimo muchotsebe,
Lero ndikhale ’ne 108
Wa Mlunguyo. 1. Yesu mundimve ndikuliratu,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

‘Dzani kwa inetu; Thupi lonse, mtima womwe,


Mtimangawu ufuna unidi, Mwini wake ndinu nokha.
Bwerani, Yesudi. 4. E, ndikukhurupirirani,
Ndauona mwazi wanu;
Ndinasokeratu kutaliko, Tere ndikugwadirani,
Ndalekana naye Mulungudi; Tere ndapachikwa nanu.
Tsopano koma mndirandirenso,
5. Wadza Yesu wandidzoza,
Bwerani Yesudi.
Ndakonzeka mwa iyeyu;
2. Ndilibe malo mokhaliramo, Ndine wake, tokondana,
‘Dzani kwa inetu; Ndiyamika mbuye Yesu.
Khalani nane m’mtima
mwangamo, 110
Bwerani Yesudi. 1. NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
3. Njobvuta njira ndimayendamo, Inu nokhadi
Dzani kwa inetu; Mundipulumutsa konse
Adetsa m’maso Leroli.
ndimapunthwamo, 2. Kuti mukhululukira
Bwerani Yesudi. Tchimo langalo
4. Wolap mtima simunyozadi, Ndi chifundo chachikulu
Dzani kwa inetu; Chanucho
Pemphero mumve langa lonseli, 3. Kuti muyeretsa mtima
Bwerani Yesudi. Ndibvomeratu;
Mwazi wanu unditsuka
M’mtimamu.
109 4. Kuti munditsogolera
1. Ndilinkudza kwa ambuye Paulendopo;
Ndasauka ,ndinachimwa; Mukwanitsadi zosoŵa
zonse zanga ndizisiya, Zangazo.
kudzapeza moyo wina. 5. Kuti mundipatsa mphamvu
Yopambanayo;
Mau mundilonga m’kamwa
Yesu ndikhulupirira
Mwangamo.
Munafera ine nemwe! 6. Ndikhulupira, Yesu,
Mwa umphawi ndipemphera Mndibvomereko;
Ndine wanu lero, maŵa,
Konseko.
111
1. NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
2. Kale ndinalira inu, Inde zakuipa zangazo;
Kale lomwe ndangochimwa; Anafera ine m’phirimo:
Mund’itana, “idza bwino, Pomva Mawu ake n’kondwako;
Kuti nkuchotsere tchimo”. Mumachoka m’mtima
3. Yesu n’kupatsani zonse, Mwangamo nsonizo,
Zili nanu zokhazokha, Mumachoka m’tima

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Mwangamo nsonizo. “Mwana, gonja, ndikupatsa


2. Chisoni andichotsera Mbuyeyu, Chimwemwe.”
An’thandiza ine teretu; 2. Kale ndinakana Inu,
Ndikhulupirira Iyeyu Ndinathaŵatu:
Andisunga m’manja mwakemu; Ndinazengereza, ndati:
Alimbitsa mtima “Maŵatu.”
Wangawu teretu, 3. Lero mtima ungolema,
Alimbitsa mtima Usaukadi;
Wangawu teretu. Wina wakundimasula
3. Mtima ’we siya ndi Yesu nsonizi, Ndilibe.
Usabisa tchimo lakoli 4. Mbuye, ndingogonja tere,
Zichuluka mphamvu zakezi, Ndibvomerapo;
Likusunga dzanja lakeli; Mundithyole, mundikonze
Bwera kwa Mbuyathu M’mtimamo.
leroli mwana ’we, 5. Chifuniro changa, Mbuye,
Bwera kwa Mbuyathu Ndiperekachi;
leroli mwana’we. Mutsogole, ndidzatsata
112 Inudi.
6. Tere moyo wanga wonse,
1. KWA Inu Yesu ndilira,
Mawu, ntchitonso
Wopanda Inu ndidzafa;
Zidzakondweretsa Inu
Mupulumutse ined,
Zonsezo.
Mundilandiretu.
7. E, chimwemwe chachikulu,
Mundilandiretu,
N’taperekadi
Ndiipa m’mtimamo
Mtima wanga, ndimapeza
Kotero mnandiferatu
Mtendere.
Mundilandiretu.
2. Ndifoka ndi zoipazo,
Ndidzalatu ndi machimo, 114
Sinditha kuzitayazo; 1. Chitha nchianikudyeretsa;
Mundilandiretu. Mwazi wa Ambuye Yesu;
3. Ndayesa kudzikonzadi, Nchiani chindipulumutsa?
Ndapeza mphamvu ndilibe, Mwazi wa Ambuye yesu.
Zoipa zakanikadi;
Mundilandiretu. Chitsime ndi chokoma
4. Onani Mbuye ndigonja, Chindiyeretsa bwino,
Kuyesa kwanga ndaleka; Chinanso sindifuna,
Chitani Inu mumtima; Mwazi wa Abuye ndiwo.
Mundilandiretu.
5. Muyambe ntchito yanuyi, 2. Mtanda m’mtima ndiyangana,
Musalekenso, chitani Mwazi wa Abuye yesu;
Ndidzipereka leroli; Ndikhululukidwa nawo
Mundilandiretu. Mwazi wa Abuye Yesu.
113 3. Zonse zina sizikwana,
Mwazi wa Ambuye ndiwo;
1. YESU, mulikundipempha
Ntchito zanga sinditama,
Munaterodi;

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Mwazi wa Ambuye ndiwo. Yakulenganso ife;


4. Ndikhulupirira bwino Idzakhalatu yangwiro,
Mwazi wa Abuye Yesu; Ndiyo yoyenera ’Nu
Chilungamo change ndicho Usinthika ’lemu wathu,
Mwazi wa Ambuye Yesu. Udzakhala momwemo,
115 Mpakatu Kumwamba komwe
Tidzalemekeza ’Nu.
1. MNDILANDIRE ine Mbuye
Yesu wondifera ‘ne; 117
M’mtima mwanga muzikhala 1. NDILIKUMVA m’mtima mwanga
Mawu anu okhawa. Mau ake a MbuyAnga,
2. Ndasokera m’tali ndithu Ati, “Ndakukonda iwe,
M’njira zopwetekazo; Kodi undikonda Ine?”
Wolemedwa ndingopempha, 2. Ati; “Mwana, kumbukira
Mndilandire inetu. Zonse ndinakuchitira;
3. Pakukumbukira zanga Ndakukonda, ndakufera,
Ndili ndi manyazitu; Ndakufuna posokera.
Ndingogwera pansi, ’Tate, 3. “Ku zoipa zonse zako,
Mlapo wandigwiratu. Goli la pakhosi pako,
4. Ndingopatsa Inu Mbuye Ndi kunthenda zosautsa
M’manja mwanu mtimawu, Ndine ndakupulumutsa
Moyo, mzimu, zonse zanga, 4. “Kodi mayi wobereka
Mzilandire Mbuyetu. Mwana wake adzamleka
30 Pena adzamwiŵalira,
5. Mukhululukire ine, Koma ndikukumbukira.
’Tate mundikondadi; 5. “Nthaŵi ilikudza yonse
Mundisunge nthaŵi zonse Sindisinthanika konse;
Ndi chikondi chomwechi. Imfa sindiletsa Ine
Ndisakondekonde iwe.
116 6. “Ine ndidzakuonetsa
1. A CHIKONDI chopambana, Zonse zakukondweretsa
E, chinadza ndi Mbuye; Za Kumwamba zanga izo,
Chinasangalatsa m’Mwamba, Mwana, sundikonda ine?”
Chinaloŵanso mwa ’fe 7. Ambuyanga, ndalephera,
Yesu ndinu wachifundo, Mwachisoni ndipemphera
Wa chikondi changwiro, Mundipatse ine ndithu
Ee, muloŵetu m’mtimanga, Mtima wakukonda Inu.
Mumuyese mwanutu.
2. ’Dzanitu Wamphamvuyonse, 118
Mtilanditse konseko; 1. ATI Yesu Mbuyeyo:
Musachedwe, thandizeni “Ofoka ndinutu,
Musachoke mwangamu; Mudikire, m’pemphedi,
Inu nokha timakuza Ndidzapatsa mphamvutu.”
Nditumikirabe; Yesu wathadi
Tinyadira chikondicho, Za mangaŵatu,
Tichitame konseko. Inde ndinaipa bii!
3. Tsirizani ntchito yanu Watsuka ine mbuu!

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

2. Mbuye ndimva leroli Zakukondakwakeko,


Za mphamvu zanuzi Anatuma mwana wake
Zomwe zisandutsadi Kundifera kalelo
Mtima wanga woti bii!
3. Ine kanthu ndilibe Inde ndidzaimba nyimbo
Kogula moyowu; Za kukonda kwakeko,
Ndingotsuka m’mtimamo Ndidzaimba ndi Angelo
M’mwazi wa Ambuye ’Nu Akukhala m’mwambamo.
4. M’mene ndifa inedi,
Kumwamba mzimuwu 2. Ndinachita mphulupulu,
Udzakwera komweko Waiwala zonsezo;
Kuonana Mbuyeyo. Ndinakhala ndi zoipa,
5. Ndipo pakuima phe! Wazichotsa zonsezo!
Pokhala Yesuyo, 3. Wandipatsa moyo wake,
Ndidzamama Mlunguyo Moyo wakuyera mbuu!
Kosaleka konseko. Ine ndili mwana wake,
31 Wandilera inetu.
4. Ndiyamika mbuye wanga
119 Ndidzamulemekezabe.
1. LINDIKOMERA dzina la Ambuye
Yesu wanga, 121
Lisangalatsa, lichiritsa, lin’chotsera 1. BWENZI ndinamkomanayo
mantha. Anandikonda kale;
Dzinalo la Yesu, Kukonda kwandigwirako,
Dzinalo la Yesu1 M’kukondamo nditsale.
Lindikomera dzina la Ambuye Yesu Kumtima kundimangako
wanga. Kosamasuka konse;
2. Lichiza mzimu wophwetekwa Ambuye ndine wanutu
ukakhale Kunthaŵi nthaŵi zonse.
bata, 2. Bwenzi ndinakomanayo
Lidyetsa mtima wonse, lipumitsa Anandifera yekha,
thupi langa. Anandipatsa moyowo,
3. Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo Ndatenga ine ndekha.
thanthwe langa, Zimene ndili nazozi
Chikopa changa, linga langa m’mene Nza Yesu mwini zonse,
ndibisala. Ndi moyo wanga wonse ndi
4. Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wakenso nthaŵi zonse.
Wansembe wanga, 3. Bwenzi ndinamkomanayo,
Ndi Mfumu, Moyo, Njira yomwe, Ndapeza mphamvu zanga,
Inde ndimatama, Zakundisunga inemo,
5. Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu Ndiyende m’njira mwanga.
chija, Zolemera zoti mbee!
Pakufa ine Dzina lanu lindilimbikitsa. Zindilimbitsa monse;
Ndalema kuno, komweko
N’kupuma nthaŵi zonse.
120 4. Bwenzi ndinamkomanayo
1. Ndidzaimba za Mulungu,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Wokoma mtima wake, Zidzatu zinanso.


Wotsogolera nzeruzo Mlungu wachisomocho
Zisunga m’njira mwake. Mbuye wathu ndiye,
Palibe wondichotsa ‘ne Ati zinthu zonsezo
Kwa Iye wondikonda; Nzathu mwa Iyeyo.
Pamoyo, imfa, nayeyo (Zina ndi zinanzo
Ndilipo nthaŵi zonse. Zidza kwa ifedi,
122 Inde mtima wakewo
Uli wokomadi.)
1. NDIMKONDE Kristuyo,
2. Mwamva Yesu m’mtimamo,
Ndimkondebe;
Adzanso kaŵiri,
Pemphero langali
M’mene ali nanutu
Mlandiretu;
Muli ndi Chimwemwe.
Ndipempha Inutu,
Ntchito zachifundozi
Ndimkonde Kristuyo,
Iye watha izi,
Ndimkondebe,
Kuti mwawo m’Mwambamo
Ndimkondebe.
Naye tikhalebe.
2. Ndatsatatsatabe
3. Mwamva Mzimu wakewo,
Za pansipa;
Zake zimvekanso
Ndisiye zonsezi,
Kugwa ngati mvulayo
Nditate ’Nu.
Yachisomo chake.
M’mtimanga wonsewu
Mzimu ndiye mphamvudi
Ndimkonde Kristuyo,
M’moyo mwathu muno,
Ndimkondebe,
Mpaka tidzafikako
Ndimkondebe.
Komwe kuli Yesu.
3. Chisoni chonsecho
Chidzatha phe!
Angelo anuwo 24
Afiketu; 1. Poyambapo ndakondwadi,
Nawo, ndiimbetu, N’tapeza inu Mbuyetu,
Ndimkonde Kristuyo, Ndiimba nyimbo yomweti,
Ndimkondebe, Kukondwa sindikhala duu!
Ndimkondebe.
4. Pakufa pangapo Kalelo! Kalelo!
Ndinenebe; Wandisambitsa m’mtimamo,
Myamiko wangawu Wandiweruza lomwelo,
32 Kupempha ndi kukondwako,
Ndikwezebe, Kalelo! Kalelo!
Ndidzapempheradi, Wandisambitsa m’mtimamo.
Ndimkonde Kristuyo,
Ndimkondebe, 2. Mnyamata wake ndinetu,
Ndimkondebe. Ndimvera mawu akewo;
Ndimpatsa mtima wonsewu
123 Ndimtumikira pansipa.
1. MWAKHULUPIRIRADI 3. Kumwamba ndidza……….
Yesu Ambuyathu; Za chipangano chathucho,
Muli nazo zakezo,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Wamoyo sindimsiya ‘yi, Wofatsa ndithu,


Nditafa ndinka kwawoko. Kuti ndiyambe ’ne
125 Ntchito zanuzi;
Akusokerawo,
1. AMBUYANGA Yesu,
Abwere kwawoko,
N’kukondani Inu;
Inde,kwanutu.
Ndisiya zoipa
4. Zambiri zangazo
Chifukwa cha Inu.
Mnandipatsa kale,
Ambuye wabwino
Ndibweza zonsezi
Mundipulumutse konse;
Kwa Mbuyanga ’Nu;
Ndikonda tsopano
Ndikadzaona ’Nu,
Koposa kale lonse.
Mbuye wabwinotu,
2. Ndikonda chifukwa
Mnayamba kukonda; 33
Mnafera pamtengo, Nsembe yokomatu
Munandiwombola. Ndidzakhalabe.
Mukhululukira 127
Zoipa zanga zonse; 1. WAFUNAFUNA ine
Ndikonda tsopano Ambuye Yesuyo;
Koposa kale lonse. Wapeza ine ndithu
3. Ndidzakukondani Wodwala m’mtimamo:
Mwa moyo ndi m’imfa; Zochimwa zanga zonsezo
Ndidzakutamani; Wachotsa izo zomwezo.
Chikondi n’dzaimba. E! chikondi ndithu,
Mpakatu ndidzafa, E! chikondi ndithu,
N’dzanena nthaŵi zonse; Ndi chisomo chake chonsecho,
“Ndikonda tsopano Ndi zozizwa zake zonsezo.
Koposa kale lonse.” 2. Ndafoka ine kale
126 Ndafuna kufaku;
1. AMBUYE, m’imfamo Zinthenda zangazo;
Munandikonda ine; Ndi mwazi wake woti pyu!
Sindikaniza ’Nu Ndayera nawo m’mtimamu.
Kanthu konse ’yi. 3. Mabala ake m’manja
Ndimagwadira ’nu. Ndaona indetu,
Ndikonda m’mtimamu, Ndi minga ya pamutu
Ndidzaperekatu Yolasa Mbuyeyu;
Nsembe yangayi. Etu, wakonda inedi,
2. Kumwamba kwanuko Pamtandapo kufera ’ne.
Mundipempherere; 4. Ndikhumba ine ndithu
Ndikhulupirako, Madalo akewo;
N’dzalandiradi; Ndifuna kumyamika
Ndisenze mtandawo, Masiku onsewo;
Ndikhale mboniyo, Ndikafa ine pansipa,
Ndiperekeko Kumwamba ndizamtamanso.
Mitoloyi. 128
3. Ndikhumba mtimawo 1. AMBUYE Mulungu,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Ndikondwera maka, 4. Akumangidwa ndi mzimuwo,


Ndapeza chimwemwe Mudze ndi ife kwa Yesuko,
Ndi moyo wosatha. Akuchotsereni magoli,
Aleluya, mlemekeze, Nadzakupatsani moyo,
Aleluya, ndiye Mfumu; Mlandu walipa ndi moyo,
Aleluya, mumpembedze Moyo ndi moyo ndi moyo,
Ambuye Mulungu. Tambirana za moyowo.
2. Ambuyanga Yesu 34
Nandikhetsera mwazi,
Nakonza ine 130
Milandu yangayi. 1. ADALITSIKA munthuyo
3. Pamtanda woopsya Wopeza dalo lomwelo,
Adakandifera, Chisomocho cha Mlunguyo
Natsika m’mtimanga Chogwera m’Mpingo wakewo.
Mukhale moyera. 2. Chikhulupiro chomwenso
4. Tsopano Mulungu Chogweratu m’chikondicho;
Alandira ine, Akhala nazo nzeruzi
Popeza Mbuyanga Zofumatu mwa Mbuyedi.
Nawombola ine. 3. Adalitsika, indetu,
5. Padziko lapansi Wodziŵa wadza Yesuyu
Ndikumva chisoni, Nafera iye kalelo
Komatu kumwamba Ampatse moyo wosatha.
Ndikhala ndi Mboni. 4. Akondwerera nthaŵiyi
Pomvera mwini Mlungudi;
129 Mtendere ngwake panotu,
1. IMFA ndi mfumu ya mdimawo, Nakhala nawo m’Mwambanso.
Anthu oipa imangawo,
Akhristu amapulumuka. 131
Omwe aimbira moyo, 1. NDIDZIŴITSITSA Yesu ndi wanga,
Moyo ndi moyo ndi moyo, Tsiku ndi tsiku ndimakondwera.
Wosalekana ndi moyo Anandigula ndi mwazi wake,
Wosamaliza Mulunguyo. Anandipatsa Mzimu woyera.
2. Yesu anafa pamtandapo, Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
Mzimu woipa nugomapo, Yesu ndimtama tsiku lonseli;
Ndi ife titame Mulungu. Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
Ndife tamasudwa m’moyo Yesu ndimtama tsiku lonseli.
Imfa ithedwa ndi moyo, 2. N’kamvera Yesu ndikakondwera,
Tsiku lomaliza moyo Ndiyang’anitsa nkhopeyo yake;
Wosamaliza Kumwambako. Ndipo angelo anditengera
3. M’mitima mwathu mwakhala mbee! Ine chisomo ndi chuma chake.
Mtambo wamdima wang’ambwa ke! 3. Ndine kapolo wa Mbuye wanga;
Panyanjapo pagawanika. Andigwiritsa zintchito zake.
Ndife tipita ku moyo, Ndimyembekeza adzabweranso,
Mtima wabwino ndi moyo; Adzanditenga kwawo ndikhale
Kumbanda kucha kwa moyo 132
Kumatiuza za dzuŵalo. 1. SINDINANYENGEDWA konse

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Pakutsata Yesuyo; Aleluya, Amen.


Yesu apambana zonse Aleluya, ndidzamtama
Ndinalingalirazo. Mulungu wanga.
Pakuyenderana naye 2. Mwazi wa Yesu
Ndimamdziŵa ndi woona; 35
Ndifunitsa anthu onse Unditsukatu,
Adziŵenso Yesuyo! Ndiye Mbuye wanga
Ndifunitsa anthu onse Ndi Mpulumutsi.
Adziŵenso Yesuyo! 3. Pamtanda wake
2. Sindinanyengedwa konse: ’Nafera ine,
Yesu wachotsera phe! Ndi zoipa zanga
Zakuchimwa zanga zonse ’Nazichotsadi.
Zakupsinja mtimazo. 4. Mulungu wanga
Yesu potsagana nane Andilandira,
Wandidzaza ndi mtendere; Chifukwa cha Yesu
Kundisunga, kundikonda Mwana wakeyo.
Sadzaleka konse ’yi! 5. Adzabweranso
Kundisunga, kundikonda, Kundilandira
Sadzaleka konse ’yi! Ndikhale ndi Iye
3. Sindinanyengedwa konse, Masiku onse.
Yesu adzabwerabe;
Mtima wanga undiuza 134
Akuyandikiradi 1. TILI ndi mtendere
Omwe sangamzindikire Wopambanatu,
Andinyoza nandijeda, Monga ngati mtsinje
Koma Yesu ati zedi; Mumitimamo;
“Ine ndidzabweradi.” Koma mtsinje uno
Koma Yesu ati zedi; Umayenda phee,
“Ine ndidzabweradi.” Nthaŵi zonse mtima
4. Sandinyenga, salephera; Nutonthozabe.
Yesu wadalitse ’ne Tikakhulupira
Mpulumutsi ndi Myeretsi Mlungu wathuyo,
Ndi Mchiritsi yemweyo Tidzaona mwayi
Wandiyanjanitsa naye, Ndi mtenderewo.
Mtima wanga nakhutitsa; 2. Dzanja la Mulungu
Sindinanyengedwa konse, Litisunga nji!
Yesu akwaniradi! Nkhondo ya Satana
Sindinanyengedwa konse, Sitiopa ’yi.
Yesu akwaniradi! Zaphokoso zonse
Ndi zoopsyazo
133 Sizibvuta mtima,
1. MULUNGU wanga, Siziloŵamo.
Ndapeza moyo; 3. Masauko athu
Ndili wokondwera Ndi zokondwazo,
Masiku onse. Azilola zonse
Aleluya, muyenera! Ndi Atatewo.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Pokhulupirira Chete! Chete!


Tidzapezabe M’tima mtendere ‘phee!
Kuti mtima wake Udzera kwa Yesu wokonda
Utikonda ’fe. Mtendere mumtimamu.
135
1. YESU ndiye Mbuye wanga,
2. Pamtanda mbuyanga ‘nafera,
Ndamva Mawu akewo
Akandichotsera zochimwa;
Andilandira ine,
Anandigulira mtendere;
Nandipulumutsatu.
Anditonthoza ‘ne phee!
Mwalembedwa mukalata
3. Pomlambira Yesu Mbuyanga,
Mawu ake omwewo,
Mumtima mtendere walowa;
Kuti iwo akumvera
Mdaliso woposa ndapeza,
Akalandiridwatu.
Anditonthoza ‘ne phee!
2. Ndinakahala wakuipa,
4. Pokonda Yesuyo, mtendere!
Ndinamkana kalelo;
Kanthawi kosatha, mtendere!
Koma Yesu waiŵala
Potsata Mbuyanga apatsa
Mphulupulu zangazo.
Mtendere mumtimamu.
3. Wapumitsa mtima wanga,
Kaamba ndaphunziratu 138
Mau ake olembedwa 1. KHALANI duu! Ambuye adzatu;
Mukalata mwakemo. Senzani chete mtanda wanuwu;
4. Mumvetu abwenzi athu, Mulungu adzakonza zanuzo,
Musakanirire ’yi; Sangasinthike mtima Iyeyu.
Yesu aitana inu, 36
Zalembedwa zomwezi. Khalani duu! Bwenzilo Yesuyo
136 Atsogolera m’njira mwathumu.
1. MTENDERE uli m’mtima 2. Khalani duu! Mulungu wanuyu
mwathumu, Akonzeratu nthaŵi zonsedi;
Chifukwa mwazi watitsuka mbuu! Musakayike mtima; zo’psyazo
2. Zakutsogolo sitidziŵa ’yi; Zimasulidwa pomalizapo.
Adziŵa Yesu wathu zonsezi. Khalani duu! A Yesu Mawuwo
3. Abale angakhale m’talimo Ngamphamvu lero monga kalelo.
Mbuyethu asungira onsewo. 3. Khalani duu! pakufa mnzathuyo,
4. Imfa ndi manda sitiopa ’yi, Pakumlirira ndi misoziyo;
Chifukwa Yesu wazithetsadi. Pa nthaŵizo abwera Yesutu,
5. Mtendere wopambana m’Mwambamo Mitima yathu natonthozadi.
Pakufa ife tidzaonanso. Khalani duu! Ambuye athadi
Kutibwezera zochotsedwazi.
4. Khaladi duu! pakufa ifetu,
137 Ndi Yesu tidzakhala indetu
1. Ndiimba mumtima mokondwa Popanda mantha ndi zoŵaŵazi,
Ndi nyimbo yokoma, yoyera; Chikondi chokha koma m’mtimamo.
Ndiimba na Yesu Mbuyanga, Khalani duu! pakutha zonse phe
Anditonthora ‘na………… Tidzasonkhana tonse kuli ’Ye.
139
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

1. NAMONDWE akawombabe, Andifere kalelo.


Mafunde akakulanso, 2. Ngatitu abwenzi anga
Palipo pobisala ’fe. Sandikonda ine ’yi,
Ndi popemphera Yesuyo. Ndikhulupirire Mlungu,
2. Paja athira Yesutu, Iye sandikana ’yi.
Chimwemwe muli m’manthamo, 3. Pansi pano ndili mlendo,
Paja pokometsetsatu, Kwathu ndi Kumwambako;
Mwazi wa Yesu nukhapo. M’mene ndimalira ine
3. Pakulekana ifetu Ndidzapita komweko.
Mitima ikomanapo; 142
Tikumbukana ’bwenzi ’fe,
1. MBUYANGA Yesu, mundigwire
Popempherana komweko.
Dzanja.
4. Tidzathaŵira kuti ’fe
Kuyenda ndekha sindikwana ’yi;
Pochita mantha nkhaŵanso?
Mukandigwira dzanja langa, Mbuye
Pakuyesedwa, tinke ku?
Sindikaopa kanthu kena ’yi.
Tipemphe Yesu mphamvuyo.
5. Tikhale ndithu pomwepo; 37
Zapansi zisaloŵe ’yi. 2. Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
Sitidzapempha m’Mwambamo; Pafupi ndi ’Nu nthaŵi yonseyo;
Tidzayamika Mlungudi. Ndikasoŵatu Inu, Mpulumutsi,
Ndingosekera m’talimo.
140 3. Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
1. MULUNGU anditsogolera, Ukadza mdima m’mtima mwangamu;
Ndapumula m’mtimamo; Koma ndinutu dzuŵa langa ndithu
Ayang’anira njira zanga Lakuwalitsa m’mtima momwemu.
Nsiku zanga zonsezo. 4. Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
Mulungu anditsogolera Pamene ine ndimwalirapo.
Nsiku zanga zonsezo; Mkhaletu m’fupi nthaŵi yomwe Mbuye,
Ndidzatsatira Mbuye wanga Mundiloŵetse ine m’Mwambamo.
M’njira mwake momwemo.
2. Masiku ena pali mdima, 143
Ndivutidwa m’mtimamo; 1. NDIFUNA Inu, Yesu
Masiku ena ndikondwera Ndadzala ndi machimo,
Ndi zabwino zangazo. Mumzimu muli mdima,
3. Masiku onse m’mtima mwanga Ndikufatu m’katimo.
Ndili ndi mtenderewo, Ndifuna kutsukika
Chifukwa ndimakhulupira M’chitsimecho cha mwazi
Mtsogoleri wangayo. Wa Inu wokondedwa,
Munandifera kale.
141 2. Ndifuna Inu, Yesu,
1. M’MENE ine ndisauka Lisoŵa bwenzi lina
Ndi zoipa zangazo, Losungiritsa ine,
Ndidzapita kwa Mulungu, Londithandiza mwina.
Adzandilandiratu. Ndifuna mtima wanu
Mlungu adzandilandira, Wodziŵa nkhaŵa zanga,
Iye ndiye ’Tate wanga; Wondisezera mtolo
Watumiza Mwana wake Wa tchimo lonse langa.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

3. Ndifuna Inu, Yesu, Ukukonda ‘we;


Ndimasauka ndithu, Ndiye mukaona
M’ulendo andisoŵa Wopirirabe;
Kambayo wa padziko. Ukasowa bwenzi,
Ndifunanso chikondi Usaope ‘yi;
Cha Inu chondisunga, Chikondano chake,
Chakundisangalatsa Chikwaniradi.
Panjira ponse panga. 2. Akukumbukira
4. Ndifuna Inu, Yesu, Yesu yemweyo;
Ndidzaonana nanu, Mkuyanjana naye
Mudzadza pamitambo Muli moyomo.
Ikhale mpando wanu; Uderanji nkhawa!
Pamodzi ndi ananu Mpulumutsiyo
Ndidzakondwera kuti; Atisamalira,
Ndilemekeze Inu, Atisungatu.
Ambuye, Mpulumutsi. 3. M’munda mwa Mbuyako
144 Muli ntchitomo;
Amithenga ake
1. Ndifuna yesuyo
Aigwirayo.
Ambuyanga,
Usaime chabe,
Mtendere ndinkemo
Usakhale duu!
Mwa iyeyu.
Yesu akufuna
Umthandizetu
Ndifuna inu Yesu,
4. Kwawo kwa Mbuyeko
Nthawiyi ndifuna!
Udzafikako;
Kwa Yesu Mbuyathu
Mwa ulemerero
Ndifunako.
Udzapuma ‘phee!
Usalowerere,
2. Ndifuna Yesuyo
Mvera Yesuyo,
Mobvutamo,
Ati: “mwana wanga,
Ndipulumukemo
Bwera kwathuko.”
Mwa iyeyu.
3. Ndifuna Yesuyo 146
Mokondwa ndi 1. PAMENE ndisauka,
Mowawa, adzemo Pamene ndivutidwa,
Ndi moyodi. Mizimu yakuipa
4. Ndifuna Yesuyo, Ikadza nindiyesa,
Ndichite ‘ne Mulungu wanga,
Zofuna zakezo, Mwini mphamvu,
Ndidzazabe. Mkandikumbukire ’ne.
5. Ndifuna Yesuyo 2. Pamene ndilemedwa
Woyeratu, Ndi zakuipa zanga,
Ndikhale wakeyo Poloŵa mdima m’mtima,
Wa iyeyu. Pochita ine mantha,
145 3. Masiku anga onse
Mulungu mundisunge;
1. Mtima wa mbuyako

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Pamene ndimwalira, Mbuye, ndithaŵire kwanu


Ndi tsiku lomaliza, Poti mundikonda.
147 3. Sindidziŵatu zamaŵa,
Koma sindiopa;
1. KHALA chete mtima wanga
Ndidzakhulupira Inu
Mlungu wako ndiye Mfumu;
Kuti mundikonda.
Zinthu zonse zisinthika,
4. Inde wakukonda ndinu;
Mlungu ndi wachikhalire.
Mawuwo oona
(Khala chete,
Andidzaza ndi chimwemwe:
Chidzakupinga ninji?
Mlungu andikonda.
Usaope,
Mulungu ali nawe.) 150
2. Anthu onse pansi pano 1. Odala ndi onsewo
Sakhutitsa mtima wawo; Oyera m’mtima mwawo;
Amadera zinthu zawo, Adzaonana ndi Mulungu,
Namakhumba zakutali. Yesu ndiye wawo.
3. Khala chete mtima wanga, 2. Ambuye anachoka
Zikwanire zinthu zako; Mumwamba, mwini moyo,
Usakhumbe zapansipa Wofatsa anakhala nafe,
Koma Mlungu wako yekha. Mfumu yachisomo.
148 3. Mumtima wakufatsa
Anaconda kukhalabe
1. NGATI mtima sumakonda
Asankha mtima wakuyera,
Yesu supumula bwino;
Ndiwo nyumba yake.
Mbuye, suwu mtima wanga,
4. Tifuna inu mbuye,
Ndiwo wanu, mulandire.
Mtininkhe mtima uwu
38 Wodzichepetsa, wakuyera,
2. Dziko lonse ndilitaya; Woyenera inu.
Ndikondetsa Yesu Mbuye;
An’komera kopambana 151
Andikondweretsa ndiye. 1. MNDIYANDIKITSE nanu.
3. Ndakudani, mnandikonda Yesu,
Ndi kukhetsa mwazi wanu. Ndiyenderane nanu;
Simuleka kundikonda; E, nditsamire panu, Yesu,
Ine sindidzalekanso. Panjira yonseyi.
4. Mndisungire mtima wanga, 2. Ndionetsere kuunika
Uzikhulupira Inu, Kokoma kwanu, Yesu!
Kuti moyo wanga wonse Yabwino mbiri ndibukitse
Ubisaletu mwa Yesu. Yokondweretsayo.
3. Chitsime chakuyera ine
149 Ndifanefane nacho;
1. NJIRA yanga sindiziŵa, Mundigwiritse ntchito zanu
’Tate muikonza; E! zanu zokhazo.
Komatu muzindikira 4. Mulamulire mtima, Yesu,
Kuti mundikonda. Ndi chifuniro changa;
2. M’mene mantha andigwira, Muloŵe mwanga ngati Mfumu;
Andidetsa m’mtima, Mundimveretsedi.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

152 Kumwamba n’dzaimbira


Kukoma kwanuku;
1. “KHALA mwa Ine,” Yesu anatero;
N’dzatama nthaŵi zonse
Mawu abwino, koma Mbuye wanga
Chikondi chanucho.
Sin’ngathe ndekha, mukhalitse ine
Mwa ’Nu ndikhale nawo moyotu. 154
2. “Khale mwa Ine,” munachotsa tsoka, 1. KHALATU woyera, pempheratu
Mletse Satana anganyenge ine: m’tseri;
Mibvi yamoto yake muizime Werengani Mawu masiku onsewo.
M’mtimamo, ndikhulupirire ’Nu. Uthenga omwe ali akufoka,
3. “Khala mwa Ine,” ndinu mwini Madalitso ake ufunefunebe.
mphamvu, 2. Khalani woyera, dziko laipadi;
Mundithandize ine ndikafoka; Pemphera kolimba kwa Yesu
Mzimu Woyera andiululire Mbuyathu.
Zoona zanu m’mtima mwangamu. Yang’anitsa Yesu ndi kumutsatira,
4. “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo. Kuti anthu ena aonenso Iye.
Nthambi zouma zidulidwa m’mtengo: 3. Khalatu woyera, akutsogozetu;
Ine wopanda Inu ndifokanso, Usamtsogolere munjira zakozo.
Zipatso zikasoŵa msadze ’ne. Pokondwa ndi m’nsoni tsata Ambuyako
5. “Khala mwa Ine,” Mbuye, ndifunitsa; Khulupira Yesu ndi Mawu akewo.
Mzimu Woyera mlonge m’mtima 4. Khalatu woyera, khalatu wofatsa;
mwanga, Alilamulire ganizo lakolo.
Akagonjetsetu machimo anga, Utatsogozedwa ndi Mzimu wakeyo,
Mtima woyera andipatsenso. Msanga udzagwira m’Mwamba
153 ntchito yake.
1. AMBUYE mundisunge 155
Pafupi ndinutu; 1. MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi
Palibe malo pena chikondicho,
Popuma pansipa. Ukhazikike pa Mulungu wosachokapo.
Adani andizinga, 2. Mwa ine myatse moto wanu waku
Zoipa m’katimo; yera mbuu,
Chifundo chanu Yesu Utenthemo zoipa zonse zidakhalamo.
Chikonze m’mtimamo. 3. Mubweretu nomwe ’Nu munatsika
2. Ndikabisala mwanu kalelo;
Ndilibe mantha ’yi; Ndilira Inu mundidzaze mphamvu
Ndikasungidwa kwanu yanuyo.
Mumtima muti phee! 4. Ndikhazikike inetu, mumtima muli
Ndi mphamvu yanu yokha mwai,
39 Ndi Yesu ndikondanetu, si kanthu
Ndiposa ’daniwo; kena ai.
Chifundo chanu Mbuye 156
Chitchinjirize ’ne 1. MBUYE ndamva mwawazira
3. Ndidzaonana nanu Anthu ena madalitso;
Mokondwakondwadi. Mvula yanu yawagwera;
Oyera mtima onse Mbuye, ine mudalitse.
Apenya Mbuyeyo.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Etu ine, etu ine, Moyo wangawu ngwabwinotu.


Mbuye, ine mudalitse. Moyowo
2. ’Tate, msandipitirire, Ngwabwino,
Ndimaipa mtima ine; Moyo wanga ulitu bwino.
Ndiyenera munditaye, 2. Ngakhale Satana andizunza ’ne,
Koma mukhululukire. Chilipo chitonthozacho;
3. Yesu, msandipitirire Chifundo cha Kristu anafera ’ne,
Kuti ndinu ndikondane; Kundipatsa ’ne moyo wake.
Ndinalira Inu Mbuye, 3. Uchimo unapachikidwa pomwe
Msandileke poitana. Pamtanda wa Yesu Mbuye;
4. Mzimu, msandipitirire, Machimo angawo anatherapo;
Mupenyetsatu akhungu Mbuye wanga, ndiyamika ’Nu.
Mboniyo ya Mbuye Yesu, 4. Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
Mundipatse ine mphamvu. Limene ndidzaona ’Nu;
5. Ndinagona mwa zoipa, Lipenga limveke, ndidzakondwatu
Ndinakunyozani ine, Pakukomana ndi Yesuyo.
Dziko lino ndinakonda, 159
Mbuye, mukhululukire.
1. NDILIRA ine kukayenda
6. Ha! chikondi cha Mulungu,
M’njira ndi Mulungu;
Mwazi wa Mbuyathu Yesu,
Ndilira nyali ndikaone
Chiyanjano cha Mzimuyo
Njira Ya kwa Yesu.
Zonse zidzalemekeza.
2. Chimwemwe chija chamumtima
157 Ndinalaŵa kale
1. AMBUYE, thandizenitu Poyambutsata ine Yesu,
Ndi mphamvu zanuzo; Chili kuti tere?
Pantchito zathu zonsezi 3. Kalelo m’mtima ndinakondwa,
Mthandize Mbuyathu. Tere ndingolira,
2. Zochimwa zathu m’mtimamo Zokoma zonse zapadziko
Tilira nazotu; Sizindikwanira.
Mumtima mwathu muti zii; 4. Mubwere, Mzimu wa mpumulo,
Mthandize Mbuyathu. Mundileze m’kati;
40 Ndidana nazo zoipazo
3. Mthandize Mbuye, timvetu, Zinakuchotsani.
Tikalandiredi 5. Mundichotsere tchimo lonse
Zimene muperekazo Ndinakonda kale,
Zakudalitsa ’fe. E, muligwetse kuti ndinu
4. Kumwamba Yesu mthandize, Mfumu mukakhale.
Tilibe wina ’yi: 6. Mkatero ndidzayenda m’njira
M’moyo, muimfa mthandize, Ndi Mulungu wanga,
Tikhale kwanuko. Idzandiunikira nyali
Njira ya Kumwamba.
158
1. POKHALA mtendere mu 160
mtimangamu, 1. NDILIRA mtima wotamanda
Pamene ndisaukanso, Mlungu, ndi woyera,
Pamene mabvuto ndi akuludi, E, mtima woyamika mwazi

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Munandikhetsera. Musambitse ine, ndiyeretu mbuu!


2. Mtimatu wopirira ndi 4. Chifukwa cha ichi ndipempheratu,
Wofatsa mkati mwake, Ndidikira Inu Ambuyangayu;
Mumveka Mbuye Yesu yekha, Ndikhulupirira pa mwaziwo pyu!
Ndiye Mfumu yake. Musambitse ine, ndiyeretu mbuu!
3. Ndilira mtima wakulapa 163
Ndi womvera Yesu,
1. USAFUNE, chuma chokha,
Wosasiyana ndi Ambuye
Pena maseŵera okha,
Wakukhala m’mwemo.
Koma za Mulungu zokha
4. E, mtima watsopano ndi
Zipambana zinazo.
Wodzala ndi chikondi,
2. Ukafuna kulemera,
Wangwiro ndi wokoma, Mbuye,
Pempha chuma chosathera,
Wonga wanu wonse.
Ndiwo mtima wakuyera
5. Mkhalidwe wanu mundipatse
Ndi wokonda Yesuyo.
Ndifanane nanu
3. Zosauka ubvomere,
Mulembe m’mtima mwanga Dzina
Ndipo Yesu chaulere
La chikondi chanu.
Chikondano ndi mtendere
161 Aloŵetsa m’mtimamo.
1. Zoipa zangazi 4. Zonse umazinyadira
Zidetsa m’mtimamu; Udzaleka kusirira;
Mnditsuke, Yesutu, Uli nazo zokwanira
Kutsuka koti mbuu! Pakupeza Yesuyo.
41 5. Mbiri yake ubukitse,
2. Ndafoka inetu, Anthu onse nuphuzitse,
Ndalema m’mtimamu; Kwa Mulungu nufikitse
Andilimbitsa ’Ye, Osokera onsewo.
Kulimba koti njo! 6. Yesu sakusiya konse;
3. Zin’soŵa indedi Mphamvu, nzeru, chuma chonse
Zabwino m’mtimamu; Akupatsa nsiku zonse;
Ambuye, mdzazebe, Tsata Yesu yekhayo.
Kudzaza koti tho! 164
162 1. MKRISTU, ulimbike
1. AMBUYE, ndifuna nditsukenitu; M’ntchito yakeyo;
Mukhalire ndine mumtimangamu; Yesu anafera
Muthyole zonsezo zodetsa ’netu; Anthu akewo.
Musambitse ine, ndiyeretu mbuu! 2. Mphamvu zathu zonse
Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu! Tionetsenso,
Musambitse ine, ndiyeretu mbuu! Kuti kudziŵike
2. Ambuye, chotsani zonse zomwezo Tili akewo.
Zakundisautsa mumtimangamu; 3. Mtima wakufatsa
Ndileke zangazo zoipsa ’netu Amakondako;
Musambitse ine, ndiyeretu mbuu! Ndipo anthu onse
3. Kumwamba ndiona Ambuyangayo, Angatengero.
Mudzandithandiza, nditsate ’nemo; 4. Mapemphero athu
Mudzandichotsera zoletsa ’netu; Tikakwezebe,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Dzina lake lomwe 4. Tioperanji ifetu?


Tiyamike ’fe. Ali pafupi Mbuyeyu;
5. Limbikani nonse Sangasinthike mtima ’yi;
Mpaka imfayo. Kristu akonda ifetu.
Ndipo Mfumu yathu 167
Idzakondwako.
1. MBUYE, nditsate bwanjiko?
165 Ine ndikonde bwanjinso?
1. GWIRA zintchito zako, Bwanji kuyenda m’njiramo
Pomva usiku udza; Yonka Kumwamba kwawoko?
Yamba mamaŵa ndithu 2. Kodi m’njiramo ndimvadi
Potuluka dzuŵa. Nsoni zoŵaŵa, nkhaŵazi
Gwiranso m’msana monse Ndi masauko, mingayi?
Dzuŵalo likatentha; E, nkana izi n’tsatabe.
Gwira tsopano ntchito; 3. Anasauka Mbuyeyo,
Msanga udzaleka. Mwini nalola zonsezo;
42 Anatsiriza ntchitozo,
2. Ntchito za Yesu gwira Osabwerera imfayo.
Pomva usiku udza; 4. Ndikamayenda m’dimamo,
Lero lonseli gwira, Mletse zodandaulazo;
Bwino udzapuma. Mundikumbutse mtandawo;
Gwiratu tsiku lonse Zanga zichepa zonsezo.
Ntchito zakuyenera; 5. Ine nditaya chumacho,
Gwira tsopano ntchito, Ndikondweretse Mbuyeyo,
Tere udzaleka. Thupi liopa mingayo,
3. Mkristu gwiratu ntchito Koma mlimbitse mtimawo.
Pomva usiku udza; 168
Dzuŵalo lopendeka 1. YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Tere lidzaloŵa. Loŵa m’njira yake yakuyerayeratu;
Gwiranso ’dzulodzulo Anadzera m’Mwamba kutiperekezako;
Kutada mdima bii! Yamba msanga iwe kunka kwanuko.
Tsono zintchito zonse Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
Zatha zonsezi. Iwetu, iwetu, ukatsatanso.
166 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
1. TITHAŴIRENJI ifetu Inu nonse mukatsate Mbuyeyo
Mphamvu za Yesu nzathunso. 2. Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
Kristu atithangatatu. Udzakhaliranso kuli Mbuye wakoyo;
M’nkhondo ya moyo wathuyo. Adzapulumutsa thupi, mzimu wakonso,
2. Yendani bwino m’njiramo M’mphamvu ndi chilango cha zoipazo.
Ya kwa Mulungu wathuyo; 3. Kunsi kudambo, pena m’mwamba
Kwezani maso kuli ’Ye; m’phirimo,
Kristu ndi njira yomweyo Pomwe pali Yesu ndidzayenda
3. Nkhaŵa tilbe; Yesuyo yendapo:
Atsogolera m’njiramo; Andiperekeza bwino m’njira yakeyo,
Tikhulupire Iyeyo, Kuli Mzinda wa Mulungu wangayo.
Kristu ndi moyo wathuwo.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

169 Tidzabwera tonse


Ndi zipatsozo.
1. MBUYE, mwatiuza ’fe
3. Tingolira kaya,
Tizikhala mchere
Koma tidzafesa
Wokometsa onsewo
Mbewu za Ambuye;
Akumanga kwathu.
Ntchitoyo nja Yesu.
Mcherewu ndi ifetu;
Adzachotsa msozi,
Mtifanize nanu,
Adzatilandira,
Tikakope ndi chitsanzo
Tidzabwera tonse
Onse akuchimwa.
Ndi zipatsozo.
2. Mbuye, mwatiuza ’fe
43 171
Tizikhala nyali 1. M’MENE umauka m’maŵa,
Yoonetsa onsewo Sunagwire ntchitozo,
Njira yonka kwanu. Sunayambe kukayenda,
Nyali ndi ifetu; Ugwadire Mlunguyo.
Kuunika kwanu Pena uli kusekera,
Mutipatse tiŵalire Pena nkhaŵa m’mtimamo,
Osokera onse. Wachimwemwe, wachisoni,
3. Tisasungaluke ’yi, Uza Yesu zonsezo.
Tisasiye Yesu. 2. Wakuchezacheza naye
Tisabise nyaliyi Ukagwira ntchitozo;
Pakuchita mantha. Pakukumbukira Yesu,
Mcheretu ndi nyaliyi Nkhaŵa zidzachokanso
Tizikhala tonse; Ndi zapansi zikafuna
Mbuye, mtiyeretse m’mtima Kukudzaza m’mtimamo,
Tikatero ndithu. Utsogole kopemphera,
Uza Yesu zonsezo.
170 3. Ndi m’kutero udzadziŵa
1. M’MAŴA tizifesa Chifuniro chakecho;
Mbewu zakukoma, Iye adzakuthandiza
Msana ndi usiku Uthangate enanso:
Tizifesa momwe. Ndi ofoka ulimbitse,
Nyengo yamasika Akulapa bwezatu;
Tidzatema m’munda, Ndi za ntchito zake izi
Tidzabwera tonse Uza Yesu zonsezo.
Ndi zipatsozo. 4. Ndipo ngati ungolema,
Ndi zipatsozo Ulefuka m’dzulomo,
Ndi zipatsozo Ndi Satana akayesa
Tidzabwera tonse Kukukola m’mtimamo:
Ndi zipatsozo. Wakufoka, wakuopa,
2. Tizifesa m’dzuŵa Penyetsetsa Iyeyo;
Tizifesa m’mthunzi, Udzakhazikika m’mtima
Sitiopa ife Pakumuza zonsezo.
Mtambo ndi chisanu.
Athatu masika 172
Ntchitozi zidzatha; 1. HAYA! ’nzanga taonani

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Yoonekayo Tiyeni, tiŵauze za Mbuyathu


Yakumwamba iti: “Yesu Mpulumutsi
Alikudzako.” Nitiŵanditse mbiri yake
Kanganani nkhondo yanu M’dziko lonse lathu.
Ndi mbendera mbuu! 174
Tibvomere: ‘Inde Mbuye
1. LIMBA mtima mbale wanga
Mtithangatetu.”
Usapunthwe m’njirayi;
2. A! mizimu yakuipa
Onatu nyenyezi ija
Isautsabe,
Ikutsogoleradi.
44 Tamveratu Mlungu yekha,
Tikaniza zakuipa Chita zolungama ’we,
Zotizinga ’fe. Yenda bwino, khulupirira
3. Mdani adza nazo mphamvu, Mbuyeyo, Mbuyeyo,
Koma ifetu Ndikuchita zakezi.
Tidzamthetsa nkhondo yake 2. Taya zako zochenjera,
Timwingitsetu. Taya zamumdimanso;
4. Yesu ati, “Ndidza msanga!” Nthaŵi zonse khulupira,
Thangateni phee! Chita zolungamazo.
Mbweze mawu akulimba: Usayang’anire wina
Tikanganabe. M’khondo yake yomweyi,
173 Koma m’zonse khulupirira
1. ANATILEMBA Yesu tikagwire Mbuyeyo, Mbuyeyo,
nkhondo yake, Ndi kuchita zakezi.
Natilimbitsa tipirire osaopa kanthu. 3. Leka zakuipa zako,
Kwa Satana n’ziwembu zake Myambi yonse yoti bii,
Sitigonja konse; Usakhulupire mommo:
Tiyenderana naye Mfumu Tamveradi Mbuyedi.
yathu yopambana. Adzadana nawe ena,
2. Amaliwongo ochuluka amaloŵa Ena adzakonda ’we;
m’mtima Kweza maso, khulupirira
Nafuna kuipitsa usana ndi usiku; Mbuyeyo, Mbuyeyo
Tikatsatabe Mfumu yathu Ndikuchita zakezi.
Sitidzagwa konse, 4. Mawu ake atipatsa
Pakuti atipatsa mphamvu Mphamvu ndi mtenderenso,
tipambane nazo. Bwino atitsogolera,
3. Amatininkha zida zoteteza mtima, Tikhulupirira ’wo
Ndizo; Limba mtima, usapunthwe
Kupempherabe, kukhulupirira ndi M’njira yamumdimayi;
kufatsa; Yenda bwino, khulupirira
Mtheradi, ndi lupanga ndilo Mbuyeyo, Mbuyeyo,
Mawu a Mulungu; Ndi kuchita zakezi.
Pogwira zida zakezi sitilephera 175
konse. 1. POYESEDWA ine
4. Mafumu atiuza tikaletse ukapolo, Yesu mudzetu,
Ndi kumasula goli la anzathu akuopa Mundipempherere

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Ndisachimwetu. Kumwamba kuli Inu,


Mukaona kuti Ambuye wangayo.
Ndilefukatu, 3. Yochita ndi yodikha
Mbuye mndilimbitse Mupatse mphamvuyo,
Nazo mphamvutu. Ndikhale wochenjera,
2. Ndi zapansi pano Wogwira ntchitozo.
Ndikokedwadi, Zoipa zanga zonse
Koma ndi chisoni Mufafanizezo,
Mndiphunzitsedi; Ndiyende nanu nokha
Ndisaiŵalire Masiku onsewo.
45 177
Za Getsemane, 1. TIYENI Akhristu,
Pena mtanda wanu Nkhondo tigwire;
Yesu Mbuye ’Nu. Yesu Mbuye wathu
3. Mukandipweteka, Atitsogolera.
Ndipirirapo: Mfumu yathu mwini
Nsembe yanga ndiyo, Atipatsa moyo;
Landirani ’yo. Taonanitu mbendera
Ndikachita mantha Yailoŵa nkhondo!
Sindithaŵa ’yi: Tiyeni Akristu,
Mtima udzalimba, Nkhondo tiigwire;
Ndidzaima nji! Yesu Mbuye wathu
4. Pakumalizidwa Atitsogolera
Moyo wangawu, 2. Nkhondo ya Satana
Pomwalira ine, Idzakuthaŵani;
Mudze Mbuyetu. Tiyeni Akristu,
Ndidzadzipereka Kaipambaneni.
M’manja mwanumo: Idzanjenjemera
Mpulumutsi Yesu Mukapfu’litsatu;
Mndilandireko. Imbitsanitu anzathu,
176 Mau mukwezetse.
1. AMBUYE wa Kumwamba, 3. Mpingo wa Mulungu
Mundithangatetu Uli ngati nkhondo;
Kuyenda bwino lomwe Titsagane nawo
M’ulendo unowu. Ana a Mulungu.
Kaŵiri ndi kaŵiri Sitipatukana,
Ndipunthwa m’njiramo Ndifetu amodzi;
Mlimbitse mtima wanga, Ch’yembekezo, chikondano,
Ndingatayikeko. Chonse ndi chimodzi.
2. Ndikhumba Mzimu wanu 4. Zonse zapadziko
Kundiyeretsa mbuu! Zidzamalizira,
Pang’ono ndi pang’ono Koma mpingo wake
Mundiphunzitsetu; Uli chikhalire;
Ndifuna nzeru zanu Udzakhala ndithu
Zakundifitsako Mphamvu za Satana,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Yesu analonjezetsa, Ya Mbuye wathuyo;


Mawuwo sakana. Tileke zakuipa
5. Tiyeni anzathu Zokhala m’mtimamo.
Tizithandizana; Sitikwanira tokha
Imbirani nafe Kuleka zathu zomwe,
Nyimbo zopambana Koma Mbuyathu Yesu
Kristu ayenera Atithangatatu.
Mphamvu ndi ulemu; 3. Tsopano timenyana
Komwe kuli Yesu. Ndi zakuipazi;
46 Pamene nkhondo yatha
Tidzanka kwathuko.
178 Yesu adzalandira
1. TIYENI, Akristu inu, Ankhondo ake onse;
Mumenyane nkhondo iyi, Adzakhalika naye
Mukafoka nonse, koma Kumwamba komweko.
Yesu akulimbitsani.
2. Muyendanso kunka komwe, 180
Mugonjetse mdani wanu; 1. MBUYE, ndapangana
Musafoke, musaleme, M’njira yanuyi,
Musagone konse inu. Kuti ndidzayenda
3. Musagonje, anthu inu, Osaleka ’yi.
Mtamiretu Yekha Mbuye; Mundipatse mtima
Ipambana mphamvu yake, Wopiriramo,
Ya Mtsogoli wanu yemwe. Wakukana zonse
4. Mtima wanu wonse ndithu Zondipingazo.
Udzakhala ndi chimwemwe. 2. Mzimu wakuipa
Zida zanu mbvale bwino Undiyesa ’ne;
Zakudzera m’Mwamba momwe. Mundithangatire
5. Limbikani inu nonse, Ku’thaŵitsabe.
Msangalalo ngwanu nokha; Akandisautsa
Musaope kanthu kena Kum’dzi kunoku,
Mumtamire Mbuye Yekha. Muloŵetse mphamvu
6. Tiyeni ku nkhondo iyi, M’mtima mwangamu.
Mugonjetse zonse konko; 3. Akathira nsembe
Muingitse mdani uja, Ku mizimuyo,
Muyendetse m’njira momwe. Ndipenyera kwanu,
E, Kumwambako.
179 Tsoka ndi zonyenga
1. AKRISTU limbikani, Za ufitizo,
Imani mtima nji! Yesu mndilimbitse
Mbendera nyamulani, Ndisaopezo.
Msatenthemere ’yi. 4. Pena kumwa nawo,
Wotsogolera wathu Ndisateroko,
Ndi Mwana wa Mulungu; Pena kukaona
Adzagonjetsa onse Gule woipa,
Adani athuwo. Pena kuwombeza
2. Tigwire nkhondo yomwe

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Sindifuna ’yi; Inde, mudze inu nonse,


Yesu mundithandize Mudze nafe paulendo.
Kuzikanazi. Inde, mutiperekeze,
5. Ndinu mbusa wanga; Yesu atilinda ife.
Mndithandizetu; Yesu atilinda ife
Ndisaipse nazo Kuli dzikolo labwino,
47 Yesu atilinda ife
Mtima wangawu. Kuli dzikolo labwino.
Osaopa konse, 182
Osachimwa ’yi. 1. ANA akumwamba ndife,
Mundiyendetse Yesu Paulendo timaimba;
M’njira yanuyi. Timatama Mbuye wathu
181 Wa ulemerero wonse.
1. AULENDO, munka kuti Tilikupita kwathu kuja
Ndi zindodo m’manja mwanu? Munjira ya atate athu,
Paulendo tizipita; Amakondwera lero lomwe;
Aitana Mbuye wathu; Tinka kuonana nawo.
Pamapiri, pamadambo 2. Mbuye anatiitana
Tizipita komwe kwawo. Kukagwira ntchito yake,
Tizipita komwe kwawo Kuitana anthu onse
Kuli dzikolo labwino, Atsatenso njira yino.
Tizipita komwe kwawo 3. Inde Mbuye, tibweradi,
Kuli dzikolo labwino. Zathu zonse tizisiya,
2. Kodi simuopa njira, Mtsogoleri wathu ndinu
Inu anthu akufoka? Titsatabe inu nokha.
Ayi, atiperekeza 183
Mbuye wathu wotikonda. 1. MBUYE munditsogolere,
Iye amakhala nafe, Ndine mlendo m’dziko muno;
Natitsogolera ife. Ndikafoka mundikweze,
Atitsogolera ife Mundisunge m’manja mwanu;
Kuli dzikolo labwino. Mundidyetse, mundidyetse,
Atitsogolera ife Sindingamve njalayo.
Kuli dzikolo labwino. 2. Mundimwetse madzi anu,
3. Mundiuze, aulendo, Andichize nthenda zanga;
Muli chiani m’Mwamba muja? Utsogole mtambo wanu,
Atibvekako zoyera Ndikadziŵe njira yanga;
Akorona natininkha; Mpulumutsi, Mpulumutsi,
Moyo, moyo atipatsa, Munditchinjirizetu.
Kwa Mulungu tidzakhala. 3. Ndikaloŵa m’mtsinje muja,
Kwa Mulungu tidzakhala Mndichotsere mantha osne;
Kuli dzikolo labwino, Mndiwolotse tsidya lija,
Kwa Mulungu tidzakhala Ndikondwere nthaŵi zonse;
Kuli dzikolo labwino. Nyimbo zanga, nyimbo zanga
4. Kodi inu, aulendo, Zidzalemekeza ’Nu.
Ife titsagane nanu?

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

184 Nditsatatu.
Ndidadzikuza osaopa ’yi;
1. NDIMAYENDA paulendo
Ambuye, msakumbuke zomwezi.
Ndi yaminga njira yake;
3. Ndi kale lonse mnandisunga ’ne;
Tsoka ndikapeza, koma
Tsopanonso.
Ndinka kwa Atate;
M’khwaŵa, paphiri, mundisungebe
48 M’tsogolomo.
Pena m’mtima mwanga mwada, Ndipo mamaŵa n’dzaonana ndi
Pena andibvuta ‘dani, Abale anga adafikadi.
Ndikatenga nkhaŵa, mantha,
Amadziŵako. 186
2. Ichi chindisangalatsa 1. TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
M’mene nkhondo indigwira, Tiimbe nyimbo yabwino,
M’mene nsoni zazikulu Tiimbe nyimbo yabwino,
Zimanditsatira; Ku mpando wakewo,
Mtima ukhazika m’mene Kumpando wakewo.
Kwathu kuja ndikumbuka Tiyeni pamodzi
Kuti Mlungu ali ndine, Tilikupita Kumwamba;
Andisungako. Akristu tilikupita
3. Mbuye andipeza lero, Ku mzinda wa Mlungu.
Andikonda, andisunga; 2. Ngakhale enawo aleke kwimbako,
Adzapitikitsa mdani Akristu ’fe tidzaimba,
Akamandibvuta. Akristu ’fe tidzaimba,
E, ulendo wanga utha, Kumlemekeza ’Ye,
Tsono ine ndimwalira; Kumlemekeza ’Ye.
M’mene ndidzafika kwawo 3. Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
And’landirako. Koposa anthu enawo,
4. Komwe ndi chimwemwe ine Koposa anthu enawo,
N’dzaonana ndi Atate, Tisanafikeko,
N’dzagwadira ndi kumtama, Tisanafikeko.
Amandikondabe. 4. Tiimbe mokondwa, misozi iume;
Sakandisautsa kanthu Poyenda kunka kwathuko,
M’dziko lija lakukoma; Poyenda kunka kwathuko,
Adzandidalitsa Yesu, Kwa Mlungu wathuyo,
Ndidzakondwako. Kwa Mlungu wathuyo.
185 187
1. MUNDIŴALIRE m’njira 1. NDAMVATU kuti tifika komweko
mwangamo, Kuli Ambuye, Mtetezi wathuyo.
Mbuyanga ’Nu. Ine, pakutha zobvuta zathuzo
Kwada usiku, ndasokerako, Iye tidzamwona maso ndi maso.
Mtsogoletu. Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
Phazi langali mndisungirenso, Kupenyanso wokondatu;
Ndilonde Inu m’njira monsemo. Tidzakondwera, E, nthaŵi zonsezo
2. Sindidapempha kale Mbuye ’yi, Ndicho chimwemwe ndi ulemutu.
Mtsogole ’Nu; 2. Kaamba chisomo cha Mbuyathu
Ndisankha ndine, koma leroli uyu,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Malo okoma tipeza m’Mwambamo; Poliriratu abale,


Kumva mtetezi amene ndi Yesu, Yesu mutimveretu.
49 2. Munabvala thupi lathu,
Ndicho chimwemwe ndi chachikulutu. Munadziŵa masauko,
3. Onse aliko takonda kalelo, Mnalirira bwenzi lanu;
Kale napita kwa Yesu Mbuyawo; Yesu mutimveretu.
Koma kumwona Mtetezi wathuyo 3. M’mene imfa yathu idza,
Ndicho chimwemwe choposa, Mweya wathu ukaleka,
nchathucho. M’mene ife timwalira,
Yesu mutimveretu.
188 4. Mnamwalira Inu paja,
1. UKATHA moyo wanga Mwazi wanu munakhetsa,
Kumwamba kundichera; Koma Inu munadzuka;
Dzuŵalo ndimalira Yesu mutimveretu.
Lafika lokomera. 5. Mtima ukachita nkhaŵa
Usiku m’nali mdima, Ndi zoipa zotimanga,
Tsopano mbanda kucha; M’mene tikachita mantha,
Kudzaŵalitsa ndithu Yesu mutimveretu.
Ku Dziko la Mulungu.
2. Chitsime chachikondi 190
Ndi Yesu Mbuye wanga; 1. KODI uli ndi chisoni
Ndalaŵa mtsinje pano Choliritsa mtima wako?
Ndzamwetsa ine m’Mwamba. Kweza maso, ndi Atate
Komweko zidzakula Akumvetsa zonsezi.
Chisomo ndi chifundo, 2. Kodi umadandaula;
Pondiŵalira kuja “Mbale wanga waferanji?”
Ku Dziko la Mulungu. Kumbukira Wakumtenga
3. A! Yesu Bwenzi langa Saphophonya konse ’yi.
Inenso bwenzi lake, 3. Mbale wako unamkonda,
Woipa ’ne alola Koma Yesu amkondetsa;
Ndiloŵe m’nyumba mwake; Anamfuna nagomtenga;
Ndikhulupira Iye Usammane Yesu’yi
Achotsa mphulupulu; 4. Pakutsazikana nanu
Kudzandiŵalitsira Ndi potseka maso ake,
Ku Dziko la Mulungu. Imfa, bii! Anangogona
4. Ambuye andisunga Koma adzadzukanso.
M’chifundo chachikulu; 5. Usalire; Mpulumutsi
Zisoni zisanduka Analaŵa imfa Yekha;
Chimwemwe cha Mulungu. Imfa yomwe nagonjetsa
Dzanjalo ndilitama Potuluka m’mandamo.
Ndi mtima wachifundo, 6. Chikondano sichifera;
Mpakatu kwaŵalitsa Mbale wako udzamwona
Ku Dziko la Mulungu. Kwathu komwe; zipirira
189 50
Mpaka ukafikako.
1. TIKAGWIDWA ndi chisoni,
7. Leroli chisoni chokha,
Ikayendanso misozi,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Tsiku lija kungokondwa; 3. Ndi nkhondo ikaleka


Kweza maso osalira, Kwa Mlungu komweko,
Yesu akukondadi. Ndi ukapolo watha,
191 Udani wathanso;
Ndi zakuopsa zonse
1. NTCHITO yonse yakeyo
Ndi zosauka zii!
Yatha m’dzikoli linoli
Ndi mwayi wa kwa Mlungu
Mlendo wafikatuko
Udzoza mutu tho!
Pokocheza leroli.
’Tate, mwa kusunga kwanu
Timusiya mwana wanu.
’Tate, mwa kusunga kwanu
Timusiya mwana wanu. 193
2. Yathatu misoziyo 1. Nlokoma dziko langa!
Zobisika zonse mbee! Ndiyang’anirapo,
Aweruza bwinoko Ndilira ndi chikondi
Ndiye Wolungamayo. Poona dzinalo;
3. Komwe Mbusa kwawoko Pakumva mbiri yanu
Atengera nkhosa zonse, Mumtima muti duu!
Zake asungiramo Ndi moyo ndi mtendere
Zosaopa kanthu konse. Imalowetsamo.
4. Onse akulapawo 2. Mokhala mokhamokha
Ayang’ana mtanda wake; Mokondwa momwemo;
Aphunzira komweko Misozi yatha yonse,
Zonse za kukonda kwake. Angosekeramo;
5. Dothili kudothilo, Panyezimira ponse,
Pfumbili kupfumbi tere; Panyumba pati mbee!
Mpaka adzadzukanso Pamyala pakongola
Timusiya mumtendere. Yoyala ponsepo.
192 3. Makomo afanana
Ndi myala yoti mbuu!
1. MUMZINDA wa Mulungu
Ndi kristu wopambana
Moyera mulimo,
Aonekeramo;
Ndiye amathu omwe
Ndi mtanda woyeretsa
Olera ifewo;
Wopachikidwapo,
Mitima yathu yomwe
Amamlambira Mfumu
Ikondwereratu,
Namlemekezanso.
Nikhala nawo Mzinda
4. Kulibe gombe, Nyanja,
Wakukongolawu.
Kulibe nthawi ‘yi,
2. Akondwerera anthu
Alendo alandira
Zokoma zonsezi
Zoziziritsazi;
Za midzi ya padziko
Pa mwala wa muyaya
Lapansi lonseli;
Amanga nyumbayo,
Mtendere wake koma
Ndi omwe opambana
Wa Mzinda wathuwo
Adzakondweramo.
Upambanditsa zonse
5. Nlokoma dziko langa!
Zapansi pomwepo.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Kopita onsewo Iwo adatichimwira.


Mulungu awasankha, 3. Musatifikitsemo
Tifuna kunkako. Muli mayeserowo,
Ambuye, mutsogole Koma mutipulumutse.
Ku dziko komweko; Wanu ndi ufumuwo,
Tidzakuimbirani Mphamvu ndi ulemunso
M’ulemerero. Kufikira nthaŵi zonse.
194 196
1. NDIKONDWA kuganizirabe 1. Mtima wanga ndikonzera,
Za Dziko la Mulungu; Mbuye Yesu aitana;
Momwemo muli abwezitu Ati: “Mwana, tapemphera,
Okhala mumtendere. Ine sindidzakukana.”
Iwo salekana, iwo salekana, 2. Mbuye ndinu Mfumu yanga
Ayi salekana abwenzi omwewo. Yolemera ndi yamphamvu;
2. Komweko akhala Yesuyo Ndikapemphatu zambiri,
Mtetezi wa inedi Simundimanira kanthu.
Pakati pa ’womboledwawo; 3. Ndikabwera nd katundu
Sadzamva kuŵaŵanso. Wa zoipa zanga zonse;
Iwo asekera, iwo asekera, Mwazi wake wa Ambuye,
Inde asekera kumwona Yesuyo. Udzandiyeretsa konse.
3. Mulibe zoipa m’Dzikolo, 4. Mbuye ndinalema ine,
Nzokomazo zabwino; Mloŵe Inu m’mtima mwanga;
Ndi nthenda, imfa, misoziyi Mkhale m’mwemo mwini wake,
Kumwamba kulibenso. Mantha mwandichotsera ’ne.
Dziko labwinotu, Dziko labwinotu, 5. Ndine mlendo pansi pano,
Nawo mtenderewo, tikhumba ilotu. Mndilimbitse ndi chikondi;
4. Ndikonda kuganizirabe Bwenzi mundilondolere
Za Dziko la Mulungu, Njira pa ulendo wonse.
Za zonse zotikondweretsamo, 6. Mndidziŵitse ntchito yanga,
Nzosathanso chikondi. Mphamvu yake mundipatse;
Ife tikondwera, ife tikondwera, Mundilimbikitse m’mtima
M’mene tidzampenya Ambuye wathuyo. Ndikhale kwa Atate.
195 197
1. ’TATE wa Kumwambako, 1. PEMPHERA m’mbanda kucha,
Likayere Dzinalo, Pempheranso usana;
Udzetu Ufumu wanu; Pemphera m’dzulo momwe,
Chifuniro chanucho Pemphera ndi usiku.
51 Ndi mtima wonse idza,
Chichitike pansipa Tulutsanso zachabe;
Monga chachitika kwanu. M’nyumbamo ugwadire
2. Mutipatse leroli Ndi kukapempherabe.
E, chakudya chathuchi 2. Kumbuka ’bale ako
Tsiku n’tsiku tichilira. Ndi onse uŵakonda;
Mukhululukiredi Pemphera ’dani ako
Tchimo lathu, monga ’fe Amene akutonza.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Dzipempherere wekha M’wapulumutse ndi k’ŵachitira


Mulungu akusunge; Zomwe mufuna k’ŵapatsawo.
Tchulanso popemphera 6. Poloŵa ndi Inu
Dzinalo la Ambuye. M’chipinda cham’tseri,
3. Akakusoŵa malo Posonkhananso pamodzi,
Opempheramo m’tseri, Muyandikire nafe, Atate,
Komatu m’mtima mwako Mtibvomere, mtidalitsepo,
Mwaloŵatu zoyera;
Anazilonga m’mwemo
Ndi Mzimu Wakuyera; 199
Zolingirira zija 1. Bwenzi lathu ndiye Yesu
Kwa Mlungu zidzakwera. Atikonda ifetu;
4. Tilibe madalitso Zifunsiro zathu zonse
Akulingana n’lino Tipemphere mbuyathu.
Atate atipatsa, Mtima phee tisowa tonse,
Kupempherabe bwino. Zitibvuta chabeko,
Ukamvatu chisoni, Kaamba sitimanka konse
Kwa Mbuye kapemphera. Kupemphera Mlunguyo.
Adzakusangalatsa, 2. Tili nazo zotiyesa,
Pemphero adzamvera. Zitidetsa nkhawamu;
Tisadandaule chabe,
198 Timpemphere Mbuyathu.
1. POKUPEMPHERANI Kodi tikaona wina
Mundiphunzitse ’ne Timkhulupiriremo?
Ndi Mzimu wanu Woyera, Yesu adziwa bwino,
Ndikayanjane nanu, Atate, Timpemphere yekhayo.
Ndi kukulemekezani ’Nu
2. Mdikumbutse zomwe 3. Kodi tikulema nazo
Munandichitira Zotiwawa m’mtimamo?
Ndikakuyamikireni, Atipulumutsa Yesu,
Ndikweze Dzina lomwe angelo Timpemphere iyeyu.
Aliimbira Kumwambako. Kodi adathawa ‘balo?
3. Mndimvetse chisoni Pempheratu Bwenzilo;
Pakuululira Akusunga m’mkono mwake,
52 Udzapumuliramo.
Zochimwa zanga zambiri; 200
Mumtima ndi kupatsa mtendere
1. ZOKOMA ndithu nthaŵizi
Mutachotsera zoipazo
Kwa Mlungu zondifitsadi;
4. Chikondi, chimwemwe,
Kumpando wachifumuwo
Chifatso, chiletso,
Ndiuza zanga zonsezo.
Zipatso zonse za Mzimu
Pobvuta ine mtimamo
Mundibalitse, ndikafanane
Nditulapo pa Yesuyo;
Ndi Mbuyathu popempherapo.
Pakuyesedwa ndinkatu
5. Pakupempherera
Kwa Mbuye, sindikhala duu.
Anzanga ndi onse
Pakuyesedwa ndinkatu
Akusokera mumdima,
Kwa Mbuye, sindikhala duu.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

2. Zokoma inde nthaŵizi Ambuye yemwe,


Zotama Dzina lomweli Chitsime chomwe, njira yomwe
La Yesu, ndiwoonayo yokhulupirira;
Wopatsa dalo lonseli Tiyeni tonse, m’Mpingo ’modzi
Ndilakalaka Iyeyu tiziyenderana.
Wofera ine pansitu; 2. Atate yemwe anatuma Mpulumutsi
Pakuda nkhaŵa ine bii mmodzi
Nditchula Dzina lomweli, Kudzatifera kuti atiyanjanitse tonse,
Pakuda nkhaŵa ine bii Ndi Mzimu yemwe ayeretsa akumvera
Nditchula Dzina lomweli. onse;
3. Zokoma etu nthaŵizi Tiyeni tonse, m’Mpingo ’modzi
Ndicheza naye Mlungudi; tiziyenderana.
Koma kwathu m’Mwambamo 53
Kumwona ndi koposako. 3. Anatipatsa Mawu omwe olimbitsa
Pobvula ine thupili, mtima;
Ndiloŵa Dziko lakedi; Kumwamba komwe tinka ndi kulonda
Ndidzati nthaŵi yomweyo; njira yomwe.
“Tsalani bwino pansipo.” Tibalalikiranji ife akutsata Yesu?
Ndidzati nthaŵi yomweyo; Tiyeni tonse, mMpingo ’modzi
“Tsalani bwino pansipo.” tiziyenderana.
201 4. Satana apambana tikayamba kusiyana;
1. MTIDZUTSE, Mbuyetu, Tikayanjana, yemwe adzagonja ndi
Mtionekeremu: kuthaŵa;
Munene zakukmvekazi, Mbuyathu adzamthyola konse ndi
Timvere ifetu. kumlamulira.
Mtidzutse, Mbuyetu, Tiyeni tonse, m’Mpingo ’modzi
Mtipatse moyonso; tiziyenderana.
Mudzetu Mbuye, mudzetu, 5. Tiphatikane tonsefe okonda Yesu
Tidalitseni ’fe. Kristu;
2. Mtidzutse, Mbuyetu, Tisalekane pakugwira ntchito za
Tikweze Dzinali: Mbuyathu;
Tiuzireni Mpweyawo Tilimbitsane pakuyenda m’njira yonka
M’mitima yathuyi. kwathu.
3. Mtidzutse, Mbuyetu, Tiyeni tonse, m’Mpingo ’modzi
Timvere Mawudi; tiziyenderana.
Zoona zanu tonsefe 203
Tikhulupire ’zi. 1. MBUYE, Mpingo wanu usauka
4. Mtidzutse, Mbuyetu, kwakukuludi;
Mthirenso moyowo; Kale lija munatsitsa Mzimu wanu
Ulemu ngwanu nokha ’Nu, Wakuyera;
Dalitso nlathulo. Lero linonso muchite, ulimbike
202 Mpingo wanu.
1. AKRISTU ndi abale, tiziyenderana 2. Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu
tonse, wachifundodi;
Mulungu mmodzi tili naye, ndi Mutipatse Mzimu wanu tsopanoli,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

tere lino; 5. Pakufika tsidya lija,


Tikakhale ndi chimwemwe kuti tili Zotibvuta zonse phe!
mbike ndithu. Mfumu yathu yopambana
3. A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira Idzatikondwetsadi.
’balewo 6. Nthaŵi yina adzadzuka
Adasokerera kale ndi zoipa zapa Ogonera m’mandamo,
dziko. Kuthaŵatu mphamvu zonse
Muwabwezerenso kwanu kuti akakhale Zotibvuta pansipa.
mommo. 205
4. Ndi chikondi mtithandize kuigwira
1. TADZUKA mzimu wanga’we
nkhondoyi;
Ugwire ntchito zakozi;
Mwa kulema ndi kulimba
mutipempherere 54
ife, Kukondwa ukutengedi,
Kuti tilimbane naye Satanayo, Pemphero ulikwezedi.
osamwopa. Pemphero, pemphero,
5. Pakubweradi Woyesa tidzamlaka Pemphero ulikwezedi
ifetu; Pemphero, pemphero,
Angelonso adzabwera kutithandizira ife, Pemphero ulikwezedi.
Kuti tilimbike ife ndi kumchotsa 2. E, nthaŵi ya mamaŵayi
m’mtima mwathu. Umtamandire Mbuyeyo,
6. Pa la Mulungu tibwera kulandira Nuyese lero ngatitu
zidazo; Tsiku lakumalizalo.
Mphamvu yanu ndi chikondi 3. Munkhani zako zonsetu
zititsogolere Unene molungamadi,
ife; Nudziŵe kuti Mbuyako
Machitidwe ndi mkhalidwe zikokere ena Adziŵa zachinsinsizi.
kwanu. 4. Pa tsikuli, Mbuyanga ’Nu,
Munditsogolere m’njiramo;
204 Ulemerero wanuwo
1. AULENDO amayenda Undilimbitse monsetu.
Muusiku wo’psyawo, 5. Timlemekeze Mlunguyu
Namaimba nyimbo zawo Wa madalitso onsewo;
Kunka kwawo m’Mwambamo. Timlemekeze tonsefe,
2. Kuunika kuoneka Atate, Mwana, Mzimunso.
Koingitsa mdimawu;
Mbale amakondwerera, 206
Osaopa konse ’yi. 1. KRISTU wakuyeratu,
3. Mlugu amaunikira Kristu wakuŵalayo,
Anthu ake onsewo, Wolungama mdzuketu,
Namachotsa mantha omwe, Muingitse mdimawo.
Nayeretsa m’njira mbee! Dzuŵa lathu m’Mwambamo
4. Anthu osaŵerengeka M’wale m’kati m’mtimamo.
Amtamira onsewa, 2. Konse kuli mdima bii
Nagonjetsa zosautsa Kosakhala Inutu;
Pomtamira Mbuyeyo. Nlosakondwa tsikuli
Mosaŵala Inu ’mu.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Ndionetu m’katimo Komatu mukhalitse ndinetu.


Mwakuŵala kwanuko. 4. E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
3. Mudze, mloŵe m’mtimamu, Ndi mphamvu yanu yokha ndisungika;
Mchotse monse mdima bii; Mukatsogola ndidzadikha m’mtima;
Mdzaze ndi kuyeraku, 55
Mchotse zosamverazi; Usiku, msana, mkhale ndinetu.
Ndi kuyera kwanuku 5. Adani sindiopa mukalipo
Ndikaone bwinotu. Muletse tsoka ndi chisoni chino;
207 Ikadza imfa n’dzalimbika m’mtima;
1. AMBUYE munapatsa tsiku M’moyo ndi m’imfa mkhale ndinetu.
Limene langopitali, 209
M’mamaŵa nyimbo zathu zomwezo 1. ATATE ndiyamika, mwandisamalira
Mukhale nafe nthaŵiyi leroli;
Mukhale, mukhale, Mulungu wandikonda, mndisungenso
Mukhale nafe nthaŵiyi; m’mdima muno bii.
Mukhale, mukhale, 2. Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za
Mukhale nafe nthaŵiyi. Kumwambako;
2. Tipempha kuti Mpingo wanu Zoganizira zoipitsa m’mtima
Ukhale ponse m’dzikoli; muchotseremo.
Mumdima monse muŵaletu, 3. Zochimwa za usana uno
Kuŵala kwanu kudzedi. mndikhululukire
3. M’maiko monse, zisi zomwezo, ’ne;
Kuŵala kumafikanso; Mtendere wanu muloŵetse m’mtima
Kupempha sikuleka konse ndikagone phee.
Kuyamikira Yesuyo. 4. Mundilimbitse ndikayese manda
4. Pogona ife, amadzuka ngati mphasayi,
Abale akutaliwo; Nditagonamo ndikadzuke tsiku
Panthaŵi yonse anthu ena lomalizalo.
Alemekeza Mbuyeyo. 5. Tiyamike Mlungu wotipatsa
5. Ufumu wanu, Mbuye Yesu, zachifundozi,
Ukhale nthaŵi zonsedi; Amyamikire onse a Kumwamba ndi
Magulu onse adzagonje, apansipa.
Naloŵe m’njira mwanumu.
210
208 1. DZUŴA lapitira,
1. MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa, Wadza mdimawo,
Wagwa usiku, bwenzi lindisoŵa; Mthunzi wamadzulo
Ndilibe wina wakundithandiza, Wagwa m’mwambamo.
Wamphamvu ndinu, mkhale ndinetu. 2. M’mwambamo nyenyezi
2. Kamoyo kanga katha lero lino, Zithwanima mbee;
Zidzachokanso zinthuzo za dziko; Zonse zili m’tulo
Zimasinthika zonse zooneka, Pansi pali duu.
Simusinthika, mkhale ndinutu. 3. Yesu mutipatse
3. Koma kalelo mnakhalitsa pano, Tulo toti phee;
Mukhale ndine, msandichokerenso, Ndi mdalitso wanu
Sin’pempha kuti Mbuye mungotsotse, Mndigonetse ’ne

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

4. Mpatse ana ’ng’ono Odwala anagona duu;


Alotemo mbee; Opwetekedwa nthendazo
Anthu aulendo Munachiritsa Inutu.
Msungesungebe. 2. Tsopano lino kwada bii,
5. Mutonthoze mtima Nafenso timva m’mtimamo;
Wopwetekawo; Simuoneka, komatu
Akutsata tchimo Tidziŵa muli nafedi.
Mletse onsewo. 3. Wopulumutsa mudzetu;
6. Wonsewu usiku Adwala ena m’mtima bii,
Andisunge ’ne Ena sakukondani ’Nu,
Amithenga anu Ena sasamalira ’yi.
Akuyera mbee. 4. Ndi ena sanamvera ’yi
7. Ndidzukanso m’maŵa, Enanso alemedwatu,
Kucha koti mbuu, Zoopsya nazo tifadi;
Ndiyeretu mtima Mukadza tidzaposatu.
M’maso mwanumo. 5. Wopulumutsa, Inunso
8. Titamadi ’Tate, Munasauka kalelo;
Mwana wakeyo, Muona zoda m’mtimamo
Mzimu Woyeranso, Tibisa ndi manyaziwo.
Nthaŵinthaŵizo. 6. Mutichiritse ifenso,
211 Mutiphunzitse zanuzi;
Timve tsopano mawuwo
1. DZUŴA lapita,
Ochiza nthenda yathuyi.
Dzuŵa lapita,
Mlungu, mutigonetse phee. 213
2. Mdima wafika, 1. MPULUMUTSI, tikagona
Mdima wafika Mtidalitse m’mtimamo;
Mutisunge tonse bwino. Tingolapa zakuipa,
3. Tibvomereze, Muzichotse zonsezo.
Tibvomereze Kukadetsa bii usiku,
Zakuchimwa zathu zonse. Inu mutipenya ’fe;
4. Mkhululukire, Simulema, simugona;
Mkhululukire Anthu anu msungabe.
Zoipa zathu zonse. 2. Atipsinjadi masoka,
5. Lero tigone, Mibvi iponyekatu;
Lero tigone, Atisungadi angelo,
Tigonemo mumtendere. Moyo mutipatsa ’Nu.
6. Ndife ananu, Ngatitu usiku uno
Ndife ananu, Ikabwera imfayo,
’Tate Mlungu wotikonda. Mtiukitse m’maŵa kwanu,
7. Aleluya! Mpatsenso zoyerazo.
56 214
Aleluya! 1. MULUNGU wanga, Dzuŵatu
Aleluya, Aleluya! La mtima wanga ndinudi;
212 Palibe mdima ngatitu
1. MADZULO aja kalelo Mukaŵalira inedi.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

2. Muchotse zonse zoti bii Munapuma tsikulo;


Zobisa nkhope yanuyo; Tipumadi ifenso.
Mudzazetu mtimangawo Mommo tilandiratu
Ndi kuunika kwanuko. Zopumitsa mtimawu.
3. Madzulo ano mkhaletu 4. Yesu munadzukanso
Pafupi ndine, Yesudi; M’manda lero lomwetu;
Ndisanagone tuloto, Ntchito munayambayo
Ndilingalira Inudi. Yakudzutsa anthu ’fe,
4. Kapena wina leroli Kuti ndi mitimayi
Wasokerera m’njirayi Tigwirebe ntchitozi.
Ya Inu Mbuye, mbwezetu, 217
Mumpulumutse iyedi.
1. AMBUYE, tasonkhana
215 Tsiku lino lopatula,
1. LERO mwatipatsa moyo, Tidzapembedza Inu
Wadza mdima, kwada bii; Tsiku lino lopatula.
Mtigonetsetu usiku, Bwenzilo lakufatsa,
Mchotse zakuipazi. Mbweretu kutipatsa
Yesu mutisunga ife; Mtima wakumvesetsa
Tidzakhulupirabe. Tsiku lino lopatula.
Yesu mutisunga ife; 2. Sitinanyalanyaza
Tidzakhulupirabe. Tsiku lino lopatula.
2. Ndife anthu aulendo, Tigwadirira m’mantha
Tili ndi adaniwo; Tsiku lino lopatula.
M’manja mwanu mtigonetse, Mbwezetu maganizo,
Mtichotsere manthawo. Mtimvetse malangizo;
Ndipo pakumuka ife, Tchimo mufafanize
Kwanu tidzapumabe. Tsiku lino lopatula.
Ndipo pakumuka ife, 3. Timvere Mawu anu
Kwanu tidzapumabe. Tsiku lino lopatula
216 Muŵadalitse ndithu
Tsiku lino lopatula.
1. KWACHA lero kwati mbee,
Mtiperekeze kwathu,
Tsiku la Mulunguli;
Msunge mitima yathu;
Dzuŵa liŵaliradi
Mpatse chisomo chanu
Thambo ndi zapansipa
Tsiku lino lopatula.
Upumira mpweyawu
57 218
Wa Mulungu konseku. 1. DZUŴA la Mulungu
2. M’nyumba yanu, Mlungu, ’yi Ladzatu labwino;
Tisonkhana teretu, Ndi chimwemwe ife
Ndi mitundu yonseyi Tiliona lero.
Tikulambireni ’Nu: Lithaŵitsa nkhaŵa,
Yesu Mbuye wathuyo Lichotsanso mantha
Ndiye Mfumu ponsepo. Ndimo m’mtima mwathu
3. Inu Mlungu kalelo Likhalitsa bata.
Mutalenga zonsezi 2. Tikondwera kuti

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Tipumula lero; Timdikirabe.


Tazileka ntchito 221
Kuti tipemphere.
1. ANTCHITO a Mulungu ’nu
Koma ntchito zathu
Olinda m’nyumba mwakemo.
Za palero lino
Myamike, muimbiretu
Nzakumvera Yesu,
Mlungu Mbuye wathuyo.
Kumlandira bwino.
2. Mugwade pansi m’nyumbayo
219 Mpembedze nonse Mlungutu;
1. NDI lokoma m’Mwambamo, Mugadamire m’mwambamo.
Mbuye, Bwalo lanulo; Mtamande Mbuye wanutu.
Ndi mwabwino muli ’Nu 3. Yehova adalitse ’nu,
Dziko losachimwali; Ndiye wachifundocho,
Mtima wana wonsewu Asunge moyo wanuwu;
Umakhumba m’Mwambamo Amtame anthu onsewo.
Nkhope ya Mbuyathuyu, 222
Mlungu wa chisomoyo.
1. KWEZANI mitu yanuyo,
2. Zimbalame zonsezi
Zipata zamuyaya,
Zimayamikira ’Nu;
Ikaloŵemo Mfumu ya
Anthu amakondwanso
Ulemereroyo!
Okhumbira m’Mwambamo;
Amfumu awa ndaniko?
Njiŵa yosapumayo
Ambuye ndiyeyo,
Inafika m’chombocho;
Mulungu wogonjetsa onse,
Okhulupirira ’Nu
Wolimba mphamvu njo!
Amapuma kwanuno.
Mulungu wogonjetsa onse,
3. Anthu opembedzawo
Wolimba mphamvu njo!
Amakondwa m’mtimamo;
2. Tatsegukani inutu,
Munapatsa madzitu,
Zitseko zosathera,
Munagwetsa manawo;
Amfumu akumwambako
Mumakoma mtimatu
Aloŵe mwanumo.
Tidzayamikiratu,
Amfumu awa ndaniko
Pachimpando chanucho
Wolemereroyo?
Mkhale Mfumu yathudi.
Mulungu wa makamu ndiye,
220 Wolemereroyo.
58 Mulungu wa makamu ndiye,
1. YESU mkhale nafe Wolemereroyo.
Nthaŵi yomweyi, Aleluya, aleluya, aleluya, aleluya,
Kuti mphamvu zanu aleluya.
Tilandirezi. Amen, amen, amen.
2. Mzimu Wakuyera 223
Mutipatsetu, 1. MLUNGU ali muno,
Mtima wathu wonse Tonse timgwadire,
Usakhale duu. Mantha omwe timchitire;
3. Moyo watsopano Ali mukachitsi,
Ulimbitse ’fe, Tonse tili chete,
Mlungu wathu yemwe

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Ndi ulemu timpembedze; Alonjezetsa lero


Ndiye yekha Mlungu wathu Kutsata Mbuye onse
Atipulumutsa, M’ŵathangatire iwo
Tidzamlemekeza. Asabwerere konse.
2. Mwini madalitso, 2. Tsopano alandira
Mndikonzere m’mtima, Chizindikiro chanu
Mbuye, ndingokhulupira. Munachiika ndinu
M’Mwambamo angelo Cha Ubatizo wanu
Agwadira inu, Mulembe dzina lanu
Ife tigonjanso kuno; M’mitima mwa onsewa;
Mpingo wonse uchiitse M’ŵabatizenso Mbuye,
Chifuniro chanu. Ndi Mzimu Wakuyera.
Ponse pansi pano. 3. Muŵalimbitse onse
3. Yesu Mbuye wanga, Akhazikike m’mtima,
M’khale m’mtima mwanga, Akhale chikhalire
Ndiwotu kachisi wanu. Oyera ndi olimba;
Ikafika imfa, Mutithandize tonse
Mundisunge kwanu A Mpingo wa Mulungu
Kuli inu ndi angelo. Tikhale oyenera
Moyo wanga ulimbike Ndi okondana ndithu.
Kufikira ine 226
Ndidzakupenyani.
1. MONGA zomera zonsezo
224 Zikula ponsepo,
1. MTSINJE woyerawo Mulungu mumeretsazo,
Wotuluka m’nyumbayo Momwemo anawo.
Ya Mlungu wathuyo 2. Munali mwana, Yesu ’Nu
Uyeretse tonsefe. Wamng’ono kalelo,
Ife tifikeko Ndi munakula m’msinkhu ndi
Tibatizidweko, Kutama ’Tatewo.
Tiyeretsedwedi 3. Ndi ife tinga, mbewuzo
Ndi Ambuye leroli. Zomera m’mundawo;
59 Mumtima mutidyetsedi,
2. Mwa anthu onsewo Tikule bwinomo;
Umayenda mtsinjewu, 4. Ndi kutsukidwa m’mwazimo
Nuŵachiritsadi Mumtima mwathu mbee,
Okhulupirirawo. Tionetsedwe konseko
3. Tikondwereratu A Mlungu ana ’ke.
Pakumvera Yesuyo, 227
Abwere onsewo 1. USIKU uja kalelo
Ndi kuloŵa m’mtsinjewu. Anampereka Yesuyo,
225 Usiku womwe m’manja mbuu
1. ATATE, muwapenya ’Natenga mkate Iyeyo.
Anzathu ali pano, 2. Natamandira Mlunguyo
Abvomereza Inu Wolamulira pansipa,
Ambuye Mfumu yawo; Natema mkate, natitu

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Kwa omwe anatsatawo; Ndi nkhope yanu dwii,


3. “Ndi thupi lopatsidwali Thukuta la pamphumilo
La Ine, mtenge, mudye, ndi La myazi yanuyi.
Muchite ichi nonsenu, 4. Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
Ndi chikumbutso changatu.” Ndiona m’menemo,
4. Ndiponso m’manja chikhocho A Yesu kufa kwanuko,
’Nakweza, natamandamo Kuthetsa imfazo.
Mulungu, mtima wake mya, 5. Pamene padzakhalapo
Nanena mawu omwewa: Milomo yanga phee,
5. “Chikho cha mwazi wangachi Mukadza ndi Ufumunso,
Chitsuka mtima woda bii, Mukumbukire ’ne.
Cha mapangano omwewo 230
Chisomo cha Kumwambako.
1. MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
6. “Chikho cha mwazi wangachi
Mkate ndi chikhocho cha Mbuyathu.
Chitsuka mtima woda bii,
2. Khristu ndi mwini moyo wathuwu,
Cha mapangano omwewo
Pamtanda anafera ifetu.
Chisomo cha Kumwambako.
3. Anatifera nsembe Iyeyo,
228 Ndiye Wansembe wake Iyenso.
1. SINDILI woyenera ’ne, 4. Imfa ndi mdima zinathaŵa zii!
Ambuye, kudzamo; Ndipo chisomo chikuŵala mbuu.
Munene mawu, ndimvebe 5. Tadzanitu, okhulupiradi,
Okondweretsawo. Talandirani zachinsinsizi.
2. Sindili woyenera ’ne, 6. Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
Mumtima mwanga zi; Moyo wosatha atipatsa ’fe.
Munene, ndikachiradi, 7. Ndiye wodyetsa anthu omwewo,
Ndilibe moyo ’yi. Napatsa mwazi, moyo wakewo.
60 8. Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ’Nu,
3. Sindili woyenera ’ne; Tsopano mkhalebe ndi ifetu.
Pamtanda panupo 231
Munamaliza mlandu phe 1. MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
Ndi mwazi wanuwo. Mommuno ndizikhudza zanu phee,
4. Ndilaŵako tsopanoli Mommuno zachinsinsi zanu mbuu,
Zakudya zanuzo; Mwa Inu mtima ndipumirabe.
Mudzaze mtima wanga ndi 2. Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
Kukonda kwanuko. Mommuno vinyo wakumwambako,
229 Mommuno zolemera zanga du,
1. MONGATU mawu anuwo, Chisomo chanu ndidzalaŵanso.
Ndi Mtima chete phee, 3. Ndilibe wondithangata ‘ne ’yi,
Mbuyanga kufa kwanuko Ndilibe wina wondisunga ’ne;
Ndikumbukire ’ne. Zikwaniratu mphamvu zanuzi,
2. Chakudya chakumwambachi Ine, Ambuye, mphamvu nzanudi.
Ndi thupi lanudi; 4. Tsopano nthaŵi yake phwandoli,
Chikho cha chipanganochi Loyala ili m’gome mwanumu;
Ncha mwazi wanuwo. Ndidye ndimwere zakukomazi,
3. Getsemane ndionako Ndiyanjanabe nanu, Mbuyathu.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

5. Chakudya ichi chidzapita du, Mukhaletu pafupi,


Chizindikitsa za Kumwambazo; Mundithangate ’Nu.
Zosapitazo tidzalaŵatu, 3. A! Yesu mwapangana
Za Yesu mwini wakukondako. Ndi anthu anuwo
6. Tikadya phwando zaka zonsezi, Adzakhala ndinu
Ndipo zakudya zimalozatu Ku Dziko lanulo;
Kuphwando lija la Kumwambako, Inenso ndapangana
Komwe tidzadya kwa Mulungutu. Ndisabwerere ’yi;
232 Mndipatse mphamvu yanu
Ambuye ndinudi.
1. NDIMAMVA njala, Yesu,
4. Mundionetse, Yesu,
Ya mtima wakusoŵa;
Mapazi anuwo,
Mdidyetse ngati mana
Ndidzapondera awa
Anagwa m’chipululu.
Munjira monsemo;
2. Ndimamva ludzu, Yesu,
Ndithangateni ine
61 Ndisalefuke ’yi;
Muloŵe mwanga lero; Mundilandire m’Mwamba
Mndimwetse ngati madzi Ndikamwaliradi.
Anatuluka m’mwala.
3. Ndi mkate wanu, Yesu, 234
Ndi thupi lobvulala, 1. MUNDIMVERE, Mbuye wanga
Mndilimbikitse, Mbuye Nkana ine ndimalakwa,
Mundikhutitse mtima. Koma ndinu moyo wanga;
4. Mwa chikho chokumbutsa Mbuye, mkhale ndine.
Chikondi chopambana, 2. Ndine mlendo pansi pano,
Mndipatse moyo wanu, Msanditaye m’dzanja lanu,
Ndikayanjane nanu. Mundisunge mwana wanu;
5. Mndidyetse m’chipululu Mbuye, mkhale ndine.
M’ulendo wanga wonse; 3. Munafera ine kale
Mdimwetse, ndipirire Kuti mukandimasule,
Osalefuka konse. Lero lino mndinyamule;
Mbuye, mkhale ndine.
233 4. Mundidzaze ndi chikondi,
1. A!YESU, ndapangana Mndiyeretse m’mtima monse,
Kutumikira ’Nu Chifuniro changa mthyole;
Ndi moyo wanga wonse, Mbuye, mkhale ndine.
Mbuyanga ndinutu; 5. Imfa ikandifikira,
Mukhaletu pafupi Inu ndidzakangamira
Masiku onsewo, Ndikaloŵa ine m’mdima,
Sindidzaopa konse, Mbuye, mkhale ndine.
Mutsogolereko.
2. Ndikufuna kumva Inu, 235
E, Mawu anuwo, 1. ANU Mbuye ndifetu!
Ndisamve za satana Mutimvere kwanuko;
Zonyenga zakezo; Anu tikhalirebe
Adani anga onse Kuno ndi Kumwambako.
Andizingiratu; 2. Anu Mbuye ndifetu!

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Mwanu tipumiredi; Njira yakuunika.


Ndinu Mbale wathu ’fe, 2. Mbiri ya Hananiyayo
Mutusunge nthaŵizi. Inali yodabwizatu;
3. Anu Mbuye ndifetu! Ananyengatu Peturo;
‘Dikireni tonsefe; “Zopereka ndinapereka.”
Moyo ndinu, n’choona, 3. Ife tonse tichenjere
M’njiramo tiyendebe. Tingadzachite zomwezo:
4. Anu Mbuye ndifetu! Tisaname ndi kunena:
Ndife nkhosa zanuzi; “Zopereka ndinapereka.”
62 4. Mulungu akondadi leroli
Mwanu tibisalemu, Wopereka mokondwera;
Mwanu mosungikadi. Tikapereka motero
5. Anu Mbuye ndifetu! Tidzalandira dalitso.
Tsogolani nthaŵizo; 238
Mtiyendetse m’moyomu 1. MBUYE wathu, mutipatsa
Kunkabe Kumwambako. Zonse tili nazozo,
236 Mutikomeratu mtima
1. AMBUYE, Mwini zonsezi, Osaleka konseko,
Ulemu tiperekadi; Mutikonda, mutisunga,
Chikondi tionetsanji? Mutisamalira ’fe.
Mwapatsatu. 2. Dzuŵa, madzi, kudya, mpweya,
2. Dzuŵa ndi mvula yonseyo Moyo, zonse nzanuzi,
Ndi mame mwatipatsanso, Si za ife, nzaulere,
Masika ’dzera kwanuko; Tingozilandiradi;
Mwapatsatu. Zifumira kwa Aate
3. Mwapatsa Mwana wanu, ndi Wotikondakondatu.
Mwapulumutsa dzikoli; 3. Monga tilandira, Mbuye,
E, zaulere zonsezi Mtiphunzitse tonsefe
Mwapatsatu. Tipere chuma chathu
4. Tibwezeretu bwanjiko Ndi kusangalalatu;
Ziperewera zathuzi; Zakukhala m’manja mwathu
Ndi moyo tili nawowo Tiziyese nzanudi.
Mwapatsatu. 4. Tikhaletu nawo, Mbuye,
5. Ambuye zathu zonsezi Mtima wosauma ’yi
Kwa Inu tibwezeredi; Ndi wofatsa ndi wabwino
Tingopereka zanuzi, Ndi woyerayeradi,
Mwapatsatu. Kuti tiyenere Dzina
La Mbuyathu Yesuyo.
237 5. Tisaiwalire ’bale
1. PETURO ’nafunsa Hananiya: Athu osadziŵa ’Nu,
“Zopereka zili kuti?” Akulira ndi odwala
Hananiya ananena: Tiŵapemphereratu;
“Zopereka ndinapereka.” Titsanzenso Mbuye Yesu
Munthu aganize Ndi k’ŵathangatira ’wo.
Zimene anachita Hananiya 6. Dalitseni, Mbuye, zonse
Munthu aganize

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Zomwe taperekazi, Yake ya Wokondayo,


Mzilandire, nsembe yathu, Ang’ono akwezanso mawu
Mziyeretse Inudi Poimba nyimbo zawozo.
63 4. Ufumu wake udalitsa
Ndi mitima yathu yonse Osauka onsewo;
Tikuyamikirani. Otopa amapuma chete,
Magoli amathyoka thyo!
239 5. Zolengedwa zonse zidze
1. POLENGA dzikoli Kugwadira Mfumu yathu,
Pakumva Inudi, Amlemekeze akumwamba,
Kwayeratu; Tiimbe pansipa; Amen.
Mumve pempheroli,
Ndipo pamenepo 241
Palibe mawuwo, 1. ANTHU akum’maŵa
Muŵaletu. Nanka msangako,
2. Inu wakudzatu Nzeru ’nali nazo,
Kuŵachiritsadi Nafatsansowo;
Anthendawo, Nanka kuli Mwana
Kupatsa moyowo, Anabadwayo;
Kuona m’masomo, Anatsogozedwa
Pa anthu onsewo Ndi nyenyeziyo.
Muŵaletu. 2. Anapeza Mwana
3. Mzimu woonadi Ali m’kholamo,
Ndi wachikondicho, Nagwadira Iwo
Idzanitu; Mbuye wawoyo;
Muunikirepo Anthu onse omwe
Pali zamdimazo, Ali pansipa,
Pa dziko ponsepo Azitsata Mbuye
Muŵaletu. Ndi nyenyeziyo.
4. Inu atatuwo, 3. Mu ulemerero,
Wodala Mlunguyo, Yesu m’Mwambamo
Timveretu; Muli eni ake;
Pa dziko ponsepo Anthu onsewo
Muchotse mdimawo, Osadziŵa konse,
Mutume Mawuwo, Akutalinso,
Muŵaletu. Akokedwe iwo
Ndi nyenyeziyo.
240 4. Akukhala kunja,
1. ADZAPAMBANA Yesu ponse Osokeranso,
Pakuyenda dzuŵalo; M’ŵaŵalire Mbuye,
Adzamverabe namgwadira Asagone’wo;
Pa dziko lonse pansipa. Amumdima omwe,
2. Sadzalekeza kuyamika Olemedwanso,
Ndi kuimbaimbabe; Mtsogoleri wawo
Adzapemphera nsiku zonse Ndi nyenyeziyo.
Natchula Dzina lakelo. 5. Paulendo wathu
3. Pomveka konsekonse mbiri

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

64 Mitima yanu yonseyo iyeretsedwe


Tili pansipa, mbuu!
Muŵalire tonse 4. Tsatani Mbuye Yesuyo ndi
Tili m’njiramo; mtanda wakewo;
Mutitsogolere Mlaliketu Uthenga kwa anthu
Anthu tonsefe, onsewo.
Mutifitse tonse 5. Musamaopa kanthu ’yi tamani
Ndi nyenyeziyo. Yesuyo;
Kaimbireni nyimboyi ndi
mphamvu zonse.
242 6. Zipata zatsegudwa mbee! za
1. Timva mawu omwewo m’dziko monsemo;
Atitu: Yesuyo Ambuye wapambanatu ndi
Mpulumutsi ndiyedi, mtanda wakewo.
Yesuyo, Yesuyo.
Pita m’midzi monsemo, 244
Dziko lonse limvetu, 1. PAMAIKO pali mdima,
Pita iwe konseko, Penya mtima chetetu,
Mveratu mbuyeyo. Leroli malonjezano
2. IMbadi za iyeyo, Angokwaniridwatu.
Amvetu anthuwo Kondwerani, kondwerani,
Kuti Yesu ‘nafadi Yesu mulitsetu.
Kalelo, kalelo. 2. Adze amitundu yonse,
Atikonda ifetu, Adze akutaliwo;
Natifera indedi Ayang’ane mtanda uja
Kuchotsera chimoli, Woti nji paphiripo
Yesuyo, Yesuyo. Mbiri yanu, mbiri yanu
3. Bukitsani mawunso Ibukitse ponsepo.
Konseko, konseko! 3. Ponse padakhala mdima
Kaitane anthuwo Pakaŵale dzuŵali;
Ponsepo, ponsepo. Kumalire konsekonse
Kodi wina samvatu? Muthaŵitse mdima bii!
Pitako, pitako ‘we; Mpulumutsi, Mpulumutsi,
Angofuna onsewo Muyeretse zonsezi.
Yesuyo, yesuyo. 4. Ibukitse mbiri yanu,
Ifikire konseko,
243 Iŵagwire anthu mtima,
1. ZIPATA zachitsulo zitseguke Iŵathyole m’katimo
zonse mbee! Mphamvu yanu, mphamvu yanu,
Ambuye wa Kumwambako aloŵe Idziŵike konseko.
momwemo.
2. Mbendera yake ikupiza 245
m’mlengalengamo, 1. MBWERE Mlungu Mbuye
Kufana ndi nyenyezi younika wathu,
m’mdimamo. Msunge zakuonazo,
3. Ankondo a Mulungu ’nu, Mudalitse anthu onse
Yendani m’njiramo, Ndi chifumu chanucho.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

2. MMbwere Yesu Mwini moyo, Nagonjera konseko.


Ukuletu ’lemuwo; 247
Gonjetsani anthu onse,
1. Anthu ali m’mdima akuitanitsa
Mpatsenso mtenderewo.
Unikani! Unikani!
3. Mbwere Mzimu Wakuyera,
Alikumwazika mungawalanditse,
Mutitsitsimutseko;
Unikani! Unikani!
Muthaŵitse mdima wonse,
Muŵalitse m’mtimamo.
Tumizani kuunikako
4. Anthu onse taukani,
Kuoneketu kwa onsewo;
Imbirani Mlunguyo;
Tumizani kuunikako,
Zichuluke zomtamanda
Nthawi zonsedi kuwaletu.
Pansi ndi Kumwambako.
246 2. Tamva aku makedonyako atero,
1. ANYAMATA a Mulungu, Unikani! Unikani!
Muzigwira nkhondoyo, Tititu, Mbuye tizinka komweko,
Mumenyane ndi Satana Unikani! Unikani!
Mzimu wakunyengayo. 3. Tisaleme pakuchita zabwinozi,
2. Komwe asauka anthu Unikani! Unikani!
Akukhala m’mdimamo Tidziunjikire ngale
65 zakumwamba,
Osadziŵa Mpulumutsi, Unikani! Unikani!
Phunzitsani konseko. 248
3. Pomangidwa anthu nayo 1. MUNENE Mbuye, ’nenetu,
M’yambo yoipitsayo, Nditsanze mawu anuwo;
Pomwe amaopa chabe, Munandifuna Inetu,
Masulani golilo. Ine ndifune zanuzo.
4. Walitsani nyali yanu 2. Nditsogolere m’njirayi
Ikachotse mdima bii! Nkhosazo zisokerazo;
Mpaka ikainga zonse Ndidyetse Mbuye, zanuzi
Zosautsa m’dzikoli Zimene zifa njalayo.
5. Akutopa ndi ofoka 3. Ndilimbikitse, Mbuye, nji!
M’ŵatonthoze mtima phee! Pamwalapo ndiimebe;
Osokera, onyozeka Onse alibe mphamvu ’yi
Muŵafunefunebe. Omwe ndithangate ’ne.
6. Achisoni obvutidwa, 4. Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
M’ŵathandize msangatu; Ndidziŵitse nzeru zanuzo;
Zosautsa zawo zonse Munole mibvi yangayi,
Yesu azichotsadi. Ipyole yonse m’mtimamo.
7. Anyamata limbikani, 5. Ndipumulire panupo,
Gwiranitu nkhondoyi; Ndinene motonthoza phe!
Yes salephera mwini, Ndi mawu opumitsawo
Sitiiŵalira ’yi. Olema ndikanenebe.
8. Isaleke ntchito yake 6. Ambuye, ndi chikondi tho!
Mpaka anthu onsewo Mudzaze mtima wangawu;
Alambira Mfumu yathu, Ndinene zachikondicho,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Ndiyamikire monsemu. Odza kuphunzira ’mu,


7. Ndichitireni, Mbuye ’ne, Ndi antchito anu omwe
Monse mufuna mwanumo; Odza k’ŵaphunzitsa ’mu.
Kumwamba tionane mbee, 3. Tiyamike Mlungu ’Tate,
Maso ndi maso kwanuko. Tiyamike Mwanayo,
249 Tiyamike Mzimu wake;
Onse omwe Mmodzitu,
1. MULUNGU wa Kumwamba
Waulemerero wonse
bwera kunoku
Ndi wamphamvu ponsepo.
Ndi mtima wokondwera kuloŵa
m’nyumbayi; 251
Chifukwa cha zabwino 1. ANAKWATIRA kale
mwatichitirazi Pa Eden pajapo;
Tikukuyamikirani leroli. Ulipo lero lino
Inde, tikuyamikani, Atate, leroli, Mdalitso womwewo.
Mwatimangira ’fe kuno kachisi 2. Aŵiri aimamu,
wanuyu! Mwamuna ndi mkaziyu;
Ndi ulemerero wanu mudzaze O! Mzimu Wakuyera,
m’nyumbayi; Mdalitso mpatsetu.
Muyeretse, mudalitse munomu. 3. Mulunzanitse awa,
2. Tikondwa tonse ndi Atate, leroli;
kukuthokozani ’Nu Munakwatits’ Adamu
Poyamba kupemphera ndi Ndi Hava kalelo.
kuimbiramu; 4. Mukhale nawo, Yesu,
Mommuno nsiku zonse mukhale Mongatu kalelo
nafetu, Ukwati mnadalitsa
Monga ndi angelo anu Pa Kana pajapo.
m’Mwambamo. 5. M’ŵasunge, m’ŵayendetse
3. Ikhale ngati nyali yoŵala Munjira yanuyo,
nyumbayi, Akhale ndi kudala
Yakutsogoza onse ophunthwa Pabanja pawopo.
m’mdima bii; 252
Akunja ndi Akristu
1. YEHOVA Mlungu wathu,
m’ŵapulumutse ndi
Amene mumapatsa
66 Zipatso za chikondi
Kuunika kotuluka munomu. Polenga anthu anu,
250 Mupatse awa ‘ŵiri
1. KRISTU ndiye Mwala wathu, Mitima yokondwetsa,
Kristu timangirapo; Yofana m’munda muja
Wosankhidwa ndi Mulungu, Munayendamo kale.
Atimange tonsefe; 3. Mbuyathu wokondedwa,
Iye ndi Mthandizi wathu, Pokhala m’dziko muno
Timkhulupirira ’Ye Munadza ku ukwati,
2. Mudalitse nyumba yathu; Naŵadalitsa onse;
Mbuye, nthaŵi zonsetu Ukwatiwu mukonze,
Muthandize anthu onse Mukhale nafe pano;

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Iwowa m’ŵadalitse Mtsogoleri wathu ndinu


M’chifundo chanu chonse. Paulendo pomwepo
4. Ndi Mzimutu Woyera Tingakutameni bwanji
Mufike nayo mphamvu, Kaamba zonse zanuzo?
Mukatsangane nawo 2. E! Chisomo chosaleka
Akupangana omwe; Tachiona kalelo;
Mupatse ’wo chisomo Masungidwe ndi chikondi
Chokometsetsa mtima; Zikalimo momwemo;
Chikuletu chikondi Pausana, pausiku,
Chitsazo nchanu chomwe. Muli nafe ponsepo;
5. Mulungu mwa Atatu, Madalitso anu omwe
Atate, Mwana, Mzimu, Tiri ndi ambiriwo.
Tikhaletu wokondwa 3. Tinayenda muli mdima
Ndi Inu m’chiyanjano; Wotidetsa nkhaŵawo,
Titama Inu Mlungu, Pena tinangosauka
Wokonda ife ndinu; Ndi zobvuta zathuzo;
M’ulendo wathu wonse Koma Inu munalimo
Tiyende m’chikondano. Mumitambo yomweyo,
253 Nafe tinathandizana
Ndi mdalitso wanuwo.
1. MULUNGU wa Yakobo Inu,
4. Ena atsagana nafe
mdyetsa anthu anu,
Natsiriza njirayo,
Kalelo munatsogolera makolo
Nafikira kuli Inu,
athuwo.
Natilindirirako;
2. Tsopano tipereka mapemphero
Tithadi ulendo wathu
athu ano.
Ndi kupita komweko,
Mulungu wawo mukhalenso
Mutitsogolere ’Tate
Mlungu wa anawo.
Kukuŵala kosatha.
3. Tikasokera m’njira mutilondolere
ndithu, 255
67 1. MBUYE, tikuthokozani,
Chakudya ndi chobvala mutipatse Ndinu mwatitsogolera;
tsiku n’tsiku. Zaka zonse mwatisunga;
4. Mtifungatire ndi mapiko Tiyamika mokondwera,
paulendo pathu, Zotibveka, zotidyetsa,
E, tikafike okondwera kwa Atate Mphamvu, moyo, zonsezi;
wathu. ’Tate tikuthokozani
5. Tipempha madalitso ano mpatse Chaka chatsopanochi.
ife tonse; 2. Ndinu mwatithangatira
Tisankha Inu ndinu Mlungu wathu Pakuona zosautsa;
nthaŵi zonse. Polefuka ndi podwala
Ndinu mwatitsitsimutsa.
254 Munatiteteza bwino
1. MLUNGU wathu mwatifitsa Tili ana kalelo,
Kufikira leroli; Ndipo zomwe mwazichita
Moyo wathu munasunga Chaka chotitheracho.
M’njira yonse yathuyi;

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

3. Chaka chino mutipatse Mitima yoyamika.


Mphamvu zosachimwa konse, 257
Zoipitsa ndi zodetsa
1. YAMIKANI nonse ’nu,
Mtima mtichotsere zonse.
Pomwimbira nyimbozi
Mtithandize tizimvera
Za masika athuwa;
Kuyambira leroli,
Potumiza mvulayi,
Ndi kugwira ntchito zanu.
Mlungu wathu yemwedi
Chaka chatsopanochi.
Atipatsa zonsezi;
4. Inde,’Tate, mtiyendetse
Timwimbire m’nyumbayi
M’njira yolungama yanu,
Za masika athuwa.
M’mtima mwathu mtiyeretse
2. Dziko lathu lonseli
Kuti tikondane nanu.
Nla Mulungu yemweyu;
Zaka zonse muli nafe,
Atumiza mphatsozi
Sitiopa konse ’yi
Zakutilimbitsadi,
’Tate tikuthokozani
Mmera wathu wonsewu,
Chaka chatsopanochi.
Mbewu zathu zonsezi;
256 Timtamande Mbuyeyu
1. TILIMALIMA m’minda, Wotipatsa zonsezi.
Tibzala mbewu zathu, 3. Nthaŵi yina Mbuyeyu
Komatu zibvumbidwa Adzafika pansipa,
Ndi Mlunguyo wamphamvu. Nadzakonza zonsetu;
Dzuŵalo aŵalitsa Zosakondweretsazi
Namatumiza mphepo, Naziponya m’motowo,
Mbewuzo nameretsa Koma m’nkhokwe mwakemo
Mulunguyo wabwino. Mudzadzala mbewu tho!
Mphatso zonse zathu Zokomera bwinotu.
Zifuma kwa Mulungu, 4. ’Dzani Mbuye msangatu,
Tilemekeze Mbuye wathu, Msonkhanitse zonse phe;
68 Anthu anu onsewa
Atikondadi. Muŵapulumutse ’wo;
2. Wolenga ndi Yemweyo Zopweteka zawozo
Wa zinthu zonse zathu; Ziŵathere zonse phe;
Maudzu ameretsa, ’Dzani mu Ufumu ndi
Nayatsanso nyenyezi. K’ŵasonkhetsa onsewo.
Mphepo zonse zimva, 258
Nyamazo aziŵeta; 1. OYAMIKA Mlungu mbwere,
Sadzaiŵala konse Za masika mudzaimbe;
Anake kuŵadyetsa. Dzinthu zathu takolola,
3. Tiyamikira ’Tate, Sizionongeka m’minda.
Zabwino zonse zino, Mlungu Mlengi asamala,
Kubzala ndi kukunkha Zotisoŵa akonzera;
Ndi moyo tili nawo. Mloŵe m’nyumba ya Chauta,
Kuninkha Inu Mbuye Mkweze nyimbo zamasika.
Tilibe mtulo wina, 2. Dziko lonse nla Mulungu
Komatu tipereka Kuti limbalire dzinthu;

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

M’munda zonse zimamera Timgwadiretu.


Zakukoma ndi zoipa; 6. Nafenso tidzadzuka kwa ’kufa
Mmera udza, bwino ngala, ngati maluŵawo,
Maso omwe amakhwima; Timlambire Mbuye;
Mutilole, Mwini dzinthu, Oyera mtima adzabvala mbuu! pakudza
Tikakhale dzinthu zanu. Kristuyo,
3. Adzabwera Mbuye wathu Timgwadiretu.
Kukolola dzinthu zawo; 7. Tidzakhala naye nthaŵi zonse ndi
M’munda mwawo akachotse kuimbako,
Minga ndi zoipa zonse. Timlambire Mbuye;
Adzatumanso angelo Kumene moyo wa anthu
Minga akaponye m’moto, okhululukidwa uli wokomatu,
Koma tirigu amsunge Timgwadiretu.
M’nkhokwe yake nthaŵi zonse. Aleluya, Amen!
259 260
1. CHIFUKWA cha zokoma mtima 1. MLENGI wathuWakuyera,
zonse za ulerezo, Mutimvere ’fe,
Timlambire Mbuye; M’ŵasungire akutali,
Tikweze nyimbo yathu Bwinodi.
yakukondwa kuli ’Ye, 2. Mbuye Yesu, myandikire
Tigwadiretu. M’ŵakondwetsebe;
2. Dzinja lokondweretsa lafikanso, Mulimbitse mphamvu zawo
litapumatu, Zonsezo.
Timlambire Mbuye; 3. Akaona masautso
Mvula igundanso, Mulungu Mkhale nawodi;
wotikonda ’fe, Akondwere mwa chikondi
Tigwadiretu. Chanucho.
69 4. Mpulumutsi wakukoma,
3. Dziko lonse lilikukondwa, Muŵagwirize;
mlengalenga mpheponso, Nsiku zonse akulemekezeni,
Timlambire Mbuye; (Akuleme-keze.)
Zapansi pano zonse zimtamandire 5. Mzimu wanu Wakuyera,
Mlungu wathuyo, Aŵayeretse;
Timgwadiretu. Agonjetse ndi chisomo
4. Maluŵa abwino aphuka m’mapiri M’nkhondoyi.
ndi m’madambomo, 6. ’Tate, Mwana, Mzimu ,ndinu
Timlambire Mbuye; Mlungu mmodzitu,
Masamba aŵisi ang’ono Muŵasunge m’fupi mwanu
agwedezekanso, Ponsepo.
Timgwadiretu. 261
5. Zanu zapansi nzokoma Mbuye; 1. YESU, munditsogoza
Tikondwera ’fe, M’njira yanga yonseyo;
Timlambire Mbuye; Wakunditsogozatu
Koma kwanu Kumwamba komwe Ndinu, mundisungetu;
Kwapambanatu, Inde, paulendowo

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Mundisunge kolimba. Ndikatamandetu


2. Monga may’asusunza Wondisamalabe,
Mwana wake polira, Mbuyangayu.
Wakunditonthozatu 264
Ndinu, munditonthoze,
1. A! MULUNGU
Ine, m’njira yanuyi
A! Mulungu
Munditsogoleretu.
Anatuma mwana wake
3. Mbuye, ndinu wamphamvu,
Uja, ndiye Yesu
Mumatola ananu.
2. Anabadwa,
Anthu onse pansipa
Anabadwa
Ali otaikatu;
Ndi Maria Mbeta ija
Muchitire chifundo,
M’Betlehem muja.
Muŵatole onsewo.
3. Ndi angelo,
262 Ndi angelo
1. MLUNGU alinane; Anaimba: “Ndiye Yesu
Amadziŵazi Mpulumutsi wanu.”
Ndizinena, penanso 4. Alanditsa,
Za mumtimamo. Alanditsa
2. Mlungu alinane Ife anthu muzoipa
Ndi usikuwo, Zonse tazichita.
Nandiona momwemo 5. Yesu Mfumu
Mu usanamo. Yesu Mfumu,
70 Timagonja, mutisunge
3. Mlungu alinane; Moyo wathu wonse.
Zachinsinsizo 6. Mutisuke,
Zosaonekerako Mutisuke
Azidziŵatu. M’mwazi wanu, tikakhale
Ana anu tonse.
263
1. MLUNGU, Inutu,
Mwalenga dzuŵali, 265
Nyenyezi, mwezi mbee, 1. Taonani m’kholamo
Ndi dzikoli. Mwabadwira Mfumuyo
2. Koma ineyu Yakulonjezedwadi,
Simuiŵala ’yi; Nsembe yathu ndiyeyu.
Mundisamala ’ne
Ndisagwe ’yi. Kondwerani nonsenu
3. Mbuye, Msungi ’Nu, Pomvetsedwa mbiriyi
Mutuma indedi Yakumveka m’msindomo;
Za moyo wangawu “Wabadwira m’betelehemu.”
Zokomazi.
4. Yesu Mwanatu 2. Adagona m’ndyeromo
Anafa imfayo Wachokera m’mwambayo,
Achotsa zoti bii; Adasiya mpandowo
Nadzukanso; Yesu Kristu Mfumuyo.
5. Kuti m’Mwambamo 3. Falitsani mbiriyi,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Inudi abusa ‘nu; Munagona m’kholamo;


Nkhosa zanu zonsezo Mudzikonzere leronso
Mwasiy’ranji mphirimo? Mogona m’mtima mwangamu.
4. Pochezera m’dambomo, 6. Ulemerero m’Mwambamwamba
Tinaona ‘ngelotu Ndi mtendere pansipa;
Oimbira mawuwo Tiimbe nafe nyimboyi,
A mtendere pansipa. Timyamikire Mbuyathu
5. Mwana wakuyera ‘Nu, (Yesu ndiye Mfumu,
Munakonda ifedi; 71
Munasiya kwanuko Yesu ndiye Mfumu!
Ndi kufika pansipa. Ndikhulupirira Yesu wobadwira
6. Mtiphunzitse bwinotu, m’kholamo.)
Mwana wakuyera ‘Nu,
Tifanane nanudi 267
M’makhalidwe anuwo. 1. ANA inu, ana inu,
7. Tamverani, aitana; Taukani ndi kumvera
“Ana, munditsatetu.” Amithenga akumwamba;
Yesu, tisapite kwina, Anafika kalelo,
Tizikutsatani ‘Nu. Natiuza Mpulumutsi
8. Posachedwa tilekana Anabadwa pansipa.
Osalankhulananso, Zaka zonse, tsiku lomwe
Koma tidzaona tonse Umamveka mthengawu.
Wina mzake m’mwambamo. 2. M’nyumba zonse ponseponse
Zimamveka nyimbo izi,
266 Kuti Yesu anabadwa,
1. TIIMBE ndi kulalikira Anagona m’kholamo,
Mthenga wa chikondicho Anafika Mpulumutsi
Anamva Mlungu m’Mwambamo Wotikondweretsadi,
Kulira kwathu pansipa. Kondwerani, kondwerani
(Ndikhulupirira Yesu Inu nonse ana ’nu.
Wobadwira m’kholamo; 3. Taukani, taonani
Iye ndiye Mfumu yathu, M’mwamba monse mwakuyera;
Timtame nthaŵi zonse.) Amithenga a Mulungu
2. Kwa ife lero anabadwa Aimbabe nyimboyo.
Mwana wa Mariyayo, Yesu Kristu anatsika,
Pamsinkhu, ine mng’ono koma Anachoka kwawoko;
Mwini dziko lonseli. Lero lonse tiimbenso
3. Anadza nazo mphatso zake Nyimbo yathu yomweyo.
Anatikonzeratu;
Anatitseguliradi 268
Pakhome pa Ufumuwo. 1. KALE m’mzinda wachifumu
4. Ambuye takutamandani Munalimo m’kholamo,
Tsiku lakubadwali, Momwe mkazi anaika
Mwa Inu tonse tikondwera, Mwana wake m’ndyeromo.
Tiseke tonsefe. Ndiye mkaziyo Mariya,
5. A! Yesu Mbuye wakuyera, Yesu Kristu Mwanayo.
2. Uyu ’natsikira kuno,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Mlungu Mbuye wathuyo; Ife tonse anthuwo


Anabadwa uyu m’khola Attenga Mlunguyo.
Anagona m’ndyeromo. Mlemekeze “Tate,
Mwa osoŵa ndi oipa Mwana, Mzimunso.”
Yesu anakhalamo.
3. Mwa ubwana wake wonse 270
Anakula m’mtima phee!
1. Kale anthu m’kholamo
Anakonda, anafatsa,
‘Napembedza mwanayo.
Amay’ wake namvabe;
Ndipo ana nonsenu,
Ndiye Mbuye, Mfumu yanga,
Mukamtsate bwinotu.
Ndiye Mbuye wa kumwamba,
4. Ndipo Mwana uyu Yesu
Amgwadira anthuwo,
Anakulakulabe;
Timtamande Mfumuyo.
Ndi wamng’ono ndi wofoka,
Anagona enawo.
2. Wosauka iyedi
Nsoni zathu anazimva
Anagwira ntchotozi
Ndi chimwemwe chathunso.
3. Ndani kodi mbuyathuyo
5. Ndi chifukwa atikonda,
Woyesedwa m’bwinjamo?
Tidzampenya masowa,
4. Analira ndaniyo
Kuti Mwanayo wofatsa
Pomwalira Bwenzilo?
Ndiye Mwini m’Mwambamo;
Atengera ana ake
Aleluya! Aleluya!
Komwe adapitako.
Timwimbire Yesuyo.
6. Koma sitimpenya m’khola
Aleluya! Aleluya!
Muli ng’ombe momwemo;
Timwimbire Yesuyo.
Ayi, tidzamwona m’Mwamba
Muli Mlungu ’Tatewo.
5. Iye anachoka kwawo,
Ana akuyera mbuu
Anakhala pansipa.
Adzamzunguliratu.
Kale ana ‘namwimbira
Namukondweretsadi.
269 6. Anafika ‘kazi omwe
1. Usikuwo oyerawo! Ndi tiana tawoto;
Mwana adamlerayo Yesu anatiyangata,
Akakhale Mfumuyo. Anatidalitsatu.
Anabadwa mkholamo, 7. Amithenga akumwamba
Mfumu ya mamfumu Amamuyamikiratu;
Ndi ya anthuwo. Zikwi zosawerengeka
2. Mwanayo wa Mulunguyo Zimtamanda Mfumuyo.
Andikonda inetu, 8. Ana inu yamikani
Nan’tayira chumacho Bwenzi lanu lomweli;
Nadzagona m’udzumo. M’mwamba momwe
Ndiyamika mbuye mudzampenya
Wanga Yesuyo. Ndi kumtamandirabe.
3. Usikuwo woyerawo! 271
Wadzatu mtendere
1. KULI kaphiri m’talimo

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Kunja kwa mzindawo, 5. Ana inu, yamikani


Kwapachikidwa Yesuyo Bwenzi lanu lomweli;
Nafera ifetu. M’Mwamba momwe
(Kuli kaphiri m’talimo Mudzampenya
Kunja kwa mzindawo, Ndi kumtamandirabe.
Kwapachikidwa Yesuyo 273
Nafera ifetu.)
1. ANANU, ziimbani,
2. Zoopsya sitidziŵapo
Aleluya, Amen.
Anazitengazo,
Ambuye tamandani,
Komatu tidziŵitsa ’fe
Aleluya, Amen.
Anatiferapo.
Kwezani mawu anu,
3. Anatifera tonsefe
Patsani mtima wanu,
Tiwomboledweko,
Afuna kumva inu,
Tifike momwe m’Mwambamo
Aleluya Amen.
Ndi mwazi wakewo.
2. Bwerani, kondwerani,
4. Kulibe wokwanira ’yi
Aleluya, Amen.
Kulipa mlanduwo,
Ambuye akumvani,
Wina wakutsegula ’yi
Aleluya, Amen.
Pakhomo pakepo.
Amatitsogolera,
72 Kalelo natifera,
5. Anatikondakonda ’Ye, Kukonda salekera,
Timkonde ifenso; Aleluya, Amen.
Tizimtsatira, tithetu 3. Mbuye timlemekeze,
Zintchito zakezo. Aleluya, Amen.
272 Kwawo tikabwereze,
1. ANA inu, myamikeni Aleluya, Amen.
Mpulumutsi Yesuyo, Kumwamba timtamire,
Kaamba ka chikondi chake Tikamgwadire ife,
Ndi chipulumutsocho Tikhale chikhalire,
Aleluya! Aleluya! Aleluya, Amen.
Timwimbire Yesuyo. 274
Aleluya! Aleluya! 1. MNANDIDZERA, Ambuye,
Timwimbire Yesuyo. Kumwambako,
2. Iye anachoka kwawo, Munasiya akuluwo;
Anakhala pansipa. Koma m’mudziwotu
Kale ana ’namwimbira Munabadwamo
Namukondweretsadi. Munasoŵa pogonapo.
3. Anafika ’kazi omwe Idzani mumtima mwanga,
Ndi tiana taoto; Muli malo a Inu ’mo.
Yesu anatiyangata, 2. Amithenga ’naimba pamlengapo,
Anatidalitsatu. Nalalika ulemuwo;
4. Amithenga akumwamba Koma Inu munadza mofatsatu,
Amamyamikiratu Munabadwa mukholamo.
Zikwi zosaŵerengeka 3. Zili nazotu nkhwimba zirombozo,
Zimtamanda Mfumuyo. Ndi mbalamenso zisatu;

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Koma Inu Ambuye mwapandadi Kopani anthu abwere kwa Inu.


Potsamira mutu duu! 276
4. Munanenatu mawu a moyonso
1. ANA a Yerusalemu
Omasula ochimwawo;
Anatama Mbuye wawo;
Koma omwe ochimwa
Lero lomwe ife ana
’Nanyozatu,
Timwimbira nyimbo yawo.
Nakuphani pamtandapo.
Mverani, aimba anawo,
5. Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
Mverani aimba anawo
Ndi zamphamvuzo zanunso,
Zakutama, zakutama,
Mundimvetse za kwanu
Zakutama Mbuyeyo.
Kumwambako
2. Tamva tikondane naye,
Kuli malo a ine ’ko.
Tiŵerenge Mawu ake,
Ukondwere mtima wanga
M’njira mwake tiyendemo,
73 Tiziimba nyimbo zake.
Pakumvera zokomazo. 3. Aphunzitsi, ana omwe,
275 Ndi akulu, t’imbe tonse;
1. AKAZI anadza kwa Yesu Nyimbo zathu zidzakwera
ndi anawo, Zikamveke m’Mwamba monse.
Anaŵaletsa anyamata nawakana 277
ndithu; 1. OSANATU, osana,
Ambuye naŵapezadi, ’Naimba anawo;
Anati: “Musatero ’yi M’kachisi wa Mulungu
Lolani ana abwere kwa Ine, Mwamveka nyimboyo.
Lolani ana abwere kwa Ine. ’Nalemekeza Yesuyo
2. “Ndidzaŵalandira, k’ŵasunga Wak’ŵadalitsayo;
M’manja mwanga; Anamuyamikira
Ndi Mbusa wao Inetu, msachotse M’ubwana wawowo.
ana anga; 2. Kuphiri la ’Zitona,
Akandipatsa mtimawo, Mumpingo wa ’nthuwo,
Adzanka ndine Kwathuko; ’namkupizira mnjedza
Lolani ana abwere kwa Ine, Naimba nyimboyo,
Lolani ana abwere kwa Ine.” Angelo akumwambako
3. Wokoma Mbuyathu kwitana ana Napokerezanso:
onse; “Osana m’Mwambamwamba
Atsalanso ambiri ena sanamvera Kwa Mlungu wathuyo.”
zake; 3. Zitsamba zakuyera
Sanamva mawu akewo, ’Naponya pansipo;
Sadziŵa kuti ’natinso: Kukondwa kunamveka
“Lolani ana abwere kwa Ine, Paphiri ponsepo.
Lolani ana abwere kwa Ine.” Ambuye yemwe Mfumutu
4. Afike masiku akuti anthu onse Nakwera cheteko;
Adzamva mawu anu ndi kutsata Tiana toyamika
Inu nokha; Sanatinyozato.
Muwale m’mtima mwawomo, 4. “Osana m’Mwambamwamba!”
Adziŵe muŵakondanso; Nyimboyi t’imbenso,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Pokhala Kristu Mfumu Zochimwa zindizinga,


Ndi Mpulumutsiyo. Koma ndidziŵatu
Timtamandire Iyeyu Anawombola ine
Ndi mtima wonsewo; Pakundikondadi.
Tipite kwawo komwe 2. Ndikondwa kuti Yesu
Tikaimbirenso. ’Nakhala mwanatu,
278 Chitsanzo atipatsa
Cha moyo wakewo;
1. NGOLIZO zilira
Ndikati ndimtsatire
Za ’mithengawo,
Zochita zakezo,
Ndi zipata zonse
Sadzandinyoza konse
Zatsegudwa mbee!
Pakundikondadi.
74 3. Pakumyamika Iye
Kristu, Mfumu yathu, Ndidzamwimbiratu;
Mbuye wathudi, Ngakhale sindimwona
Wapambana monse, Amandimveradi;
Alamulabe. Pakuti walonjeza
Ntchito zake zatha, Adzalandira ’ne
Timwimbiretu; Ndiimbe ndi angelo,
Yesuyo wakwera, Pakundikondadi.
Timtamandetu.
2. ’Natipulumutsa 281
Natiferako, 1. YESU andikonda ine,
Ali mfumu ndithu Amatero m’Buku Iye;
Kwa Atatewo; Akafoka mwana wake
Osasautsidwa, Adzamlimbikitsa Mbuye.
Osafanso ’yi Yesu akonda,
Yesu, Mfumu yathu Yesu akonda
Adakweradi. Yeu akonda,
3. Atipempherera Atero m’Bukumo.
M’malo ’dalawo, 2. Anandifera Mbuye wanga
Tinke kwathu komwe Anditsegulire m’Mwamba,
Ndi chisomocho; Ndi machimo anga onse
Akonzera malo Adzandichotsera konse.
Ana akewo; 3. Mbuye Yesu andisunga
Yesu alipobe, M’njira ya Kumwamba kuja;
Atikondanso. Andigwira m’dzanja langa
Ndingagweremo m’makwaŵa.
279 4. Yesu andikonda ine;
1 Ndikadzafa tsiku lina
Atengera ine kuno,
280 Ndikakhale naye Kwawo.
1. NDIKONDA mbiri yomwe
Ya amithengawo 282
Ya Mbuye, Mfumu yathu 1. YESU Mbuye ’Nu wofatsa
Pofika pansipa; Muyang’anedi kamwana,
Mndichitire chifundo;

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Mundilole kwanutu. Mfumu yakumveka;


2. Ndimalira kwa Inutu, Ife sit’yenera,
Mpatse mtimawo wabwino; Koma mutimvere.
M’Dziko lanu loŵalalo 3. Ndife akuchoka,
Mulandire mwana wanu. Mwina tisokera;
3. Yesu, E, ndikufunani, M’njira ya Kumwamba
Ndinu chuma change chonse; Mutitsogolere
Mtima wanu ngwofatsadi; 4. Mutiletse, Mbuye,
Kale munali kamwana. Lero tisachimwe;
4. Wonga Inu ndikhaledi, Tikondane ndinu
Mtima wanu mundipatse; Mutitsuke m’mtima.
75 5. Mukatiitana
Yesu ndinu wokomatu, Tikakhale kwanu,
Mndiphunzitse kukonda ’Nu. Tidzayankha, “Mbuye,
5. Yesu Mbuye ’Nu wabwino, Tsopano tili pano.”
M’manja mwanu ndikhalemo; (Yesu, Yesu,
Mzimu wanu mundipatse, Tikugwadirani
M’mtima mwangatu mukhale. Mwana wa Mulungu!)
283 285
1. YESU, ndikabwera 1. MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
Mundikondweretsa, Mutitsogolere ife;
Nsoni zanga mun’chotsera Mutiŵete, mutisunge,
Zonsezo. M’khola mwanu mtilandire
Ndikabwera, Mbuye; Yesu wathu, Yesu wathu,
Ndidzakondwera ine; Mnatigula ana anu.
Muitana ana onse 2. Ndife ana, mutikonda,
Onga ‘ne M’njira mutiperekeze;
2. Yesu, ndikabwera, Mchotse nsoni ndi zoipa,
Mumva mapemphero Osokera muŵabweze:
Mundikonda, mnandifera Yesu wathu, Yesu wathu,
Inetu. Mumve mapemphero athu.
3. Yesu, ndikabwera 3. Munanena mulandira
Dzanja mdzandigwira Osauka ndi oipa;
Nokha mdzandilongolera Inu ndinu wachifundo
Njirayo. Ndi wamphamvu yolanditsa
4. N’takafika kwanu Yesu wathu, Yesu wathu,
Ndidzakhala bwino, Tidzatu tiana tanu.
N’dzaonana ndi ananu, 4. Tifunitsa Inu tere,
Ndi Yesu. Chifuniro chanu ndicho;
Mbuye wathu, Mpulumutsi,
284 Mutikonzetu m’katimo;
1. YESU wa Kumwamba, Yesu wathu, Yesu wathu,
Mutimvere ife; Mutikondebe ana anu.
Tikugwadirani,
Mwana wa Mulungu. 286
2. Ndinu wakuyera 1. MZINDA woyerawo

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Konse nkotsekako; Mutimvere, Yesu.


Kanthu koipa, 3. Ife tikondana nanu,
Kanthu koipa, Tiimbira nyimbo zanu,
Sikangaloŵemo. Tiyamika mphamvu yanu;
76 Mutimvere, Yesu.
2. Yesu ndafikatu, 4. Lero mkhale nafe ndithu,
Mbuyanga kwanuku; Poseŵera ndi pantchito,
Mundiyeretse, Popemphera ndi poimba;
Mundiyeretse, Mutimvere, Yesu.
Mnditsuke m’mtimamu. 5. Mutiletse tisaname
3. Mbuye, ndikhaletu Ndikunena zotukwana,
Mbuye wokonda ’Nu, Mtiphunzitse kukondana;
Ndi wosungidwa, Mutimvere, Yesu.
Ndi wosungidwa, 289
Ndi mphamvu zanuzo. 1. YESU atiuza tiŵale ’fe.
4. Mpaka ndabvala mbuu! Monga nyali m’mdima
Wowomboledwatu, tiunike mbee!
Woyera mtima, Pansi pali mdima ŵalanitu,
Woyera mtima, Inu m’malo mwanu ndi ine ’mu.
Kwanu Kumwambako 2. Yesu atiuza tiyambemo,
287 Ationa bwino ndi kuŵalako;
1. MBUYE, tili ana anu, Ayang’ana pansi poŵala ’fe,
Tiyamike Inutu; Inu m’malo mwanu ndi ine ’mu.
Zinthu zonse zili zanu, 3. Yesu atiuza tiŵale pa
Tingadike m’mtimamo. Anthu ali m’mdima osaukawa;
Tiganize zake Yesu, Tiŵalire onse, tonsefetu,
Za Kumwamba kuli ’Ye; Inu m’malo mwanu ndi ine ’mu.
Tisachite zomsautsa, 290
Aziona zonsezo. 1. ANYAMATA inutu,
2. Amakumbukira zonse Anamwali inunso,
Tizichita zomwezo. Muti: “Tingachitenji,
Tidzamukomana tonse, Ang’ono ndifetu,
Sitinyazitsidwako. Kuthandiza Ufumu
Mukhululukire ife Wa Yesu?”
Tchimo lathu lonselo. 2. Aphunzitse anthuwo,
Mutitsogolere ife Aŵalalikiredi,
M’njira ya Kumwambako. Akukhala moipa
288 Mumdima wakunja,
1. YESU, muli pa chimpando Aloŵetu m’Ufumu
Chakuŵala mbee! Kumwamba; Wa Yesu.
Mutipenye ife ana; 3. E! ang’ono ndifetu,
Mutimvere, Yesu. Nzeru sizimafika
2. Ife ana sitiopa, Kuti tingaphunzitse;
Mukabwera mutiona, Titani tonsefe
Tamva kale mutikonda; Kuthandiza ufumu

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

77 Yesu ndi woyera;


Wa Yesu? Ana ake omwe
4. Inu nonse anzanga, Aziyera m’mtima
Tiziganiza bwino, 3. Mzimu wakuipa
Tinganene mofatsa, Ukusuzumira,
Timverenso Mbuye Umakuyesera
Kuthandiza Ufumu Kuti ukachimwe.
Wa Yesu. 4. Koma usalole
5. Pothandiza amathu, Mawu a Satana;
Pak’ŵakonda anzathu, Bweza tchimo lake,
Pakusiya zoipa, Chita zolungama.
Pokhaladi bwino, 5. Yesu ndi Mbuyako,
Tithandiza Ufumu Mbuyeyo ngwabwino;
Wa Yesu. Ana ake omwe
Aziyera m’mtima.
291
1. TIANA ife tingofoka, 293
Sitikhala ’mphamvu ’yi; 1. TCHIMO musalole,
Tikhoza kukachitiranji musadziipitse,
Yesu kumkondwetsadi? Myese kudzikana, muzilimbikadi;
2. Tiana ta Ambuye tili Mwamphamvu mpirire, mgonjetse
N’ntchito yaikuludi, zabiizi;
Kudzichepetsa ndi kusiya Mpenye kuti Yesu adzakusungani.
Tchimo lili lonseli. Mpemphe Mbuye asunge,
3. Kapena m’mtima ndimakwiya, Atonthoze m’mtimamu,
Nditukwana mnzangayo, Alikukufunani,
Kapena ndidzitama – izi Akasunge inutu.
Ndilekere Mbuyeyo. 2. Mleŵe oipawo, ayi musatukwane,
4. Ndileke kulimbana ndi Dzina la Mbuyathu
Kuŵanamiza enawo; muzilikwezadi;
Ndinene zakufatsa, Khalani achangu, oona, abwino;
Zakukondweretsa Yesuyo. Mpenye kuli Yesu,
5. Tizikondana, tisekere adzakusungani.
Tsiku lonse kwathuko, 3. Yesu alandira akupirirawo;
Muyere m’mtima popeza Chikhulupiriro chiŵathandizadi
Yesu ndi Woyerayo. Mbuye athangata onse akumvera;
6. Palibe mwana wakuchepa Mpenye kuli Yesu,
Kunyamula mtandawu; adzakusungani.
Ambuye Yesu mutipatse 294
Mtima wokondanatu.
78
292 1. NTHAŴI yaubwana yatha,
1. USACHIMWE konse, Sukulu yathu yathanso;
Lekatu kukwiya; Nkhaŵa ndi zoŵaŵa zomwe
Uli mwana wake, Zitibisaliranso.
Mwana wa Mbuyathu. 2. Yesu wakufatsa mtima
2. Yesu ndi wofatsa, Mlendo pansi pano ’Ye,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

’Natifera, natisunga, Poyendayenda ’ne;


Atitsogolere ’fe. Paŵala mosekera
3. Tamverani, aitana; Ndi dzuŵa loti mbee!
“Ana, munditsatetu,” Ndikondwa nsiku zonse
Yesu, tisapite kwina, Ndikali m’dzikoli,
Tizikutsatani ’Nu. Potsata Yesu m’njira yake
4. Posachedwa tilekana Yonseyi.
Osalankhulananso, 2. Ulendo ungoyamba
Koma tidzaona tonse Wakunka kwathuko;
Wina mnzake m’Mwambamo. Amati: “Udzapeza
295 Zakusautsa ’mo”
Zobvuta ndi chisoni
1. YESU ndiye Mbusa,
Sindiziopa ’yi;
Mbusa wakukoma,
Ndidzangomtsata Yesu m’njira
Anyamula ana
Yonseyi.
Ake akuopa;
3. Zoipa ndi zabwino
Tizitsata Yesu,
Zakundigwerazo,
Atitsogolera,
Ndingonka nazo zonse
Kwina kuli mdima,
Ndimuze Yesuyo;
Kwinanso koyera.
Zoŵaŵa adzachotsa
2. Yesu ndiye Mbusa
Zondiliritsazi;
Atipenyetsetsa,
Ndikangomtsata Yesu m’njira
Mawu ake onse
4. Zondipingitsa zonse
Atikondweretsa.
Zoloŵa m’mtimamo
Mwina alangiza
Achotsa, nandisunga
Mwana wakulakwa;
M’ulendo wonsewu.
Atsogola bwino,
Sindidzaopa kanthu,
Ife tizimtsata.
Ngakhale imfayo,
3. Yesu ndiye Mbusa,
Pomtsata Yesu yekha kunka
Anafera kale
Kwathuko.
Kuyeretsa ana
Nawo mwazi wake, 297
Tsono awalemba 1. MPULUMUTSI Yesu,
Ndi chizindikiro; Mumve nyimbo yathu;
“Ana anga onse Tikuyamikani
Andikhulupira.” Mumitima mwathu
4. Yesu ndiye Mbusa Zonse tili nazo;
Wakutisunga ife, Thupi, mzimu womwe,
Ali wachifundo 79
Chachikulu ndithu; Inde, moyo wonse,
Sitiopa imfa Tipereka zonse.
Akakhala nafe, Komwe ndi Chimwemwe
Yesu Mbuye wathu Tidzaimba tonse,
Alandira ife. Tidzatama Mbuye
296 Osalema konse.
1. POMPANO pandikonda 2. Tiyandika, Mbuye,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

M’fupifupi ndinu, 1. M’MANJA a Yesu wanga


Tikugwadirani, Ndilikugonamo,
Mutilandire bwino. Mommo aphimba ine
Inu munatsika Nacho chikondicho.
Kutifera ife; Mvera! Mudzera m’Mwamba
Inu munakwera Mawu a Yesu wanga:
Kuti titsatire. “Mwana, ndidzakusunga
3. Haya! Tipitenso Pano pamtima panga,”
M’njira yomwe ija M’manja a Yesu wanga
Ana a Mulungu Ndilikugonamo,
Onse adaponda. Mommo aphimba ine
Tizisiya zonse, Nacho chikondicho.
Tiziyenda msanga, 2. M’manja a Yesu wanga
Tisamachewuka Nkhaŵa zonsezo zi!
Mpaka tipambana. Momwe zoipa zanga
4. Tero tidzakwera Sizindibvuta ’yi
Kwawo kwa Mulungu, Mmomo mulibe nsoni,
Tidzaziiŵala Mommo mokoma monse
Zotibvuta ife. Sindiliramo msozi,
Komwe ndi Chimwemwe Ndikondwa m’mtima monse.
Tidzaimba tonse, 3. Mtima umabisala
Tidzatama Mbuye M’manja mwa Yesumu;
Osalema konse. Mbuye, musunge ine,
298 Munandifera ’ne.
Ndilinda mopirira
1. Ine ndine mlendo
Mpaka wochoka mdima.
Wa Kumwambako;
Ndikaonana naye
Pansi pandikonda,
Yesu Ambuye wanga.
Koma mpoipa.
2. Kwathu nkopambana, 300
Nkosachimwako; 1. YESU ndiye Bwenzi lathu,
Zosautsa zonse Kumwamba kuli kwao;
Sizikhalamo. Amatikonda tonse,
3. Koma azibvala Akulu ndi tiana;
Mwana zoti mbuu! Anzathu sapirira
Wosachimwa konse 80
M’mtima mwakemu. Amalekana nafe,
4. Yesu, mndiyeretse, Komabe kutiyanja
Mndimveretsedi; Saleka Yesuyo.
Mzimu, mndiyendetse 2. Ana ake adzapuma
Mn’jira yanuyi. Kumwamba mokondwera,
5. Ine ndine mlendo Amene anamkonda
Wa Kumwambako; Namtsata Yesu yekha;
Kundiyandikira Sauko ndi zobvuta
Kwathu komweko. Zotitopetsa kuno,
299 Sitiziona konse

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Kumwamba kwathuko. Ndi amithenga omwewo


3. Tidzalandirabe komwe Akondwerera kokhako.
Zobvala za mitima Nkoti mbee! Nkoti mbee!
Yoyera, ndi kubvula 2. Zochimwa siziloŵako,
Zakale za kuchimwa; Mwayitu! Mwayitu!
Chimwemwe ndi chikondi Misozi m’maso mwawo yi.
Tidzangokhala nazo, Mwayitu! Mwayitu!
Za ndewu ndi chisoni Chisomo chili m’mtimamo,
Sitizipeza ’yi. Aona nkhope yakeyo
4. Woyenera ndani kunka Ya Yesu adalitsawo.
Kukhala ndi Atate, Mwayitu! Mwayitu!
Kuimba nyimbo zake, 3. Oipa tili tonsefe;
Za Mpulumutsi wathu? Mwaziwo, mwaziwo,
Tidzamka ife tonse Wa Yesu watigulatu;
Tamtsata pansi pano; Mwaziwo! Mwaziwo!
Tiyeni ana onse, Tiyeretsedwa nawowo,
Yambani leroli. Mtendere wa Mbuyathuyo
301 Ukhala nafe komweko.
Mwaziwo! Mwaziwo!
1. yesu adza kuwerenga
Ana ake abwino. 303
1. DZIKO lilipolo
Ndikuvala zachifumu Lokondwatu
Zakuwlazo ake. Oyera ’khalamo,
Ana ake angonga Abvala mbuu!
Nyenyezi zamwamba, Tamvani nyimboyo:
“Mfumu tiyamikeyo,
Adzawala m’ufumu Mkwezeni Dzinalo
Wa ambuye yesu. Mwimbenibe.”
2. yesu adza kukundika 2. Tiye kudzikolo,
Tiyeni ’nu;
Ana ake ankhosa.
Musakayikebe,
Ndiye mbusa wakufatsa Muchedwatu.
Namalizatu lero. Tikondwekondwedi,
3. kudzachera tsiku lijalo Tchimo ndi zoipa zii!
Mbuye timwona ndi
Msangatu msanga, Kukondwabe.
Kudzawala m’mawa wake 3. Maso a m’dzikomo
Pompano Onse nga mbuu!
Mkono wa ’Tatewo
302 Ngwosungatu.
1. KWA Yesu ndi kwabwinoko, Tiye ku dzikolo,
Nkoti mbee! Nkoti mbee! Mgwire ’nu ufumuwo.
Kulibe zoipitsako, M’mwamba mwa dzuŵamo
Nkoti mbee! Nkoti mbee! Tikhalebe.
Kuimba amaimbako, 304
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

1. DZUŴA liŵala, m’tulotu 307


’Tate chikondi chanucho
1. AMBUYE, mtidalitsetu,
Chindidalitsapo.
Musunge Mawu m’mtimamu;
2. Dzuŵa la lero lonseli
Muyatse moto wanuyo,
Mundisungire ’ne;
Chikuletu chikondicho.
Mchotse zoipa zangazi,
Pokhala moyo imfanso,
Nanu ndikhalebe.
Ambuye mtiŵalirepo.
3. M’mtima mwangamu mloŵemo,
2. Laloŵa dzuŵa, kwada bii!
Mwini chifundocho,
Mwapenya ntchito zathuzi;
Kuti ndikafananetu
Taletsa mwini tchimolo,
81 Mwinanso tangolakwapo.
Ndinu Mbuyangayo. 3. Mufafanize m’bukumo
305 Zolakwa zanu zonsezo,
1. Yesu Mbusa, mutimvere, Ndi kutipatsa ifetu
Dalitsani ifetu, Mtendere wanu m’katimu.
Ndi usiku mutisunge, 4. Chimwemwe chomwe mpatseko
Tidzukenso bwinotu. Ndikukondana ndinunso
2. Lero lino mwatipatsa Tifuna kufananadi
Zonse tili nazotu, Ndi Yesu Bwenzi lathuli.
Moyo womwe; miyamiko 308
Landireni Mbuye ’Nu. 1. TIKUTHA kupemphera,
3. Tchimo lathu lonse, Yesu, Tipita kwathu tonse;
Mukhululukire ’lo; Mtiperekeze Mbuye,
Mtitengere kwanu komwe Panjira zathu zonse;
Kumpumulo wanuwo. Titamva Mawu anu,
306 Mawuwo ndi amoyo,
1. TILIKUIMBA nyimbo yomweyi, Aloŵe m’mtima mwathu,
Yakuyamika Mbuye wathuyo; Akhazikikemo.
Mtendere wake tiufunadi, 2. Ambuye, Mzimu wanu
Titapemphera tinke kwathuko. Atikumbutse tonse,
2. Titanka kwathu mkhale nafeko, Atithandize lero
Tikufunani Yesu Mbuyathu; Kumvera Mawu onse.
Musunge ife nthaŵi zonsezo, Kumudzi mkhale nafe,
Mutiyeretse m’mtima mwathu Musatisiye konse;
mbuu! Machimo onse mletse,
3. Usiku uno mutisungedi, Tiyere m’mtimamo.
Khalani m’fupi m’nyumba 309
mwathumo; 3. TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
Mamaŵanso mudzatidzutse nji! Anthu ndi zinthu zonsezi,
Kuti tigwire ntchito zathuzo. Ndi onse a Kumwambako
4. Mtitsogolere nthaŵi zonsezo; Mlungu amyamikiredi.
Kuyenda tokha sitikhoza ’yi,
Ngati mukhala Mbuye m’fupimo, 310
Sitidzaopa kanthu kena ’yi. 1. MULUNGU akhale nawo
ulemerero ndi dalitso,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Ndiye Atate, Mwana, 3. Ayamikire ’Nu


Mzimu Woyera, Mlungu mmodzi; Padziko ponsepa,
2. Tsopano, poyamba paja, Mitundu yonse ipfuule
Masiku onse alinkudza Mokondweratu.
82 4. Pakuti mfumuyo
Mphamvu, ulemerero, Ndi Inu nokha ’Nu;
dalitso, chipambano. Mudzalangiza bwinotu
Mafuko onsewo.
311 5. Zipatso zakezi
1. YEHOVA, Mbusa wangadi, Labala dzikolo;
Ndilibe kusoŵa; Adzadalitsa ifetu
Andigonetsa bwinoli Mulungu wathuyu.
Mumsipu wokoma. 6. Adzadalitsa ’fe
2. Ku madzi ake odikha Mulungu mwiniyo;
Anditsogolera; Padziko ponse anthuwo
Ndi moyo wanga wofoka Adzamuopatu.
Aulimbikitsa.
3. Anditsogolera m’njira 313
Zakulungamazo; 1. NONSE okhala pansipa,
Chifukwa changa ay’, koma Muyamikire Mlunguyo;
Cha dzina lakelo. Ndi nyimbo mtumikire ’Ye;
4. Ndipyola kodi chikhwaŵa Mubwere mokondweratu.
Cha mthunzi wa imfa? 2. Yehova ndiye Mlungudi,
Ndilibe mantha ngati ’Nu Anatilenga yekhayo;
Mundiperekeza. Amatidyetsa ake ’fe,
5. Chakudya changa chabwino Ndi nkhosa zake ifetu.
Mwandikonzera pha! 3. Loŵani m’Nyumba mwakemu
Pamaso pa adaniwo Ndi nyimbo zokondweretsatu;
Mudyetsa mtimanga. Mumyamikire Mlunguyo.
6. Mwadzoza mutu wanga ndi Mulemekeze Dzinali.
Mafuta okoma; 4. Pakuti Mbuye Mlunguyo
Mwadzadza chikho changadi, Wokoma mtima ndiyedi,
Inde, chisefuka. Woona adzakhalabe
7. Zokoma ndi zakuyanja Kunthaŵi nthaŵi zonsetu.
Zidzanditsatako; 314
Ndikhala m’nyumba ya Mlungu 1. MULI ndi ludzu, idzani
Ku nthaŵi zonsezo. Kumadzi amoyo
312 Imwani monse kolere
1. MULUNGU, anthu ’fe Kuchitsime konko.
Mutidalitsetu; 2. Munka kangati kulaŵa
Chisomo chiŵalire ’fe Madzi onyengera?
Cha nkhope yanuyo. Musataye mphamvu yanu,
2. Potero onsewo 83
Okhala pansipa Musataye chuma.
Adzamva bwino msangatu 3. Imvani, Yesu akuti;
Za njira yanuyi. “Chuma ndili nacho,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Landirani, yemwe amva Lidzakhala nthaŵi zonse


Akhale ndi moyo.” (Nthaŵi zonse).
4. Funani Mlungu tsopano. 8. Tonse timyamiketu,
Akulindirani; Tonse timyamiketu,
Iye ndiye wachifundo, Mpulumutsi wamuyaya
Akulandirani. (Wamuyaya).
5. Ali wokhululukira; 316
Imvani ananu:
1. AITANA, aitana dziko lonse,
Mtima wake usiyana
Imvani mukhaliranji chete?
Ndi mitima yathu.
Aitana,
6. Monga m’Mwamba mupambana
Aitana aitana dziko lonse.
Zonse pansi pano;
2. Mfumu iyi, Mfumu iyi ya
Choncho maganizo ake
Kumwamba
Apitira athu.
Ndi Yesu, ndi Mpulumutsiyo wa
7. Anthu onse a padziko
anthu onse.
Adzamvera Mlungu:
Anthu onse, anthu onse, tinke
Adzakhala ndi chimwemwe,
kwawo.
Nadzamtama ndithu.
3. Aitana,aitana inu mayi,
315 Ndi Yesu, amene anakhetsa
1. TIYAMIKE Mlunguyo, mwazi wake;
Tiyamike Mlunguyo, Mwazi wake unagwera inu mayi.
Watidzera ndi mtendere 4. Aitana, aitana inu ’tate,
(Ndi mtendere). Ndi Yesu amene anakhetsa mwazi
2. Anatuma, Mtetezi, wake;
Anatuma Mtetezi, Mwazi wake unagwera inu ’tate.
Ndiye Mfumu Yesu Kristu 5. Yesu ati, Yesu ati; “Muzisiye
(Yesu Kristu). Zoipa zimene muzichita,
3. Tifunafunatu, muzisiye,
Tifunafunatu, Muzisiye, muzisiye inu nonse.”
Osapeza Mpulumutsi 6. Titi bwanji? Titi bwanji ife anthu?
(Mpulumutsi). Ndi Yesu anatifera ife
4. Tifunafuna m’phirimo, akuchimwa;
Tinafuna m’phirimo, 84
Koma osampeza mommo Akuchimwa, akuchimwa tinke
(Osampeza). kwawo.
5. Tinafuna m’nyanjamo,
Tinafuna m’nyanjamo, 317
Koma osampeza mommo 1. ’TATE, ’Nu.
(Osampeza). ’Tate ’Nu, mtione ’fe
6. Yesu ndiye Mtetezi, Tadza kupemphera kwa Inu.
Yesu ndiye Mtetezi, 2. Imvani,
Wina saoneka ayi Imvani Amfumu ’Nu
(Saoneka). Mawu athu tinena lero.
7. Dzina lake Yesuyo, 3. Tipempha,
Dzina lake Yesuyo, Tipempha mdalitsetu
Mpingo wanu woyera uno.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

4. Imvani, Aleluya Bwenzilo!


Imvani akunjawo Amakonda, amasunga;
Akulira opanda Yesu . Ndimufuna Yesuyo.
5. Ayenda, 2. Yesu ndiye mphamvu yanga,
Ayenda munjirazo Andilimbikitsatu;
Zakupita kuchitayiko. Poyesedwa ndi adani
6. Ambiri, Andipambanitsadi.
Ambiri akufadi 3. Yesu atonthoza mtima
Osadziŵa za Kristu Yesu. Ndikadera nkhaŵa ’ne
7. Auke, Pakukhala ndi chisoni
Auke akristuwo, Andisangalatsabe.
Akakhale antchito anu. 4. Yesu ndiye Mtsogoleri
8. M’ŵatume, Pakuyenda m’njiramo,
M’ŵatume antchitowo Ndipo ndikafuna kugwa
Alalike Uthenga wanu. Andigwira dzanjalo.
9. Ubwere, 5. Yesu ndimafuna Inu,
Ubwere Ufumuwo, Mwapambana zonsezo;
Uoneke padziko ponse. Mlamulire mtima wanga,
318 Mndikhalitse wanutu.
1. PEREKANI mtima wanu, 320
Yesu aitana nonsenu; 1. ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
Osauka, amasiye, Ŵalira Yesu m’ntchito zakozi,
Yesu anakuferani ’nu. 85
Perekani, perekani Ŵalira Yesu pofanana ndi
Mtima wanu nonsenu; Ambuyathu Yesu Kristu.
Yesu akulindirani, Tiŵaliretu, tiŵaliretu
Perekani mtimawo. Ambuye Yesu wotikonda ’fe;
2. Tsegulani mtima wanu Mlemekeze ’Ye tsiku lonseli,
Nonse, Yesu akaloŵemo; Ine tiŵalire Yesu.
Akuchimwa, Iye adzaloŵa nazo 2. Ŵalira Yesu pazobvutazo,
zakukomatu. Ŵalira Yesu pakukondwanso,
3. Mtembenuke mtima wanu, Ŵalira Yesu, imbirani ’nu
Inu osamvera Mlunguyo; Ambuyathu Yesu Kristu.
Yesu aitana ife 3. Ŵalira Yesu wolimbitsayo,
Tikamtsate m’njira yakeyo Ŵalira Yesu m’moyo monsemo
4. Perekani mtima wanu Ŵalira Yesu; tidzaonatu
Kwa Mbuyathu Mpulumutsiyo, Ambuyathu Yesu Kristu.
Ndiye wakudziŵa kuchiritsa
Anthu akuchimwatu. 321
1. ZAMBIRI zogona m’kholamo,
319 Zosungika bwino ’mo;
1. YESU, Bwenzi la ochimwa, Koma imodzi inasokeradi,
Yesu wondikondable, Nitayika m’thengomo
Ena samandikwanira, Kutali kuphiri loopsalo,
Yesu salephera ’yi. Kutali ndi mbusa wakeyo.
Aleluya Mpulumutsi! 2. Ambuye, muli nazo zambirizi,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Kodi sizifikirazi? Maumtima muli mwai;


Koma Mbusa nanena, “Yangayo Ndi Yesu ndikondanetu,
Yatayika naneyo; Si kanthu kena ’yi,
Ngakhale njira njoopsadi, Si kanthu kena ’yi.
Ndilinga kuphiri kuipezanso.” 323
3. Koma zina sizinadziŵa ayi,
1. ATATE Wamkulu ndi
Makwaŵa ’napyola ’ye,
Wamphamvu zonse,
Ndi mdima woopsa WA usikuwo
Atate Wamkulu ndi wamphamvu
Ambuye nailonda yake.
Zonse,
Anamva kulira kutaliko,
Khalani ndi chifundo ndi ife lero.
Naipeza yofoka, yakufayo.
2. Ifetu kuchimwa timachimwa,
4. Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
Mbuye,
Panjira ponsepo?
Ifetu kuchimwa timachimwa,
“Ndaukhetsa potsata iwetu,
Mbuye,
Kukubweza ku kholalo.”
Mutume Mzimu wanu
Ndi m’manja mwalaswa
Atiphunzitse.
Bwanjimo?
3. Mwa Mzimu muloŵe mumitima
“Ndalaswa ndi minga pofuna
Yathu,
Iwe.”
5. Ndi ponse paphiri ndi padambopo 86
Ndi makwaŵa, indetu, Mwa Mzimu muloŵe mumitima
Kunakwera kupfuula Yathu,
Kumwambako, Zoipa zathu zonse mtiululire.
“Kondwani, ndaipeza yanga!” 4. Tafika Kwa inu mutiunikire,
Nd’ angelo a Mlungu Tafika kwa inu mutiunikire,
nabwezanso, Chifundo chanu chonse taleka
“Kondwani, Ambuye ’napeza lero.
yawo.” 5. Tifuna kuchita chifuniro chanu,
Tifuna kuchita chifuniro chanu,
322 Chifundo cha Mulungu
1. MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga nchabwino chokha.
Kukonda kwanuko: 6. Atate, mupatse zomwe
Mwa Mlungu ndidzalimbika, tapemphazi,
Ndisasokerenso, Atate, mumpatse zomwe
Ndisasokerenso. tapemphazi,
2. E, moto wanu woyera Tapempha m’Dzina lake la
Uyake mwa ine; Mpulumutsi.
Utenthe zonse zoti bii,
Undiyeretsedi, 324
Undiyeretsedi. 1. ONA Mwanawankhosayo
3. Munagwa pa Atumwiwo; Wakuseza zakuipa zathu zonse.
Dzazani mwa ine; Mwanawankhosa
Mzimu wamoto Woyera, Watisenzera
Ndipempha mudzetu, Zakuipa zathu zonse.
Ndipempha mudzetu. 2. Anazenza m’thupi mwake;
4. Ndikhazikike inetu, Pakukhomedwa pa mtanda anali
duu.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

3. Ona pamtanda Yesuyo Ithamange m’ntchito yanu


Anabvutika chifukwa cha anthu Yokhayo.
’fe. 6. Ndi milomo yathu iyinso njanu,
4. Imva kulira kwa Yesu Ilalike Mawu anu kwa onse.
Pamene anasiyidwa muimfayo. 7. Ndi makutu athu awanso nganu,
5. M’mwazi wake tisambamo; Muŵamvetse Mawu anu okhawo.
Zichotsedwa zakuipa zathu zonse. 87
(Ona Mwanawankhosayo 8. Tidziperekadi konse Kwa Inu
Wakusenza zakuipa Tikakhale anthu anu okhawo.
Zathu zonse.)
327
325 1. ATATE, ndipempha
1. YESU analikhanda Tsopano mundimvere,
M’Betlehemumo; Ndipempha kuti mundithandize.
M’ngelo anasimba za 2. Ine ndili munthu
Kubadwa kwake. Wochimwa pansi pano,
Kubadwa kwa Yesu Munditsuke Mbuye, ndiyeretu.
M’Betlehemumo; 3. Ndalema ndathodwa
Khandalo linagona Ndi zinthu zapadziko,
M’khola la ng’ombe. Zakhalatu goli londimanga.
2. Mngelo anatumidwa 4. Yesu Mfumu Inu
Kuŵasimbira Mumandiuza kuti:
Abusa a nkhosa za “Pemphera, ndipo udzalandira.”
Kubadwa kwake. 5. Ndipempha, Ambuye,
3. Anapita nasiya Mundidzaze n’chikondi,
Nkhosa zawozo; Mtima wangawu ukukondeni.
Anapita kumudzi
Kukamlambira. 328
4. “Tadodoma, abusa, 1. DZIKO lonse mlambire
Kwachitikanji? Yesu Mbuye wathuyo,
Mwazisiyira yani Muimbire ndi chimwemwe
Nkhosa zanuzo?” Dzinalo.
5. “Posunga nkhosa ife 2. Mbwere nonse muone
Kubusa kwathu Zomwe achita Yesu:
Mngelo anasimba za Nzozizwitsa, nzodabwitsa
Kubadwa kwake.” Ntchitozo.
3. Aweruza ndi mphamvu
326 Ku nthaŵi yamuyaya;
1. ATATE, tifika pamaso panu; Dizo Lake Lisamala
Mukomane ndi ife, Mbuye wathu. Am’dziko.
2. Mitima yathu iyi nayo njanu, 4. Mbwere mudzamve nonse
Muiyeretse, muikonze Mbuye. Zamphamvu za Yehova;
3. Ndi maso athu awa nawo nganu, Mumwibire, mumyamike
Muŵapenyetse zinthu zanu zokha. Yehova.
4. Ndi manja athu awa nawo nganu, 5. Tisonkhane tonsefe,
Agwiretu ntchito yanu yokhayo. Tigwadire Ambuye;
5. Ndi miyendo yathu iyinso njanu, Timlambire, timlambire

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Yehova. Naitana atate


329 Kupereka mzimu wake:
“Mlungu wanga, Mlungu wanga.
1. Mlungu akuyanganiradi
Mwandisiy’ranjitu Ine,
Kufikira tionana. Mundikweze m’Mwambamo,
Azasunga nkhosa zake; Landirani mzimu wanga.”
Mlungu akuyang’aniredi 4. Ankhondowo Poona
Zinachitika pamtanda,
E! Tidzakomanansotu Anabaya m’nthitimo,
Pamapazi a yesu, Munatuluka magazi.
E! Tidzakomanansotu Paphirilo la Golgota
Anaferapo Mbuyeyo
2. Mulungu akuyan’ganiredi. Nasauka koopsya
Mulungu akuyan’ganirenidi Ndi zoipa zathu izi.
M’dzanja mwake akulere, 331
Ndi mapiko akubise; 1. TUMPHATUMPHA moyo wanga,
Mulungu akuyan’ganirenidi. Sangalala ndi Mtetezi;
Kuwombola Kwa Yehova
Kwatuluka m’dziko lako.
Mulungu wakwezekatu,
88
Mpulumutsi m’dziko lako,
330 Wakwezekatu Chitetezo.
1. POTULUKA m’mudzimo Wabvundikira iwedi
Yesu anasenza mtanda, Mzimu wanga’we wafunda,
Pokwera ku Gologota Lulutiratu moyo wanga.
Kukampachikatu Mbuye. 2. Bvinabvina moyo wanga,
Pilatoyo, mfumu yawo, Lulutira mtima wanga;
Inampereka kwa ’Yuda, Wa mawuwo a Yehova
Kuti ampachiketu Watuluka m’dziko lako.
Kufera zoipa zathu. 3. Imbirira moyo wanga,
(Atate ’nu amayi ’nu, nonsenu, Mtendere wako wafika;
Onani Yesu wasenza mtanda; Mbendera ya Chitetezo
Atate ’nu, amayi ’nu, nonsenu, Waikwezetsa ndi Yesu.
Onani Yesu wasenza mtanda.) 4. Ukondwere moyo wanga,
2. Zoopsya zopambana Kuunika kuoneka,
Zinachtika pamtanda Ndi mdimawo uthaŵatu;
Kuti mdima unadza, Lulutira moyo wanga.
Dzuŵa linabisikanso. 5. Usekere moyo wanga,
Chinsalucho cha m’kachisi Ndi Yehova akufuna;
Chinang’ambika pakati, Wakwezatu mbenderayo
Myala inaswekanso, Ya Chitetezo, sekera.
Dziko linagwedezeka.
3. Pomwalira Mbuyeyo 332
Anapfuula kokweza 1. PAKUONA imfayo
Chisonicho chikula

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Ndilira misozi. AMEN, Amen, Amen.


Ndilira, ndilira, 335
Ndilira Mbuye Yesu wangadi.
1. NDIDZE pafupi pa
Ndaimba ndi kulira ndi kusisima,
Mlungu wanga,
Ndaimba ndi kulira ndi kusisima,
Ngakhale pamtanda
Ha! Ha! Aleluya!
Mundikweza;
Ha! Ha! Aleluya!
Koma ndiimbabe
Mwasiyiranji Ambuye Yesu?
Mbuye mndikhalitse,
2. Ndinasiya amayi,
Mbuye mndikhalitse,
Ndinasiya atate,
M’fupi Ndinu.
Abale komweko.
2. Ngakhale kuthengo
3. Kazembe wanga m’matenda,
Ndili m’manja mwa Mbuye. 89
Abale tsalani. Ndasokera,
4. Zoipa zakanikadi, M’mdima ndigonapa
Sizikhoza kuchotseka, E, pamwala;
Ndilira misozi. Koma m’kulotako
5. Angelo aitana, Ndiyandikizanso,
Aitana Kumwambako, Ndiyandikizanso
Tiyeni, tikwere! M’fupi Ndinu.
6. Munafera pa mtanda 3. Pajapo ndipenya
Chifukwa cha inedi, Pokwerapo,
Si cha wina ayi. Angelo atsika
Kumwambako,
333 Ndiwo akodola
1. LIDZE msanga dzuŵa lanu Kuti ndikabwere,
Lolonjezedwa, Ambuye. Kuti ndikabwere
Mnalinena polaŵira M’fupi Ndinu.
Kwa anyamata, Ambuye. 4. Tsopano poukanso
Kuli chimwemwe m’dzuŵalo Wokondwatu,
Lakufika Ambuye. Ndipeza pomwepo
Ha! Ambuye bwerani. Pali Mlungu;
Ha! Ha! Ambuye bwerani. Ndipo masautso
2. M’dziko lino chimwemwecho Andisendezanso,
Chakudza ndi Yesu Mbuye. Andisendezanso,
Mfumu yathu ya Kumwamba M’fupi Ndinu.
Ndi dziko lonse lapansi. 5. Pena pakufadi,
3. Adzakhala pampando N’kwera m’Mwamba,
Wakuweruza makamu; Dzuŵa ndi nyenyezi
Amitundu adzaima Zitsalira;
Pamaso pa Mbuye Yesu. Pomwe ndiimbanso,
4. Adzanena kwa anthuwo Ndidza pafupi pa,
Akudzanjatu lamanja, Ndidza pafupi pa
“Loŵani ’nu m’chikondwero Mlungu wanga.
Cha Atate nthaŵi zonse.”
336
334 1. Munasiyatu
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Dziko lanulo, Ataya zoipa;


E! Chifukwa cha tse; Omwe asamba mwa uyu
Ndi ku betlemuko Ataya zoipa.
Pakubandwa inu. 2. Woba wakufa ’napenya
Nyumba zao nakukanani. Kasupe, nakondwa,
Ndimo inenso mwa uyu
Ndisamba ndiyera.
Mbuye yesu lowani m’mtima,
Ndisamba ndiyera,
Nyumba yanu ndimtimanga Ndisamba ndiyera;
. Mbuye yesu lowani m’mtima, Ndimo inenso mwa uyu
Nyumba yanu ndimtimanga. Ndisamba ndiyera.
3. Mwazi wa Yesu wokondwa
2. Akumwambawo Ukhala wamphamvu
naimbitsatu, Kwa ana onse a Mlungu,
kukulemekezani Uchita kwombola.
koma monga mwana, Uchita kwombola
mziko munabadwa, Uchita kwombola;
munadzichepesadi. Kwa ana onse a Mlungu
3. nyama za mthengo Uchita kwombola.
4. M’mene ndapenya mwazi wa
Ndi mbalamezo,
Mabala anuwo,
Zili nazo zogonamo.
Kukonda kwathu nditama
Koma mwana wa mulungu Kwa kutha kwa moyo.
Analibe nyumba, Kwa kutha kwa moyo,
M’mapululu nagonatu. Kwa kutha kwa moyo;
4. munadzera ndi Kukonda kwanu nditama
mau amoyo, Kwa kutha kwa moyo.
Akupulumutsa anthu; 5. Kumwamba ndikaimbanso
anakanidza, Zimphamvu za Mlungu,
anatsautsa, Zopulumutsa onsewa
anapichika inu. Omvana ndi Yesu.
5. M’mene mubwera Omvana ndi Yesu,
Kutiweruza Omvana ndi Yesu;
Zopulumutsa onsewa
Ndi angolo oimbira,
Omvana ndi Yesu.
Mundiitane,
Muti “idza’wo, 338
Khala nane kumwamba. 1. Yesu and’itana
Adzandiyeretsa,
337 Ndi mwazi wake wkhetsa,
1. KASUPE ali wodzaza Paphiri gologota.
Ndi mwazi WA Yesu;
Omwe asamba mwa uyu
Ataya zoipa. Ndlikudzatu,
Ataya zoipa, Ndidza Kwa inu;

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Munditsuke m’mtimamo
Ndi mwazi wanuwo 4. Kalekale ndinathawa,
Ndinakana kumvera inu;
Koma lero ndamva kuti
2. Ndafoka, ndaipa, Muli mwini wake wa moyo.
Mundilimbikitsetu;
Mundiyeletse konseko,
340
1. MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
Ndiyereyere mbuu. Ndi nyimbo zake zakuitana:
3. Atero ndaniyo? “Loŵa, loŵa,
Ndi yesu wabwino; Tsopano loŵatu.”
2. Mdima ufika, dzuŵa laloŵa,
Apatsa mvanu mtendere Nthunzi zilipo, wadza usiku.
Ndimphamvu m’mtimamo. 3. Nyumba yodyera ilikudzaza;
4. Yesu akhzika, Idza nuloŵe, Mkwati anena:
Zonse za m’katimo; 4. Chakudya ichi ndi cha iwenso,
Nalonga mzimu woyera 90
Madzi amoyo umwe kolere.
Munafoipamo. 5. Onse am’Mwamba Ali momwemo,
5. Nditam mwaziwo! Ndipo Angelo akuitana:
Nditama chifundo! 6. Mawu a Yesu ati: “Msangatu
Nditam yesu ambuye, Idza, wochedwa, loŵa
Nditenga mphamvu “ko. m’nyumbamo.”
7. Msanga adzachitseka chitseko,
Adzakuuza: “Choka, chokatu.”
Choka, choka,
339 Anena chokatu.
1. Ndi misozi ndi chisoni 341
Ndiliratu Kwa inu yesu. 1. PAMTANDAPO, pamtanda,
Ndichifundo chandi gwira Yesu ’nafera;
Ndirila kuti ndine wanu. Pamutupo chilemba,
Chisoni ine.
E! kwa inu, E! kwa inu, Analira, “Eloi, Mlungu wanga!
Lama Sabakatani,
Ndirila kuti ndine wanu.
Mwandisiyiranji?”
2. Kumandako, kumanda
2. Mbuye yesu ndi atate, Yesu nauka;
Mundiona ndili wosowa Anaposa imfayo,
Ndimasowa mzimu wanu Watha zonsezi.
Kuyinga zonse za mumtima. Ndikondwera, Mbuyanga
’Naukadi;
3. Mtendererewo wosanyenga
Sekerani nonsenu,
Ndirila ine m’mtima mwanga. Yesu ngwamoyo.
Kondimvets chimwemwetu 3. Pakukwera Kumwamba
Ndirila ine m’mtima mwanga. Yesu anati,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

“Musachoke m’mudzimu, Tikomana mwadzikolija.


Pempheranitu;
Mzimu Wakuyeradi adzabwera,
Kuthangata nonsenu, 2. Tidzaimba komwekonyimbo
Kuti msafoke.” Za abwino omvero yesu.
4. Uzanitu abale, Sitizamva chisoni Ife.
Onse alongo, Tidzakondwe masiko onse.
Ndi amitundu yonse
Adzakondwera. 3. Tidzatama atate wathu
Musaope ntchitoyo yokomadi, Kuti iye napatsa yesu
Mphotho yake Kumwamba, Kuchotsera zochimwa zonse
Moyo wosatha. Ndikutidalitsira Ife
342 344
1. M’DZIKO lino tikhalamo APITA anzathu dzuŵa lino
Utibvuta moyo, Kosaoneka,
Koma dziko la mtendere Apita anzathu dzuŵa lino,
Lili kwa Mulungu. Apita anzathu dzuŵa lino
2. Watitsogolera Mbuye, Kosaoneka.
Komwe Kwa Atate, A! Kumwamba
Ndimo tidzatsata naye A! kuli a Yesu.
Moyo wathu wonse.
3. Ndi tsopano tilindira
345
1. INE ndili ndi manyazi
M`dziko lathu lino;
Kuti kale lomwelo
Ntchito atipatsa Mlungu,
Ndinanyoza kudza komwe
Tizigwira bwino.
Kwa Mtetezi wanga Yesu,
4. Ngati zakuipa zathu
Ndati, Sindimfuna `yi.
Zikatisautsa,
2. Koma Iye wandipeza;
Tithaŵire kwa Mbuyathu,
Ndamuona m`mtandamo,
Atipulumutsa.
Mwa kufera ine momwe;
5. Timpemphere kutipatsa
Ndipo ndati m`mtima mwanga:
Mtima watsopano,
Mbuye, ndikufunani.
Kutithandizira kunka
3. Nsiku zonse kwanja kwake
Paulendo uno.
Kunandithandizatu,
343 91
1. kuli dziko la bwino mwamba Kunandichiritsa mtima;
Lakuwala kopotsa dzuwa; Ndipo ndati: Mpulumutsi,
Yesu atikonzera malo Ndinu Mbuye wangatu.
4. Sindifuna Mbuye wina,
Pokarila Ife komweko. Koma Yesu yekhayo;
Ine ndili munthu wake,
Bwinoli tipita Iye anandigonjetsa
Ndi kukonda kwakeko.
Tikomana mwadzikolija,
Bwinoli tipita 346
1. KONDWANI nonsenu,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Mpulumutsi anadza; 1. MEMA nkhondoyo, wadza


Onani kukhola, Mdaniyo,
Ndi mtanda ndi manda Kweza mbendera ya Mbuye.
Mlemekeze, bukitsani, Bvala zidazo, imba nyimboyo,
Naferatu kale; Khazikikatu pa Mulungu.
Kondwerani, mlemekeze Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
Akhaladi moyo. Limbanitu, nkhondo nja Yesu.
2. Kondwani nonsenu, Musafoke, m’thyole linga lawo;
Anakhetsatu mwazi, Mbuye ndiye Wopambanayo.
Natiwombola nawo, 2. Mlungu mverani, mphamvu
Tikhale ana ’ke. Patseni,
3. Kondwani nonsenu, Tithandizeni, tipempha.
Atikhululukira, Nkhondo itatha, titapambana,
Wosachimwa nafera Tidzalandiratu korona.
Anthu ’fe oipa. 3. Mlake mdaniyo, mwimbe
4. Kondwani nonsenu, m'njiramo
Mfumu yathu yakwera; Mpaka nkhondoyo ileka.
Kwa Atate Kumwamba Zida konzani, mantha tayani,
Atipempherera. Pitikitsani adaniwo.
5. Kondwani nonsenu, 349
Adzabweranso Yesu,
1. M'MANDA, nagonamo
Waulemu, wamphamvu,
Yesu Ambuye,
Kuweruza dziko.
Anadikiratu
347 Tsiku lija.
1. TATE ndili mwana wanu, M'manda naukamo
Nkana ndinachimwa, Napambana ’'dani akewo;
Ndingolirira kwa Inu; Anauka kupambana imfayo,
Khululukireni. 92
Machimo anga ngambiri Ali moyo ndi oyeramtimawo.
Osaŵerengeka, Wauka, wauka!
Ndingoyang’ana kwa Inu; Aleluya wauka!
Khululukireni. 2. M'manda munalibe
2. Ndinachimwa poganiza Yesu Ambuye,
Ndi polankhulanso, Nadikira chabe
M'ntchito zanga ndachimwanso; Alondawo.
Khululukireni. 3. Imfa yalephera
3. Ndinachita mphulupulu, Kumutsekera,
Ndinakunyozani, Anachotsa zonse
M'ntchito zanga ndalephera; Zomzingazo.
Khululukireni.
4. Zonse ndinakonda kale 350
Ndi zopanda pake, 1. YENDANI, Mfumu yamtendere
Sindinakhuta nazotu; Anthu akuimbirani;
Khululukireni. Apfuuletu Hosana,
Agonjeranso anthuwo.
348 Yendanitu m'ulemudi,

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Pulumutsani anthuwo. Zinthu zonse pansi pano


2. Yendani, Munthu Wachisoni, Sizikondweretsa ife.
M’mudzi wa Yerusalemu; 3. Mzimu, mlonge m’mtimamo
Angelo amapenya ’Nu Maphunziro achifundo;
M’mene mwafera anthuwo. Timve lero ndi maŵa
3. Yendanitu, Wansembe wathu, Ndi masiku onse Yesu.
Mtanda wanu mwanyamula Ndimo m’Mwamba tidzaona
Watisandukira dalo, Tidazimva pansi pano.
Watitengera moyowo. 353
4. Yendani mwaulemerero,
1. PEMPHERO ndiko kufuna,
Akulindirani mphotho,
Kulakalakatu;
Moyo wanu wosatha
Ndi monga moto liyaka
Watilonjezera moyo.
Mumtima wa munthu.
351 2. Pemphero ndiko kulira,
1. KAMWANA Yesu ’nabadwa, Ngakhale misozi,
Ndi Iye Mlungu Wamphamvu; Kupenyetsetsa Kumwamba,
Angelo anapembedza Mulungu mpafupi.
Mwana wakhanda Iyeyu. 2. Pemphero ndiko kufuna
2. Kamwana kaja ’nayamba Kwa mwana wamng’ono;
Kuonetsera Atate, Ndiponso mawu amphamvu
Lero anena Kumwamba: 93
“Tiana tidze Kwa Ine.” A munthu wamvanu.
3. Tibwera ndi tianato 3. Pemphero ndiwo mweyawo
Kukabatiza ’menewa; Apuma akristu;
Muŵachitire chifundo. Ndi mapemphero tiloŵa
M’ŵapatse Mzimu Woyera. Dziko la imfalo.
4. Angelo anu asunga 4. Mutiphunzitse, Mbuyathu,
Tiana tathu tofoka; Kupempha kotero,
Pa njira yanu tiyenda, Kuyandikira kwa Mlungu
Mulembe m’Mwamba maina. Ndi mtima wabwino.
5. Mukonda nyimbo za ana,
Kokoma amaimbatu; 354
Ndi ana athu atama 1. Ndisauka, ndinachimwa,
Atate, Mwana ndi Mzimu. Koma inu mnandifera,
Ndimo ndamva mnd’itana
352 Mwana mlungu ndingubwera.
1. YESU Mbuye, onani
2. Ndisauka, ndimasowa
Tadza poitana Inu;
Mpamvu ya kuyera m’mtima
M’dzina lanu tifika
Osekera Kwa Atate; Mwazi wanu wanditsuka;
Mkhale nafe Inu nokha Mwana mlungu ndingubwera
Tikaimba nkupemphera. 3. Ndisauka, sindikhoza
2. Mbuye, Mzimu Woyera Kuiletsa nkhondo m’mtima,
Munapatsa ana anu Ndichisoni, mantha, nkhawa
Kukalonga mumtima Mwana mlungu ndingubwera
Mawu ndimo mvanu womwe: 4. Ndisauka, sindiona

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Ndingudwale, ndilefuka, Kuti anthu ena


Zonse ndizitaya Kwa ‘nu, Amuone iye.
Mwana mlungu ndingubwera Yenda iwe, yenda.
Yenda iwe, yenda,
Siliva ndilibe;
Mwa Yesuyo, yenda!
2. Kukondwa kwa wodwalayo
5. Inde yesu mulandira. Kunali kopambana;
Muchilitsa, mpulumutsa Iye anatumphatumpha,
Mau anu ndivomera Kuzungulira
Mwana mlungu ndingubwera. Sunagoge yense.
6. Inde, yesu, mundikonda 3. Lero lino Mbuye Yesu
Zonse zina ndizitaya; Aitana nonsenu;
Tsono kukakhala wanu, Mukamvera ndi kumtsata,
Mwana mlungu ndingubwera. Mudzakondwera
Ndi mdalitso wake.
355
1. YESU, ndipemphera 357
Mndithangate 1. YESU watidzera, watidzera,
Kukonda Inutu, Way’tana anthu onse.
E, kwambiri. Udzimvere wekha.
Koposa zonsezo Aleluya, Aleluya!
Za pansi panopo, Aleluya, Aleluya!
Ndikondane Udzimvere wekha.
Ndinu Mbuye. 2. Kudziŵa ukudziŵa, ukudziŵa,
2. Kale ndinafuna Kulibe zachisoni.
Za pansipa, Udzimvere wekha.
Tsopano ndilira 3. Atumwi atumika, atumika,
Inu nokha. Akulalika Yesu.
Ndifuna kukonda Udzimvere wekha.
Inu kopambana 4. Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
Zinthu zonse WA dziko lili lonse.
Za pansipa. Udzimvere wekha.
3. Inu ndidzatama 5. Kumva ulikumva, ulikumva,
Nthaŵi zonse, Ungonyalanyaza.
Imfa ikafika Udzimvere wekha.
Ndidzanena: 6. Bwerani inu nonse, inu nonse,
“Ndifuna kukonda Mudzalandire moyo.
Inu, Mbuye wanga, Mudzimvere nokha.
Kopambana 358
Zonse zanga.” 1. MUDZE Kwa Yesu, musachedwe.
356 Kalata ilozera njira;
1. PANALITU wakudwala Amaitanatu tonsefe,
Amene akakhala Bvomerani Iye.
Pakhomo la sunagoge: Tidzakondweradi m’Mwambamo
94
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Posonkhana komwe kuli ’Ye; 4. Aliponso adani am’kati ndi


Tidzakhala naye komweko Akunja;
Ku Dziko losafa. Yesu watisekera, tidzakuimbirani.
2. Lolani ana, mumve Mlungu, 5. Aliponse mabvuto, ena ndi oipa;
Tsegulani mitima yanu, Yesu mutimasule Kwa adani athu.
Sankhani Iye, Bwenzi lanu; 361
Musachedwe, mudze.
3. Ganizansoni, ali pano, 1. Ndine mbusayo wabwino
Mthenga wake mverani lero; Ndinafera nkhosazo;
Mawu okoma ati lero, Yotaika ndaifuna,
Musachedwe, mudze. Mpaka ndataya moyo.
359
1. MWA ine, moyo wanga ndi Yesu Mbulu wandi’gamba nthiti
(Yesu) Yemwe anafera ine, Wandin’gambanso m’manja,
Ndiye anandiwombola; Wandin’gambira zbvala,
Yesu, Yesu. Ndasala waumphawi.
2. Mwazi wake ndi chitsime changa,
(Yesu) Pamene ndikasambamo
Zochimwa zanga zidzatha; 2. Nkhosa zanga zimandimva,
Yesu, Yesu. Ndikaziitanazo;
3. Yesu Mfumu, ine ndingadzafe Ndimazipatsa moyowo,
(Yesu) ngati mundisiya ndekha, Atate nazisunga.
Kukhala ndekha sinditha;
3. Atate wondipatsazo
Yesu, Yesu.
Ali nayo mphamvutu,
4. Yesu Mfumu, ine ndisekere
Kuzidyetas, kuzisunga
(Yesu) Inu Mpulumutsi wanga
Palibe wolandazo.
Pamene mukhala nane; 4. Mudzaona zovalazo
Yesu, Yesu. M’kati ali fisiyo;
360 Mananyengedwa anthuni,
1. LEKANI kubvutika ndi zinthu za Ine ndine mbusayo.
Padziko, 5. Tamverani anthu inu,
Musekerere kuti tidzaimbira Yesu. Ine ndine mbusayo;
Imbira! Ndine njira, ndine khomo
Timwimbire Yesu, Thawani mimbuluyo.
Mpulumutsi wathu! 363
Imbira! 1. TIYAMIKE mbuye Yesu
Timwimbire Yesu, Yemwe anatifera
Tonse tidzakondwera. Imfa ija yoopsetsa
2. Musadziunjikire chuma cha Kuwombola tonsefe.
Padziko Ife
Dzimbiri ndi njenjete Tapulumukadi,
Zimachiononga. Ife
3. Koma mudziunjikire chuma cha Tapulumukadi,
Kumwamba Imfa,
Kumene anapita Mtsogoleri wanu.

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Imfa yoopsa ija yapamtanda, M’ulemerero wake!


Imfa, 2. Tsopano ndimwona Iye
Imfa yoopsa ija yapamtanda. Mwa chizimezimetu;
2. Panalibe mwa abale Tsiku lija ndidzaona
Yemwe akadakhoza Ulemerero wake.
Kupereka moyo wake 3. M’mene masautso onse,
Kuwombola tonsefe. Nthenda, imfa, zidzatha,
3. Tikondwera ife tonse Dziko likadzakonzedwa,
Pakuona ntchitoyo Ndidzakondwa koposa.
Anachita Mbuye Yesu 4. Lodala tsiku lomwelo
Kuwombola tonsefe. Ndidzamwona Yesuyo,
364 Mpulumutsi wanga yemwe
Anandikonda ine.
1. MZIMU ndi mtogoleri
M’njira yachikristuyo, 366
Atitsogoleratu 1. MVERANI mbiri yozizwitsa
Paulendo wathuwu. Ya Yesuyo kalelo;
M’yoyo ikondweratu Iyeyo ’nadza pansi pano
Pomva mawu akewo, Kutipulumutsa ’fe.
Pakunena Mzimuyo, Ndani anatiwombola?
“Osokera, bwerani.” Mwana wa Mlungu pa mtanda.
2. Bwenzi lathu ndinutu, Anatani?
95 Anafera.
Mkhale m’fupi nafetu; Ali kuti?
Msatisiye tokha ’fe Akhaladi m’Mwamba
Pakuyenda m’mdimamu; Kutipempherera.
Pakuwomba mphepozo 2. Palibe m’modzi akanatha
Timaopa m’mtimamo, Kuloŵa m’malo mwake;
Tsono timve mawuwo: Ngakhale anali wamkulu
“Amantha ‘nu, bwerani.” ’Nasiyidwa namnyoza.
3. M’mene ntchito yathatu, 3. Kodi mudzampembedza Mbuye
M’mene tidikira ’Nu, Mpulumutsi wathuyo?
Pakukhumba m’Mwambamo, Kodi inu mudzaloŵamo
Tsono tipempherabe. Mu Ufumu wakewo?
Nthaŵi ya mabvutowo 367
Tikhulupirira ’Nu, 1. Ufuna kowomboledwa kodi?
Tsono timve mawuwo, Ilipo mphamvu m’mwazi wake,
“Okondedwa, bwerani.”
Ufuna kugonjetsa zoipa?
365 Muli mphamvu m’mwazi wake.
1. MASO ndi maso ndi Kristu,
Kodi ndidzachitanji Muli mphamvu yodabwitsatu
M’mene ndidzaona Yesu, M’mwazi WA yesuyo
Yemwe anandifera? Muli mphamvu yodabwitsatu,
Ndidzamwona maso ndi maso
M’mwazi wamwana WA nkhosa.
Kuseri kwa mitambo;
2. ufuna kuleka kunyadako?
Posachedwa ndidzamwona

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Ilipo mphamvu m’mwazi wake, (mloŵetsenitu).


3. idzatu pa mtanda nutsukidwe. 2. Utsegule mtimawo,
Muli mphamvu m’mwazi wake. Mloŵetseni
3. ufuna kuyera kopambana? (mloŵetsenitu),
Ilipo mphamvu m’mwazi wake, Ukachedwa achoka,
Zoipa zonse azayeretsa Mloŵetseni
Muli mphamvu m’mwazi wake. (mloŵetsenitu):
4. ufuna kugwera ntchito yake?, Ndiye Bwenzi lakolo,
Ilipo mphamvu m’mwazi wake, ’Dzapulumutsa ’we;
Ufuna kumuimbira iye? ’Dzakusamaliranso,
Mloŵetseni
Muli mphamvu m’mwazi wake.
(mloŵetsenitu).
368 3. Imva mawu akewo,
1. MPULUMUTSI Wokondedwa, Mloŵetseni
Mwandipulumutsa ine; (mloŵetsenitu),
Ndine wanu, wanu nokha, Sankha Iye leroli,
Wotsukidwa m’mwaziwo. Mloŵetseni
Aleluya, Aleluya, (mloŵetsenitu);
Mwanawankhosa ndinutu: Wangoima pa khomo,
Mwazi wanu wanditsuka, ’Dzakusangalatsa ’we,
Aleluya kwa Yesu. Udzamlemekezatu,
2. Mtima wanga wabvutika, Mloŵetseni
Zaka zonse ndingochimwa; (mloŵetsenitu).
Tsono sindikangalika, 4. Mlendo wa Kumwambayo,
Ndingopuma mwa Yesu. Mloŵetseni
3. Mwandipatulira ine, (mloŵetsenitu),
Kwa Inu ndidzipereka, ’Dzakupatsa zonsezo,
M’moyo, m’imfa mboni yanu Mloŵetseni
Ya chipulumutsocho. (mloŵetsenitu);
4. Aleluya, mwandigula, ’Dzakhululukira ’we,
Ndipo mudzandisungabe; Ndipo potsirizapo
Mwazi wanu ndi wamphamvu ’Dzakutenga m’Mwambamo,
Kuyeretsa konseko. Mloŵetseni
(Mloŵetsenitu).
369
1. MLENDO ali pakhomo, 370
Mloŵetseni 1. NDIPEREKA zanga zonse
(Mloŵetsenitu), Mwaufulu Kwa Yesu;
Wadza kalekalelo, Ndidzamkonda kopambana,
Mloŵetseni Tsiku lili lonsetu.
(Mloŵetsenitu); Ndiperekatu
96 Zonse Kwa Yesu;
Mtsegulire msangatu, Ndipereka zonse Kwa ’Nu,
Wakuyerayerayo, Dalitsenitu.
Mwana wa Mulunguyo, 2. Ndipereka zanga zonse
Mloŵetseni Pamapazi a Yesu;

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Zapadziko ndazikana, Ambuye yesu.


Nditengeni Yesu ’Nu. 3. Chiso chandisungadi,
3. Ndipereka zanga zonse, Panjira yangayo,
Ndipo n’khale wanutu; Chisomo chidzasunga ne’
Mzimu wanu ’ndidziŵitse Mpakatu kwathuko.
Kuti ndine wanudi. 4. Kwathu tizaimba nyimbo
4. Ndipereka zanga zonse, Ya chisomo chake,
Ndili wanu ndense ’ne; Yolemekeza mlunguyo
Nditamanda Dzina lanu, Munthawi zosatha.
Aleluya, Ambuye.
373
371 1. CHITETEZO chachikulu
1. Kwathu sipaziko, ndingopitilira Chotuluka m’mwaziwo
Ndazikundikira chuma kumwambako WA Ambuye Yesu Kristu,
Mungelo akodola pakhomo la mwamba Mpulumutsi wathuyo.
Ndipo dziko la pansi sindiyetsa kwathu. Mpulumutsi, chitetezo
Chipezeka m’mwaziwo.
Muye, ndinu bwenzi langa ndithu 2. Ndi chimwemwe ndimaona
Ndichitenji ngati kumwamba sikwathu Mtsinjewo wa mphamvutu;
Zonditsutsa zachotsedwa,
Mungelo akodola pakhomo la mwamba
Yesu wanditsuka mbuu!
Ndipo dziko la pansi sindiyetsa kwathu.
Mpulumutsi, chitetezo.
Chindisangalatsatu.
2. Andiyembekeza aulithuchi ndidziwa 3. Tchimo lonse ligonjera
Mpulumusi wanga wondikhululukira Chikondicho cha Yesu,
Adzandi pyolesa pamene ndafoka. Maganizo ’yeretsedwa;
Ndipo dziko la pansi sindiyetsa kwathu. Ndingofuna zakezo.
3. Mayi watsogola ku ulemelero, Mpulumutsi, chitetezo
Ndfuna kugwira dzanja Lake Konko. Chigonjetsa mtimawu.
Andi dikhilanso pakhomo la m’mwamba 4. Ndili nawo moyo w’satha
Ndipo dziko la pansi sindiyetsa kwathu. Wochuluka mwa Yesu,
4. Mu ulemelero tidzakhala m’yaya, Mzimuyo wadzaza mtima
Oyeramtimawo alikulambira. Ndi chimwemwe chakecho.
Mpulumutsi, chitetezo,
Ati, “aleluya kwa mlungu wa mphamvu’
Chiyanjano chomwenso.
Ndipo dziko la pansi sindiyetsa kwathu. 5. Mantha, nkhaŵa, ndi chisoni
Zachotsedwa zonsezo;
372 Mbuyeyo ndimkhulupira,
1. Chisomo chodabwitsacho, Anditsogoleratu.
Chapulumutsa ne’ Mpulumutsi, chitetezo,
Woipa wapambanatu Ndimkondadi Yesuyo.
Ndapeza moyo ne’ 374
2. Chisomocho chachotsatu 1. AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
Mantha a infa, Nanga inu? Nanga inu?
Pakukhulupirira ye’ Tapeza chipulumutso ndithu;
Nanga inu?

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Masiku onse timakondwera Mdalitse Mtsogoleri, nafe,


Pakumva Mawu ake a Yesu; Ndi Mayi Malaŵi.
Wolalikira tidzamumvera; 2. Malaŵi dziko lokongola,
Nanga inu? La chonde ndi ufulu,
2. Ife tiyembekezera YESU, Nyanja ndi mphepo ya m’mapiri,
Nanga inu? Nanga inu? Ndithudi tadala;
Chimwemwecho chili Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
Mumtimamu; Mphatso zaulere;
Nanga inu? Nkhalango, madambo abwino,
3. Titasokera tinabwerera, Ngwokoma Malaŵi.
Nanga inu? Nanga inu? 3. O! Ufulu tigwirizane
Tidziŵa kuti ndiwo uchimo; Kukweza Malaŵi;
Nanga inu? Ndi chikondi, khama, kumvera,
4. Tinachoka munjira ya imfa, Timutumikire;
Nanga inu? Nanga inu? Pankhondo nkana pa mtendere
Takopeka ndi Mawu a Yesu; Cholinga n’chimodzi,
Nanga inu? Mayi, Bambo, tidzipereke
375 Pokweza Malaŵi.
1. MBUYE dalitsani Afrika, 377
Itukulidwe nyanga yake; 1. ANTHU m’maiko onse
Mverani mapemphero athu, Akhala mitundu;
Ndipo mtidalitse ife ana anu. Kapena m’dziko lino
Mbwere Mzimu, Akhala anzathu;
Mbwere Mzimu, mbwere! Agona mwa zoipa,
Mbwere Mzimu Apulukiradi,
Mbwere Mzimu,mbwere! Ati, Mutilangize
Mbwere Mzimu Abale, bwerani.
Woyera, Woyera. 2. Ngakhale alemera
Mbuye, dalitsani Ndi chuma cha dziko,
Ife ana anu. Kodi akakondwera
2. Dalitsani mafumu athu, Opanda Mulungu?
Akumbukire Mlengi wawo; Kodi akhala mwaŵi
Aope ndi kunjenjemera, Otsata zawozo?
Ndipo m’ŵadalitse iwo ana anu. 98
3. Dalitsani mafuko onse, Iyai, awonongeka,
Aweruze bwino maiko; Apeza tsokalo.
Adzichepetse ndi kuopa, 3. Ndi ife akudziŵa
Ndipo mtidalitse tonse ana anu. Chikondi cha Mlungu,
376 Kodi tidzaŵamana
1. MLUNGU dalitsani Malaŵi, Kuŵala kwa Kristu?
Mumsunge m’mtendere; Chipulumutso! Inde,
Gonjetsani adani onse, Tichibukitsetu,
Njala, nthenda, nsanje; Kuti mitundu yonse
Lunzitsani mitima yathu Ibwere kwa Yesu.
Kuti tisaope, 4. Akristu nyamulani

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

Maneno a Mulunguyo, Ndimo mudzazizwa potsirizapo.


Ndi moyo lalikani 2. Kodi muvutidwa naye katundu?
Pa dziko lonselo; Ngwolemera mtanda muusenzatu?
Ndi Yesu Mpulumutsi Ŵerengani madalitso anuwo,
Anatiferatu; Ndimo mudzaimba dzuŵa
Adzabvomera onse; lonselo.
Ndi Mwana wa Mlungu. 3. Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
378 Ganizani kuti Mbuye wanudi
Adzakupatsani zake zonsezo,
1. PADZIKO pano tikhalira
Chosagula chuma chanu
M’moyo wosauka;
chonsenso.
Komatu kwa Mulungu kuli
Dziko lakudala; 380
Mbuyathu Yesu wapitako, 1. YESU Mbuyetu, mwafera
Iye ’natsogola; Mphulupulutu zanga,
Tidzamtsatira ife tonse, Ndimo ndamva mund’itana,
Tsiku lomaliza. Mutitu, Msachedwa.
Tiyeni, tiyeni, 2. Zonse za m’dziko zidzatha,
Ku dziko lakudala; Koma za moyo m’Mwamba
Tidzafikira m’dziko ilo Zomwe zidzakhalitsatu,
Tsiku lomaliza. Chakatu ndi chaka.
2. Masiku tikatsala ife 3. Nyengo ifika, chenjera!
M’dziko mwathu momwe Adzakukana m’Mwamba.
Mulungu watipatsa ntchito, Lapa zoipa zakozo,
Tikazigwiritse. Kuti ukaloŵe.
Pamene zakuipa zathu 381
Zisautsa ife,
1. TAMANDANI Mbuye,
Tikapemphere Mbuye wathu,
Inu atate,
Atipulumutse.
Mpatse Yesu mitima yanu.
3. Ulendo wathu ukadzatha
Tidzafika kwathu, 99
Adzatifitsa ife komwe 2. Tamandani Mbuye,
Yesu Mbuye wathu. Inu mafumu,
Sitidzapeza masautso Mpatse Yesu mitima yanu.
M’dziko la Mulungu, 3. Tamandani Mbuye,
Tidzakondwera chikondwere Inu abale,
Nthaŵi zonse zathu. Mpatse Yesu mitima yanu.
4. Tamandani Mbuye,
379 Inu nonsetu,
1. POZUNZIDWA inu ponseponse Mpatse Yesu mitima yanu.
Ndi kufoka m’mtima nazo 5. Tamandani Mbuye,
zonsezo, Mipingo yonse;
Ŵerengani madalitso anuwo Aleluya, Aleluya!
Ndipo mudzazizwa potsirizapo.
Ŵerengani madalitsotu, 382
Anakupatsani Mlungudi. 1. MVERA mtima wanga ’we
Ŵerengani lina linanso, Akufunsa Ambuye;

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)
REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN)
(Edited by Martin Oxford Banda MATERO CONGREGATION)

“Wosauka WA’mphaŵi, Kwa ife kudzakhala mwayi,


Kodi undikondadi?” Kwa Inu ulemu.
2. “Ndakupeza womanga, 384
Ndamasula zinsinga,
CHIKHULUPIRIRO chathu
Ndakulonda kutali,
Tatchulachi pakamwapo,
Kodi undikondadi?”
Mulungu athandize ’Fe
3. “Akaleka amake
Chikhale cha mumtimamo.__
Kusungira mwanake,
Ine sin’kuleka ’yi,
Kodi undikondadi?”
4. “Ndakukonda ku imfa
Ndi chikondi chosatha,
Kwaulere, kwambiri, Reference
Kodi undikondadi?” Christian literature association of
5. “Msanga ndidzabweratu, Malawi
Udzaona ulemu,
Udzakhala ndi Ine, P.o box 503 blantire [© 1974]
Kodi undikondadi?”
6. Mbuye ndisaukadi, Unknown editor reformed chuch in
Chimachepa chikondi, Zambia
Mtima wanga mudziŵa,
, fisrt PDF edition [online 2017]
M’ndipunzitse kukonda.
383 Martin banda seconding PDF edition
1. MBUYE mtsitsimutse [2018 June]
Ntchito zonse zanu!
Utsani anthu akufa
Ndi mawu a mphamvu.
2. Mbuye mtsitsimutse
Ntchito zonse zanu!
Tauzirani pa ife
Ndi mweya wa Mzimu
3. Mbuye mtsitsimutse
Ntchito m’mitimamo!
Mumvetse njala kwa Inu—
Mutikhutitsenso.
4. Mbuye mtsitsimutse
Ntchito m’kati mwa anthu!
Chikondi chawo chikule
Muchikolezetu.
5. Mbuye mtsitsimutse!
Mawu alimbike,
Pamene aphunzitsidwa
Onsewa amvere!
6. Mbuye mtsitsimutse!
Mzimu adzazetu!

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA NYIMBO ZA KHRISTU (HYMN) (Edited by Martin Banda MATERO CONGREGATION)

You might also like